Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,

  1. Home   »  
  2. Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,

Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,

 

YESU ndiye Mbuye wanga,
Ndamva mawu akewo;
Anandilandira ine,
Nandipulumutsatu.

Mwalembedwa mukalata,
Mawu ake omwewo;
Kuti iwo akumvera,
Akalandiridwatu.

Ndinakhala woipadi,
Ndinam’kana kalelo;
Koma Yesu waiwala,
Mphulupulu zangazo.

Wapumitsa mtima wanga,
Kaamba ndaphunziratu;
Mawu ake olembedwa,
Mukalata mwakemo.

Mumvetu abwenzi athu,
Musakanilire’yi;
Yesu ayitana inu,
Zalembedwa zomwezi.

Post navigation

Previous: Hymn 239 TILI ndi mtendere
Next: Hymn 241 MTENDERE uli m’mtima mwathumu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 130 Tidzakondweradi m’Mwambamo
  • Hymn 1799 Mulungu atipatsa mphamvu
  • Hymn 679 Zipata zachitsulo zitseguke zonse mbee!
  • Hymn 385 Tsopano, poyamba paja,
  • Hymn 1443 Ambuye Yesu anatsira
  • Hymn 1308 Ndi ine, m’mtima Mwanu mbee!
  • Hymn 1593 Wina atikonda ife,
  • Hymn 1380 Tilemekezetu
  • Hymn 1119 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 303 MEMA nkhondoyo, wadza mdaniyo,
  • Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,
  • Hymn 124 PAMTANDAPO, pamtanda,
  • Hymn 46 O! ufulu tigwirizane
  • Hymn 490 YESU adza kuwerenga,
  • Hymn 355 Tinafuna m’phirimo,
  • Hymn 168 NDINGANENE malilime,
  • Hymn 195 Bwinoli tipita,
  • Hymn 1193 Tsopano Mulungu
  • Hymn 314 E, moto wanu woyera
  • Hymn 1238 M’mene ndifa inedi,
  • Hymn 67 PAMENEPO pokhala madzulo,
  • Hymn 1066 Uchimo unapachikidwa pomwe
  • Hymn 428 MBUYE mtsitsimutse
  • Hymn 1806 Nowayo anatuma,
  • Hymn 257 Ndinasiya amayi,
  • Hymn 1127 Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja;
  • Hymn 405 POLENGA dzikoli
  • Hymn 162 PENYETSETSA Yesu,
  • Hymn 391 Mufafanize m’bukumo
  • Hymn 952 Ndimayenda paulendo,
  • Hymn 95 TAMANI mphamvu ya Yesu,
  • Hymn 1748 Ambuye tsopano lino,
  • Hymn 407 Zochimwa sizilowako,
  • Hymn 1794 Mulungu awakonda anthu
  • Hymn 235 Kumwamba ndikaimbanso
  • Hymn 1465 Akulu inu m’bwere nonse,
  • Hymn 187 UFUNA kuwomboledwa kodi?
  • Hymn 147 MUSAŴALOLE mawuwo
  • Hymn 1740 Yesu, ndi chifundo chanu
  • Hymn 297 Anapita nasiya
  • Hymn 737 Mommuno, Mbuye, tionanetu,
  • Hymn 82 Mlendo wa Kumwambayo
  • Hymn 542 Kuli kaphiri m’talimo
  • Hymn 386 Tiyamike Mlunguyo,
  • Hymn 171 M’manda munalibe
  • Hymn 1082 Ndidzaonana nanu
  • Hymn 203 NTHAWI yathadi bwerera mbale,
  • Hymn 470 YESU andikonda ine,
  • Hymn 810 Tsopano lino kwada bii,
  • Hymn 1472 Ona! Ona! Onatu!
  • Hymn 1095 Mumtima wakufatsa
  • Hymn 834 Tiyamike Mlungu wotipatsa zachifundozi,
  • Hymn 1290 Ndilibe malo mokhaliramo,
  • Hymn 427 Komwe ndi chimwemwe
  • Hymn 7 NDI Aleluya imbirani,
  • Hymn 6 Nanu akukuzani amithenga,
  • Hymn 130 PHWANDO la Belisazara,
  • Hymn 182 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 157 INU nonse ovutidwa,
  • Hymn 1522 Tikaona bvuto,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version