Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,

  1. Home   »  
  2. Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,

Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,

 

MKAZI wa ku Samariya,
Napita kukatunga madzi;
Pofika iyetu komweko,
Anapeza Ambuye Yesu.

Ambuye ananena:
“Ndipatseni madzi Ndimweko;
Ukanadziwa mtulo wa Mulunguyo,
Sukanandimana madzi.”

Ambuye nanena naye:
“Kayitane mwamuna wako;”
Mkazi anamuyankha nati:
“Inetu ndilibe mwamuna.”

Mkazi pochoka pomwepo,
Natsimikizatu mumtima;
Nati: “Uyu ndiye Mesiya,
Ndi Mwana wa Mulunguyotu.”

Abale tikhulupi’re,
Kuti Ambuye Yesuyo;
Ndiye Mwanadi wa Mulungu,
Ndiponso ndi Mpulumutsiyo.

Post navigation

Previous: Hymn 120 MUNDINYEMERE ’ne
Next: Hymn 141 TAONANI pamtandapo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 894 Mbuye, ndinu Mfumu yanga
  • Hymn 1130 Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja
  • Hymn 171 IWE tiye, iwe tiye,
  • Hymn 549 Ndiye Mbuye, Mfumu yanga,
  • Hymn 336 Perekani mtima wanu
  • Hymn 1492 Sakukanani Yesudi,
  • Hymn 1355 Atate, Mwana, Mzimunso,
  • Hymn 79 Mlendo ali pakhomo,
  • Hymn 910 Nlokoma Dziko langa!
  • Hymn 1383 Dzina lake tibukitsa,
  • Hymn 1479 Ndi Yesu yemwe kalelo
  • Hymn 714 Dzuwa ndi mvula yonseyo
  • Hymn 1093 Odala ndi onsewo
  • Hymn 1519 M’Buku lakuyerali
  • Hymn 315 YENDANI munjira yake,
  • Hymn 162 PENYETSETSA Yesu,
  • Hymn 122 Musadziunjikire chuma cha padziko,
  • Hymn 995 Taya zako zochenjera,
  • Hymn 1146 Khalani duu! Pakufa mnzathuyo,
  • Hymn 1677 Zomkweza zili m’Mwamba,Aleluya
  • Hymn 1790 Imfa ya anthu ake imkomera,
  • Hymn 1657 Mbuye, mutsaganebe
  • Hymn 291 ULENDO wachikhrisitu ngosawutsa ndithu,
  • Hymn 628 E! chisomo chosaleka
  • Hymn 951 Ndi kale lonse mnandisunga ‘ne;
  • Hymn 374 Pakuti Mfumuyo
  • Hymn 1358 Lemekeza Mfumu yathu,
  • Hymn 905 Iwo asekera, iwo asekera,
  • Hymn 145 MBIRI yakale lomwe
  • Hymn 446 YAMIKANI nonse ’nu,
  • Hymn 498 AMBUYE, mtidalitsetu,
  • Hymn 980 Tiyeni ku nkhondo iyi,
  • Hymn 1726 Linadetsedwa dzuwa bii!
  • Hymn 248 M’MENE ine ndisauka
  • Hymn 1532 Mubwere kuno Mzimu ‘Nu,
  • Hymn 1785 Tiyeni tizipita kwathu,
  • Hymn 964 Kodi simuona njira,
  • Hymn 212 Onse am’Mwamba ali mowemo,
  • Hymn 163 MALO anachepa,
  • Hymn 1746 Mwachimwemwe, mwachisoni,
  • Hymn 285 Ndipempha, Ambuye,
  • Hymn 1056 Mkhalidwe wanu mundipatse,
  • Hymn 297 Anapita nasiya
  • Hymn 13 Mtiwerengere m’Mwamba ndi oyera;
  • Hymn 1099 Sindidziwatu zamawa,
  • Hymn 358 Dzina lake Yesuyo,
  • Hymn 216 Ndi misozi ndi chisoni
  • Hymn 832 Zochimwa za usana uno mndikhululukire ‘ne;
  • Hymn 82 YANG’ANANI, anthu onse,
  • Hymn 283 Ndalema ndathodwa
  • Hymn 474 Yesu ndafikatu,
  • Hymn 606 Dzinja lokondweretsa lafikanso,litapumatu,
  • Hymn 374 NDI lokoma m’Mwambamo,
  • Hymn 1164 Tikakhulupira
  • Hymn 1275 Mtima ‘we siya ndi Yesu nsonizi,
  • Hymn 1632 Ndi chiyembekezo ichi
  • Hymn 842 Tipempha kuti Mpingo wanu
  • Hymn 1450 Ndi angelo akumwamba
  • Hymn 579 Pochezera m’dambomo,
  • Hymn 67 Chisomo chandisungadi

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version