Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 147 MUSAŴALOLE mawuwo

  1. Home   »  
  2. Hymn 147 MUSAŴALOLE mawuwo

Hymn 147 MUSAŴALOLE mawuwo

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 147 MUSAŴALOLE mawuwo

 

MUSAŴALOLE mawuwo
Apite ngati mphepozi,
Musaumitse mtimatu,
Polira Yesu Mbuyedi.

Idzanitu, idzanitu,
Idzani kwa Ambuyeyo.
Idzanitu, idzanitu
Apulumutse inunso.

Musachitenso nthantha ’yi,
Mufulumire inutu;
Tsiku labwino nleroli,
Mulandirenso moyowu.

Zokondweretsa m’dzikomu
Nzosakhutitsa m’mtimamu,
Koma za Yesu zonsezo
Zikwaniritsa inudi.

Sakukanani Yesudi,
E, mukalapa m’mtimamo;
Lolani kuti Mzimuyo
Agwire ntchito zakezo.

Post navigation

Previous: Hymn 140 NDINAMIRA m’machimo, wosaonekanso,
Next: Hymn 161 LERO lino mbale wanga,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1566 Mufike monga ngati mphepo yokokomayo,
  • Hymn 1553 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 585 Alanditsa,
  • Hymn 880 Bwenzi lathu ndiye Yesu
  • Hymn 33 OWONADI mtima,
  • Hymn 1855 Yesu, msandipitirire
  • Hymn 1419 Amayi ‘nu, amayi ‘nu,
  • Hymn 1656 Inu mundibisadi
  • Hymn 255 Pakuona imfayo
  • Hymn 144 Yesu, ndipemphera
  • Hymn 538 Iye anachoka kwawo,
  • Hymn 123 Koma mudzisungire chuma cha Kumwamba
  • Hymn 309 Mwa Mzimu mulowe mumitima yathu,
  • Hymn 1408 Kodi mwalandira Yesu?
  • Hymn 432 KRISTU ndiye Mwala wathu,
  • Hymn 379 Anditsogolera m’njira
  • Hymn 875 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 356 YESU Mbuye onani,
  • Hymn 365 DZUŴA lapita,
  • Hymn 463 Yesu atiuza tiwale ‘fe,
  • Hymn 111 YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;
  • Hymn 1165 Dzanja la Mulungu
  • Hymn 976 Muyendenso kunka komwe,
  • Hymn 140 Panalitu wakudwala
  • Hymn 300 AKRISTU limbikani,
  • Hymn 684 Zipata zatsegudwa mbee! Za m’dziko monsemo;
  • Hymn 1444 Wamoyo ndiye Yesudi,
  • Hymn 1592 Tsono mubwere inunso,
  • Hymn 1556 Mzimu Woyera, mudzetu kwa ine,
  • Hymn 1249 Tsirizani ntchito yanu
  • Hymn 21 Mbuye mtsitsimutse!
  • Hymn 1844 Pamaso pa adaniwo mwayala gome langa;
  • Hymn 1295 Ambuye, mwazi wanuwo
  • Hymn 112 Pangano lake m’mwaziwo
  • Hymn 460 E! ang’ono ndifetu,
  • Hymn 1582 Konda dzinalo la Yesu
  • Hymn 1830 Ndiye M’busa wanga
  • Hymn 839 Adani sindiopa mukalipo;
  • Hymn 1128 Mbuyanga Yesu, mundisunge ine
  • Hymn 388 Ambuye, Mzimu wanu
  • Hymn 1267 Kwa Inu Yesu ndilira,
  • Hymn 419 ANYAMATA a Mulungu,
  • Hymn 75 Ndiperekatu
  • Hymn 518 Ana a Yerusalemu
  • Hymn 303 Ona pamtanda Yesuyo
  • Hymn 349 MOSE anamenya thanthwe kawiri,
  • Hymn 327 Yesu salephera ‘yi.
  • Hymn 630 Ena atsagana nafe
  • Hymn 552 Analira ndaniyo
  • Hymn 195 Bwinoli tipita,
  • Hymn 170 M’manda naukamo
  • Hymn 715 Mwapatsa Mwana wanu, ndi
  • Hymn 1836 Ndi wamwayi munthu uja
  • Hymn 664 Komwe asauka anthu
  • Hymn 573 Ambuye, tikutamandani
  • Hymn 946 Ngakhale enawo aleke kwimbako,
  • Hymn 435 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 266 MBUYE ndamva mwawazira
  • Hymn 1477 Anena anthu onsewo,
  • Hymn 98 Ndidzamwona maso ndi maso

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version