Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,

  1. Home   »  
  2. Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,

Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,

 

MKAZI wa ku Samariya,
Napita kukatunga madzi;
Pofika iyetu komweko,
Anapeza Ambuye Yesu.

Ambuye ananena:
“Ndipatseni madzi Ndimweko;
Ukanadziwa mtulo wa Mulunguyo,
Sukanandimana madzi.”

Ambuye nanena naye:
“Kayitane mwamuna wako;”
Mkazi anamuyankha nati:
“Inetu ndilibe mwamuna.”

Mkazi pochoka pomwepo,
Natsimikizatu mumtima;
Nati: “Uyu ndiye Mesiya,
Ndi Mwana wa Mulunguyotu.”

Abale tikhulupi’re,
Kuti Ambuye Yesuyo;
Ndiye Mwanadi wa Mulungu,
Ndiponso ndi Mpulumutsiyo.

Post navigation

Previous: Hymn 135 USANABADWE, Yeremiya,
Next: Hymn 137 UTHENGA wa Ambuye

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1622 Anthu onse amlambire
  • Hymn 932 Munabvala thupi lathu,
  • Hymn 1270 Ndayesa kudzikonzadi,
  • Hymn 1603 Zina za Yesu m;Mwambamo,
  • Hymn 1784 Komweko titasaukira,
  • Hymn 414 INU bambo, inu mayi,
  • Hymn 1366 Sititha ifedi
  • Hymn 257 NJIRA yanga sindiziŵa,
  • Hymn 1504 Kodi ali ndi chilemba
  • Hymn 1001 Mafumu atiuza tikaletse ukapolo,
  • Hymn 1168 Aleluya, muyenera!
  • Hymn 352 NONSE okhala pansipa,
  • Hymn 1353 Ambuye Yesu, Inutu
  • Hymn 1456 Pakuti anthu akumvera
  • Hymn 403 Dzuwa liwala, m’tulotu
  • Hymn 25 “Akaleka amake
  • Hymn 692 Paulendo wathu
  • Hymn 1169 Mwazi wa Yesu
  • Hymn 828 Ndidzukanso m’mawa,
  • Hymn 239 TILI ndi mtendere
  • Hymn 1728 Zofuna zanga zonsezo
  • Hymn 94 KHAMULO liliko
  • Hymn 437 MULUNGU wa Yakobo Inu, mdyetsa anthu anu,
  • Hymn 1568 Kudzoza kwanu kutipatsa
  • Hymn 1019 Tsata, tsata, nditsatadi Yesu;
  • Hymn 479 Munanena mulandira
  • Hymn 1149 Chete! Chete!
  • Hymn 591 Yesu Mwanatu
  • Hymn 507 Yesu ndimkonda, akondanso ine,
  • Hymn 1755 Choti timtumikire
  • Hymn 39 MUNASIYATU dziko lanulo,
  • Hymn 1683 Nsinga za imfa Iye ‘nadula,
  • Hymn 1584 Konda dzinalo la Yesu
  • Hymn 1499 Simbanitu mwachete
  • Hymn 1331 Yesu wathu Mbuyeyo
  • Hymn 68 Kwathu ndidzaimba nyimbo
  • Hymn 1248 ‘Dzanitu Wamphamvu yonse,
  • Hymn 42 Masiku tikatsala ife
  • Hymn 412 Kudzachera tsiku lijalo
  • Hymn 185 NDINE Mbusayo wabwino,
  • Hymn 1663 Yesu Mbuye,
  • Hymn 265 Imbirira moyo wanga,
  • Hymn 24 “Ndakupeza womanga,
  • Hymn 922 Onse akulapawo
  • Hymn 1089 Ndionetsere kuunika
  • Hymn 1513 M’Bukuli ine ndi
  • Hymn 1842 Pabande lolunjika andilondolera njira;
  • Hymn 1244 Nthawi ilikudza yonse
  • Hymn 378 KWEZANI mitu yanuyo,
  • Hymn 623 Mbuye, tikuthokozani,
  • Hymn 314 E, moto wanu woyera
  • Hymn 375 YESU m’khale nafe
  • Hymn 185 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 266 MBUYE ndamva mwawazira
  • Hymn 1497 Simbani mobwereza,
  • Hymn 583 Anabadwa,
  • Hymn 238 MULUNGU wanga,
  • Hymn 211 TIDZALAKALAKA kuwonana naye,
  • Hymn 1004 A! mizimu yakuipa
  • Hymn 1170 Pamtanda wake

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version