Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 51 PANTHAWI yakufa Ambuye,

  1. Home   »  
  2. Hymn 51 PANTHAWI yakufa Ambuye,

Hymn 51 PANTHAWI yakufa Ambuye,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 51 PANTHAWI yakufa Ambuye,

 

PANTHAWI yakufa Ambuye,
Anthu ananena:
“Dzipulumutsetu pamtandapo.”

(M) Yesu ndi mawu aakulu,
(O) Anafuula;
(M) Yesu ndi mawu aakulu,
(O)Anafuula;
“Eloyi, Eloyi
Mulungu wanga,
Mwandisiiranji,
Mwandisiiranji?”

Imfa ya Bwenzi lathu Yesu,
Yomvetsa chisoni;
Ophunzira onse anathaŵa.

Pamene anakhomedwatu,
Pamtanda Yesuyo;
Zoipa zathu zinam’psinja ‘Ye.

Imfa yake ndi yopambana,
Yotipulumutsa;
Yotitengera ife mtendere.

Post navigation

Previous: Hymn 40 KAMWANA Yesu ’nabadwa,
Next: Hymn 61 A! MUTU wakuyera,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 912 Makomo afanana
  • Hymn 1593 Wina atikonda ife,
  • Hymn 1596 Anamnyoza pansi pano,
  • Hymn 91 Ufuna kuyera kopambana?
  • Hymn 426 Mpulumutsi Yesu,
  • Hymn 958 Ndikalowa m’mtsinje muja,
  • Hymn 759 Ndilawako tsopanoli
  • Hymn 88 Yesu, dzina lakukonda,
  • Hymn 1255 Chitha nchiani kund’yeretsa?
  • Hymn 1376 Akulu nonse ndi mafumu ‘nu,
  • Hymn 914 Nlokoma Dziko langa!
  • Hymn 187 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 1599 Inde, ndifuna kumvatu
  • Hymn 1474 Zilepheradi zonse kugula moyowo,
  • Hymn 821 Aleluya!
  • Hymn 1682 Atha masiku aja ansoni,
  • Hymn 1622 Anthu onse amlambire
  • Hymn 1668 Kumdziwitsa ndiko moyo,
  • Hymn 1166 Masauko athu
  • Hymn 198 CHITSIMECHO cha mwaziwo
  • Hymn 1030 Tioperanji ifetu?
  • Hymn 1172 Adzabweranso
  • Hymn 468 NDIKONDWA kuti
  • Hymn 845 Ufumu wanu, Mbuye Yesu,
  • Hymn 901 Musatifikitsemo
  • Hymn 331 Yesu ndimafuna Inu,
  • Hymn 1686 Ndi mtima wonse mwimbedi
  • Hymn 138 Kumva ulikumva, ulikumva,
  • Hymn 386 Tiyamike Mlunguyo,
  • Hymn 1250 Mndilandire ine Mbuye
  • Hymn 1178 Mawu omwewo, nyimbo yomweyi,
  • Hymn 1508 Mundinyemere ‘ne
  • Hymn 125 Aliponso mabvuto, ena ndi oipa;
  • Hymn 50 Akhristu nyamulani
  • Hymn 1249 Tsirizani ntchito yanu
  • Hymn 1162 Mumvetu abwenzi athu,
  • Hymn 1125 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 825 Mpatse ana ‘ng’ono
  • Hymn 183 Mlemekeze, bukitsani,
  • Hymn 1822 Lawani chikondano chake;
  • Hymn 258 Kazembe wanga m’matenda,
  • Hymn 115 Mbulu wanding’amba m’nthiti,
  • Hymn 10 TSOPANO linoli,
  • Hymn 299 “Posunga nkhosa ife
  • Hymn 1846 Mtima wanga uyamike
  • Hymn 627 Mlungu wathu mwatifitsa
  • Hymn 52 Mbwere Mzimu, mbwere!
  • Hymn 1318 Ndibwera kwa Ambuyeyo,
  • Hymn 217 CHIPULUMUTSO chathu chayandika,
  • Hymn 1710 Pamtandapo, pamtandapo
  • Hymn 1248 ‘Dzanitu Wamphamvu yonse,
  • Hymn 1065 Ngakhale Satana andizunza ‘ne,
  • Hymn 747 Tadzanitu, okhulupiradi,
  • Hymn 159 YESU ndi wokonda,
  • Hymn 1504 Kodi ali ndi chilemba
  • Hymn 1402 Mverani Iye ati: idzanitu;
  • Hymn 199 NDINASOKERA kutali,
  • Hymn 1664 Ndigwadira Inu, Yesu,
  • Hymn 281 Atate, ndipempha
  • Hymn 748 Ndiye wa moyo wonse Mwiniyo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version