Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 147 MUSAŴALOLE mawuwo

  1. Home   »  
  2. Hymn 147 MUSAŴALOLE mawuwo

Hymn 147 MUSAŴALOLE mawuwo

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 147 MUSAŴALOLE mawuwo

 

MUSAŴALOLE mawuwo
Apite ngati mphepozi,
Musaumitse mtimatu,
Polira Yesu Mbuyedi.

Idzanitu, idzanitu,
Idzani kwa Ambuyeyo.
Idzanitu, idzanitu
Apulumutse inunso.

Musachitenso nthantha ’yi,
Mufulumire inutu;
Tsiku labwino nleroli,
Mulandirenso moyowu.

Zokondweretsa m’dzikomu
Nzosakhutitsa m’mtimamu,
Koma za Yesu zonsezo
Zikwaniritsa inudi.

Sakukanani Yesudi,
E, mukalapa m’mtimamo;
Lolani kuti Mzimuyo
Agwire ntchito zakezo.

Post navigation

Previous: Hymn 146 KODI ulikulemedwa
Next: Hymn 148 PAKUPEMPHA ife pano,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 51 Mbuye dalitsani Afrika,
  • Hymn 384 USIKU uja kalero,
  • Hymn 1072 Mudzaze Yesu mtima wanga ndi chikondicho,
  • Hymn 101 MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,
  • Hymn 707 Dalitseni, Mbuye, zonse
  • Hymn 321 PAKUONA imfayo
  • Hymn 697 Zolengedwa zonse zidze
  • Hymn 220 Kalekale ndinathawa,
  • Hymn 260 Angelo aitana,
  • Hymn 857 Mlungu amaunikira
  • Hymn 271 Pomwalira Mbuyeyo
  • Hymn 964 Kodi simuona njira,
  • Hymn 1623 Adzatenga anthu ake
  • Hymn 1016 Mbuye, mwatiuza ‘fe
  • Hymn 1117 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 5 Inu Mulungu, tikuyamikani;
  • Hymn 1718 Ona chikondi cha Mulungu,
  • Hymn 1174 Sindinanyengedwa konse;
  • Hymn 138 Kumva ulikumva, ulikumva,
  • Hymn 151 UKAPENYA kwa Yesu uliko moyoko,
  • Hymn 257 NJIRA yanga sindiziŵa,
  • Hymn 30 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 1586 Mbuye Yesu timtamanda
  • Hymn 1408 Kodi mwalandira Yesu?
  • Hymn 1005 Mdani adza nazo mphamvu,
  • Hymn 44 NTHAWIYO anam’gwira Yesu,
  • Hymn 247 MULUNGU anditsogolera,
  • Hymn 1843 Chigwa choopsacho cha imfa ndikachilowera,
  • Hymn 263 AMBUYE mundisunge
  • Hymn 1856 Mzimu, msandipitirire,
  • Hymn 891 Akakusowa malo
  • Hymn 282 Ine ndili munthu
  • Hymn 420 Mtima umabisala
  • Hymn 174 Haya, anzathu, itilinda nkhondo;
  • Hymn 802 Ndife anthu aulendo,
  • Hymn 1346 Ndaima pano, ndaima pakhomo:Lowa, lowa, lowa, lowa!
  • Hymn 968 Mzimu wakuipa
  • Hymn 102 MZIMU Woyera, mudzetu kwa ine
  • Hymn 1168 Aleluya, muyenera!
  • Hymn 477 YESU, muli pa chimpando
  • Hymn 1681 Mphamvu za imfa ndi za Satana
  • Hymn 462 Pothandiza amathu,
  • Hymn 168 NDINGANENE malilime,
  • Hymn 1849 Nthawi zonse monga ‘Tate
  • Hymn 24 TITAME Mlungu Wakumwamba,
  • Hymn 245 Ngakhale kuthengo
  • Hymn 1541 Tionetseni tonsetu
  • Hymn 498 Yesu akonda,
  • Hymn 1575 Tifuna kuti komweko
  • Hymn 463 MNANDIDZERA, Ambuye,
  • Hymn 1476 Mipingo iyo idzatu,
  • Hymn 1328 Ndani afuna kunkako
  • Hymn 1824 Mulungu wathu Mmodzi yekha
  • Hymn 656 Ndipumulire panupo,
  • Hymn 160 MADALITSO ngati mvumbi,
  • Hymn 446 Yesu alandira
  • Hymn 345 Ubwere,
  • Hymn 149 Ndisauka, sindikhoza
  • Hymn 454 Kapena m’mtima ndimakwiya,
  • Hymn 361 Munka kangati kulawa

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version