Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 82 YANG’ANANI, anthu onse,

  1. Home   »  
  2. Hymn 82 YANG’ANANI, anthu onse,

Hymn 82 YANG’ANANI, anthu onse,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 82 YANG’ANANI, anthu onse,

 

YANG’ANANI, anthu onse,
Yesu Mbuye wathuyo:
Alinkudza ndi ulemu,
Kuoneka m’Mwambamo.

Anthu onse am’lambire
Yesu Mwana wa Mulungu
Alinkudza ndi ulemu
Wopambana, indetu.

Adzatenga anthu ake
Akumvera pansipo
Iwo adzakhala naye
M’dziko la Kumwambako.

Koma anthu onse omwe
Anamnyoza pansipo,
Nthaŵi Yesu alinkudza
Adzaopa m’mtimamo.

Ife tonse tikumbuke
Mawu ake onsewo;
Timuyang’anire Iye,
Yesu Mbuye wathuyo.

Post navigation

Previous: Hymn 80 KUDZA kwa Mbuye
Next: Hymn 101 MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 347 Mfumu iyi,
  • Hymn 46 INALIPO nthawi,
  • Hymn 246 Pajapo ndipenya
  • Hymn 55 Ambiri tikondwera mwa Yesu,
  • Hymn 962 Inde Mbuye, tibweradi,
  • Hymn 160 Kamwana kaja ‘nayamba
  • Hymn 793 Tikondwera kuti
  • Hymn 821 Aleluya!
  • Hymn 1161 Wapumitsa mtima wanga,
  • Hymn 1221 Bwenzi ndinamkomanayo,
  • Hymn 460 E! ang’ono ndifetu,
  • Hymn 1197 Ndafoka ine kale,
  • Hymn 1287 Wadza Yesu wandidzoza,
  • Hymn 1487 Bvumbulutsa zonse zako
  • Hymn 714 Dzuwa ndi mvula yonseyo
  • Hymn 174 YESU wathu Mbuyeyo
  • Hymn 812 Ndi ena sanamvera ‘yi,
  • Hymn 1370 Mphepo yay’kulu yakuombayo,
  • Hymn 193 A! Kumwamba
  • Hymn 1484 Idzatu, idzatu
  • Hymn 1482 Tsopano inu ‘dzanitu,
  • Hymn 364 DZUŴA lapitira,
  • Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,
  • Hymn 1022 Mbuye, nditsate bwanjiko?
  • Hymn 1770 Iye amazichita zamphamvu
  • Hymn 37 Pozunzidwa inu ponseponsepo
  • Hymn 597 Mlungu ali nane
  • Hymn 119 M’BUKU la moyotu Mbuye,
  • Hymn 292 Ndi makutu athu awanso nganu,
  • Hymn 57 TIYENI, dzalireni nane,
  • Hymn 320 Ambuye, wakuti ndi mwaziwo
  • Hymn 1274 Chisoni andichotsera Mbuyeyu,
  • Hymn 70 Mbuye ndinu bwenzi langa ndithu,
  • Hymn 274 E! tidzakomanansotu
  • Hymn 206 Uzanitu abale,
  • Hymn 328 Yesu ndiye mphamvu yanga,
  • Hymn 29 CHIKONDI cha
  • Hymn 1817 Ndi m’munda muja chete, phee!
  • Hymn 106 Ife, tapulumukadi,
  • Hymn 851 E, nthawi ya mamawayi
  • Hymn 101 MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,
  • Hymn 837 Koma kalelo mnakhalitsa pano,
  • Hymn 101 Lodala tsiku lomwelo
  • Hymn 196 Tidzimba komweko nyimbo
  • Hymn 983 Nkhondo ya Satana
  • Hymn 1251 Ndasokera m’tali ndithu
  • Hymn 967 Mbuye, ndapangana
  • Hymn 87 IDZANI nonse ’nu
  • Hymn 1081 Ndikabisala mwanu
  • Hymn 1499 Simbanitu mwachete
  • Hymn 1291 Njobvuta njira ndimayendamo,
  • Hymn 1819 Pokondwa ndi poona bvuto
  • Hymn 1292 Wolapa mtima simunyozadi,
  • Hymn 162 PENYETSETSA Yesu,
  • Hymn 757 Sindili woyenera ‘ne;
  • Hymn 463 Yesu atiuza tiwale ‘fe,
  • Hymn 1710 Pamtandapo, pamtandapo
  • Hymn 173 MWAMVA Mawu a Mulungu;
  • Hymn 709 Munthu aganize
  • Hymn 573 Ambuye, tikutamandani

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version