Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 213 INE ndili ndi manyazi

  1. Home   »  
  2. Hymn 213 INE ndili ndi manyazi

Hymn 213 INE ndili ndi manyazi

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 213 INE ndili ndi manyazi

 

INE ndili ndi manyazi
Kuti kale lomwelo
Ndinanyoza kudza komwe
Kwa Mtetezi wanga Yesu,
Ndati, Sindimfuna `yi.

Koma Iye wandipeza;
Ndamuona m`mtandamo,
Mwa kufera ine momwe;
Ndipo ndati m`mtima mwanga:
Mbuye, ndikufunani.

Nsiku zonse kwanja kwake
Kunandithandizatu,
Kunandichiritsa mtima;
Ndipo ndati: Mpulumutsi,
Ndinu Mbuye wangatu.

Sindifuna Mbuye wina,
Koma Yesu yekhayo;
Ine ndili munthu wake,
Iye anandigonjetsa
Ndi kukonda kwakeko.

Post navigation

Previous: Hymn 200 YESU mundimve, ndikuliratu,
Next: Hymn 221 A! CHIKONDI chopambana,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 810 Tsopano lino kwada bii,
  • Hymn 1053 Mtimatu wopirira ndi
  • Hymn 783 Antchito a Mulungu ‘nu
  • Hymn 116 MBUYE, Mawu anu
  • Hymn 934 Mnamwalira Inu paja,
  • Hymn 1671 Akhululukira iwe,
  • Hymn 447 OYAMIKA Mlungu m’bwere,
  • Hymn 395 Usiku uno mutisungedi,
  • Hymn 1198 Mabala ake m’manja
  • Hymn 373 Ayamikire ‘Nu
  • Hymn 493 DZUŴA li
  • Hymn 734 Ndi mkate wanu, Yesu
  • Hymn 1242 Ku zoipa zonse zako,
  • Hymn 8 MITAMBO inu yakumwambako
  • Hymn 1332 Imba kawiri ndi kawirinso,
  • Hymn 1625 Ife tonse tikumbuke
  • Hymn 1813 Pochimwa anthu onsewo
  • Hymn 1590 Mtima ndimakondweramo,
  • Hymn 1648 Uko Kumwambako Mbuyangayo
  • Hymn 1055 E, mtima watsopano ndi
  • Hymn 127 POLUMIDWA ndi njokazo,
  • Hymn 225 NDIDZAIMBA za Mulungu,
  • Hymn 1477 Anena anthu onsewo,
  • Hymn 1428 Penyetsetsa Yesu
  • Hymn 1823 Opani Iye, nimuleke
  • Hymn 457 Palibe mwana wakuchepa
  • Hymn 115 NTHAWI ija ya Sauli,
  • Hymn 1455 Uthenga wa Mulungu
  • Hymn 1586 Mbuye Yesu timtamanda
  • Hymn 478 YESU atiuza tiŵale ’fe.
  • Hymn 148 PAKUPEMPHA ife pano,
  • Hymn 1123 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 1257 Mtanda m’mtima ndiyang’na,
  • Hymn 283 AMBUYE m’chipululu,
  • Hymn 428 MBUYE mtsitsimutse
  • Hymn 1476 Mipingo iyo idzatu,
  • Hymn 1528 Naye Mzimu mndiphunzitse
  • Hymn 1635 Pakwitana Mbuye wanga,
  • Hymn 768 Ndi ife tinga mbewuzo
  • Hymn 1292 Wolapa mtima simunyozadi,
  • Hymn 186 MVERANI mbiri yozizwitsa
  • Hymn 1597 Timchimwira kopambana,
  • Hymn 1249 Tsirizani ntchito yanu
  • Hymn 311 VALANI zida tizinka kwathuko,
  • Hymn 303 Ona pamtanda Yesuyo
  • Hymn 342 Ambiri,
  • Hymn 1458 Satana ndi unyolo
  • Hymn 1462 Dzina la Yesu ndi lokoma,
  • Hymn 29 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 1246 Ambuyanga, ndalephera,
  • Hymn 1468 Zobvala zake zonse
  • Hymn 653 Nditsogolere m’njirayi
  • Hymn 1377 Ndi amithenga akumwambako,
  • Hymn 1149 Chete! Chete!
  • Hymn 361 Munka kangati kulawa
  • Hymn 753 Getsemane ndionako
  • Hymn 1618 Anakwera,
  • Hymn 42 Masiku tikatsala ife
  • Hymn 1008 Wakuchezacheza naye
  • Hymn 798 M’nyumba yanu, Mlungu, ‘yi

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version