Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 102 MZIMU Woyera, mudzetu kwa ine

  1. Home   »  
  2. Hymn 102 MZIMU Woyera, mudzetu kwa ine

Hymn 102 MZIMU Woyera, mudzetu kwa ine

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 102 MZIMU Woyera, mudzetu kwa ine

 

MZIMU Woyera, mudzetu kwa ine
E, ngati mvula m’dziko lakuuma,
Ndikhale munda wanu wakupatsa
Zipatso zoyenera Mbuyeyo.

Mphunzitsi, ndinu mudziŵitse ine
Chikondi chanu chija chachikulu;
Lembani mawu anu pamtimanga,
Kuti ndikhumbukire zanuzo.

Wosangalatsa, ine ndikalira
Muchotse nsoni, m’mtimamo mudikhe;
Mundigoneke pachifuwa chake
Cha Yesu kuti ndikakondwepo.

Wotsogolera, munditsogolere
Kuti n’kafike kwawo kwa Atate,
Nditsate Yesu ndikuyendayenda
M’njira yomweyo anapondamo.

Mthandizi ndinu, mndithangate ine
Kupempha bwino izo zindisoŵa.
Kupempha monga Mlungu amafuna
Kulingalira zake zokhazo.

Mzimu Woyera, n’dzipereke ndense,
Mundichitire ntchito yaikulu;
Mtima woyera ndi womvera mpatse,
Wodzala ndi chikondi chanucho.

Post navigation

Previous: Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,
Next: Hymn 121 MULUNGU, anthu ’fe

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 301 MBUYE, ndapangana
  • Hymn 223 ATI Yesu Mbuyeyo:
  • Hymn 115 NTHAWI ija ya Sauli,
  • Hymn 1035 Mphamvu zathu zonse
  • Hymn 953 Ichi chindisangalatsa
  • Hymn 995 Taya zako zochenjera,
  • Hymn 110 Ndaima nji pa Kristuyo,
  • Hymn 1283 Yesu ndikhulupirira
  • Hymn 990 Poyesedwa ine
  • Hymn 1785 Tiyeni tizipita kwathu,
  • Hymn 699 Inu wakudzatu
  • Hymn 1681 Mphamvu za imfa ndi za Satana
  • Hymn 17 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 1828 Timtamande Iye ndi moyo wathunso
  • Hymn 738 Mommuno, Mbuye, mkate wanuwu,
  • Hymn 236 NDIDZIWITSITSA
  • Hymn 276 MKRISTU, ulimbike
  • Hymn 1088 Mndiyandikitse nanu, Yesu,
  • Hymn 334 KULI dziko labwino M’mwamba,
  • Hymn 517 “Osana m’Mwambamwamba!”
  • Hymn 1566 Mufike monga ngati mphepo yokokomayo,
  • Hymn 28 AMBUYE ngwodalitsika,
  • Hymn 638 Ndi Mzimutu Woyera
  • Hymn 1249 Tsirizani ntchito yanu
  • Hymn 127 POLUMIDWA ndi njokazo,
  • Hymn 1444 Wamoyo ndiye Yesudi,
  • Hymn 1757 Udzadziwitsa anthu
  • Hymn 1255 Chitha nchiani kund’yeretsa?
  • Hymn 662 Tisaleme pakuchita zabwinozi,
  • Hymn 764 “Chikho cha mwazi wangachi
  • Hymn 1620 Aleluya,
  • Hymn 1652 Mabala ajawo
  • Hymn 1139 Namondwe akawombabe,
  • Hymn 468 Ife tikondana nanu,
  • Hymn 349 MOSE anamenya thanthwe kawiri,
  • Hymn 744 Kristu ndi mwini moyo wathuwu,
  • Hymn 1851 Anthu onse, anthu onse,
  • Hymn 1426 Wina panalibe
  • Hymn 476 MBUYE, tili ana anu,
  • Hymn 132 MVERA mtima wanga ’we
  • Hymn 719 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 155 UTHENGA wa Mulungu
  • Hymn 1148 Ndiimba mumtima mokondwa
  • Hymn 392 Chimwemwe chomwe mpatseko
  • Hymn 1317 Ambuye naitana ‘ne:
  • Hymn 784 Mugwade pansi m’nyumbayo,
  • Hymn 544 Zoopsya sitidziwapo
  • Hymn 1454 Ambuye, musendeze
  • Hymn 850 Pemphero, pemphero,
  • Hymn 70 LAMBIRA, Mfumuyo,
  • Hymn 1448 Yesu ndiye Bwenzi lanu,
  • Hymn 218 Mbuye Yesu ndi Atate,
  • Hymn 409 ANTHU akum’maŵa
  • Hymn 1712 E! Yesu Mbuye wangadi,
  • Hymn 102 MZIMU Woyera, mudzetu kwa ine
  • Hymn 374 Pakuti Mfumuyo
  • Hymn 1848 Tiyamike Mlungu wathu
  • Hymn 206 YESU, mulikundipempha
  • Hymn 1508 Mundinyemere ‘ne
  • Hymn 520 Tamva tikondane naye,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version