Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 102 MZIMU Woyera, mudzetu kwa ine

  1. Home   »  
  2. Hymn 102 MZIMU Woyera, mudzetu kwa ine

Hymn 102 MZIMU Woyera, mudzetu kwa ine

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 102 MZIMU Woyera, mudzetu kwa ine

 

MZIMU Woyera, mudzetu kwa ine
E, ngati mvula m’dziko lakuuma,
Ndikhale munda wanu wakupatsa
Zipatso zoyenera Mbuyeyo.

Mphunzitsi, ndinu mudziŵitse ine
Chikondi chanu chija chachikulu;
Lembani mawu anu pamtimanga,
Kuti ndikhumbukire zanuzo.

Wosangalatsa, ine ndikalira
Muchotse nsoni, m’mtimamo mudikhe;
Mundigoneke pachifuwa chake
Cha Yesu kuti ndikakondwepo.

Wotsogolera, munditsogolere
Kuti n’kafike kwawo kwa Atate,
Nditsate Yesu ndikuyendayenda
M’njira yomweyo anapondamo.

Mthandizi ndinu, mndithangate ine
Kupempha bwino izo zindisoŵa.
Kupempha monga Mlungu amafuna
Kulingalira zake zokhazo.

Mzimu Woyera, n’dzipereke ndense,
Mundichitire ntchito yaikulu;
Mtima woyera ndi womvera mpatse,
Wodzala ndi chikondi chanucho.

Post navigation

Previous: Hymn 101 MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,
Next: Hymn 103 MPUME pa inetu, Mpweya wa Mulungu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1598 Mtiphunzitse, Mbuye Yesu,
  • Hymn 1706 Pamutu minga kwe!
  • Hymn 1542 Titamire nthawi zonse
  • Hymn 457 Palibe mwana wakuchepa
  • Hymn 1058 Chimwemwe chija chamumtima
  • Hymn 1558 Wosangalatsa, ine ndikalira
  • Hymn 27 LEMEKEZANI Yehova,
  • Hymn 112 ELISA mneneri,
  • Hymn 685 Tamva mawu amwewo
  • Hymn 87 IDZANI nonse ’nu
  • Hymn 1636 Potuluka m’manda mwawo
  • Hymn 1188 Akumangidwa ndi mzimuwo,
  • Hymn 1137 Masiku ena pali mdima,
  • Hymn 31 MULUNGU Wamkulu,
  • Hymn 155 Pemphero ndiko kufuna
  • Hymn 1776 Tiyeni timgwadire
  • Hymn 1718 Ona chikondi cha Mulungu,
  • Hymn 190 CHITETEZO chachikulu
  • Hymn 1852 Mbuye ndamva mwawazira
  • Hymn 1190 Aleluya, mlemekeze,
  • Hymn 1557 M’phunzitsi, ndinu mudziwitse ine
  • Hymn 1727 Pokumbukira mtandawo
  • Hymn 840 Ambuye munapatsa tsiku
  • Hymn 1421 Alongo ‘nu, alongo ‘nu,
  • Hymn 995 Taya zako zochenjera,
  • Hymn 512 ‘Natipulumutsa
  • Hymn 1689 Dzukani nayetu,
  • Hymn 11 Imfa mutagonjetsa ndi zowawa,
  • Hymn 203 NTHAWI yathadi bwerera mbale,
  • Hymn 1318 Ndibwera kwa Ambuyeyo,
  • Hymn 1328 Ndani afuna kunkako
  • Hymn 709 Munthu aganize
  • Hymn 1437 Yesu ndi wokonda;
  • Hymn 1823 Opani Iye, nimuleke
  • Hymn 1666 Yesu, ndinutu chitsime
  • Hymn 918 Ntchito yonse yakeyo
  • Hymn 561 Uyu ‘natsikira kuno,
  • Hymn 987 Ambuye wa Kumwamba,
  • Hymn 718 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 1489 Idzanitu, idzanitu,
  • Hymn 207 Malo alimo m’nyumba ya Yesu,
  • Hymn 164 Yendani, Mfumu yamtendere
  • Hymn 701 Inu Atatuwo,
  • Hymn 921 Komwe Mbusa kwawoko
  • Hymn 1048 Kumwamba ndiona Ambuyangayo,
  • Hymn 399 M’KHOLA mwa ng’ombe ku Betlehemu
  • Hymn 813 Wopulumutsa, Inunso
  • Hymn 103 MPUME pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 192 ZAKEYU mkulu wa misonkho,
  • Hymn 484 Mutiletse, Mbuye,
  • Hymn 554 Iye ndani pamtanda
  • Hymn 61 A! MUTU wakuyera,
  • Hymn 1835 Mtima wanga lemekeza
  • Hymn 760 Usiku uja kalelo
  • Hymn 1243 Kodi mayi wobereka
  • Hymn 201 Ngati zakuipa zathu
  • Hymn 110 Ndaima nji pa Kristuyo,
  • Hymn 162 PENYETSETSA Yesu,
  • Hymn 349 MOSE anamenya thanthwe kawiri,
  • Hymn 1374 Inu mumvere anyamatawo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version