Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 213 INE ndili ndi manyazi

  1. Home   »  
  2. Hymn 213 INE ndili ndi manyazi

Hymn 213 INE ndili ndi manyazi

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 213 INE ndili ndi manyazi

 

INE ndili ndi manyazi
Kuti kale lomwelo
Ndinanyoza kudza komwe
Kwa Mtetezi wanga Yesu,
Ndati, Sindimfuna `yi.

Koma Iye wandipeza;
Ndamuona m`mtandamo,
Mwa kufera ine momwe;
Ndipo ndati m`mtima mwanga:
Mbuye, ndikufunani.

Nsiku zonse kwanja kwake
Kunandithandizatu,
Kunandichiritsa mtima;
Ndipo ndati: Mpulumutsi,
Ndinu Mbuye wangatu.

Sindifuna Mbuye wina,
Koma Yesu yekhayo;
Ine ndili munthu wake,
Iye anandigonjetsa
Ndi kukonda kwakeko.

Post navigation

Previous: Hymn 212 NDI MISOZI, ndi chisoni,
Next: Hymn 214 KUNALI munthu ku Yeriko,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 308 Ifetu kuchimwa, Mbuye,
  • Hymn 617 Nthawi yina Mbuyeyu
  • Hymn 582 A! Mulungu,
  • Hymn 1276 Ndikhulupirira, Yesu, Inu nokhadi
  • Hymn 231 Mwazi wa Yesu wokondwa
  • Hymn 42 Masiku tikatsala ife
  • Hymn 333 M’DZIKO lino tikhalamo
  • Hymn 403 NDIYIMBA ndi chimwemwe lero,
  • Hymn 939 Ambuye andisunga
  • Hymn 164 Yendani, Mfumu yamtendere
  • Hymn 943 Onse aliko takonda kalelo,
  • Hymn 1525 Mbuye, mtiphunzitse
  • Hymn 1652 Mabala ajawo
  • Hymn 69 KONDWERANI dzuŵa lino,
  • Hymn 910 Nlokoma Dziko langa!
  • Hymn 1857 Ndinagona mwa zoipa,
  • Hymn 665 Pomangidwa anthu nayo
  • Hymn 981 Tiyeni Akristu,
  • Hymn 519 Mverani, aimba anawo,
  • Hymn 488 Ndikabwera, Mbuye
  • Hymn 348 Aitana,
  • Hymn 1684 Mbuye mabala anu olimba
  • Hymn 964 Kodi simuona njira,
  • Hymn 1657 Mbuye, mutsaganebe
  • Hymn 1696 Mndiletse, ndisateme ‘yi
  • Hymn 37 YESU analikhanda
  • Hymn 498 Yesu akonda,
  • Hymn 1785 Tiyeni tizipita kwathu,
  • Hymn 1259 Ndikhulupirira bwino
  • Hymn 179 Ndinachimwa poganiza
  • Hymn 238 MULUNGU wanga,
  • Hymn 425 Ine ndine mlendo
  • Hymn 1623 Adzatenga anthu ake
  • Hymn 608 Maluwa abwino aphuka m’mapiri ndi m’madambomo,
  • Hymn 1783 Tinasokera ngati nkhosa,
  • Hymn 380 ATATE, muwapenya
  • Hymn 1746 Mwachimwemwe, mwachisoni,
  • Hymn 660 Tumizani kuunikako,
  • Hymn 91 NDITAME Mlungu m’mtimamo,
  • Hymn 1853 Etu ine, etu ine,
  • Hymn 354 Tinafunafunatu,
  • Hymn 1102 Dziko lonse ndilitaya;
  • Hymn 1262 Lero mtima ungolema, Usaukadi;
  • Hymn 395 AMBUYE, Mwini zonsezi,
  • Hymn 1132 Mlungu adzandilandila,
  • Hymn 80 KUDZA kwa Mbuye
  • Hymn 936 Ukatha moyo wanga
  • Hymn 1363 Tamani Ambuye,
  • Hymn 34 Yesu Mbuyetu, mwafera
  • Hymn 1817 Ndi m’munda muja chete, phee!
  • Hymn 679 Zipata zachitsulo zitseguke zonse mbee!
  • Hymn 557 Usikuwo woyerawo!
  • Hymn 1556 Mzimu Woyera, mudzetu kwa ine,
  • Hymn 190 Nsiku zonse kwanja kwake
  • Hymn 809 Madzulo aja kalelo
  • Hymn 918 Ntchito yonse yakeyo
  • Hymn 1777 Mulungu wamkulu
  • Hymn 1357 Mlemekeze, anakonda
  • Hymn 630 Ena atsagana nafe
  • Hymn 1662 Msandipitire, Yesu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version