Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 51 PANTHAWI yakufa Ambuye,

  1. Home   »  
  2. Hymn 51 PANTHAWI yakufa Ambuye,

Hymn 51 PANTHAWI yakufa Ambuye,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 51 PANTHAWI yakufa Ambuye,

 

PANTHAWI yakufa Ambuye,
Anthu ananena:
“Dzipulumutsetu pamtandapo.”

(M) Yesu ndi mawu aakulu,
(O) Anafuula;
(M) Yesu ndi mawu aakulu,
(O)Anafuula;
“Eloyi, Eloyi
Mulungu wanga,
Mwandisiiranji,
Mwandisiiranji?”

Imfa ya Bwenzi lathu Yesu,
Yomvetsa chisoni;
Ophunzira onse anathaŵa.

Pamene anakhomedwatu,
Pamtanda Yesuyo;
Zoipa zathu zinam’psinja ‘Ye.

Imfa yake ndi yopambana,
Yotipulumutsa;
Yotitengera ife mtendere.

Post navigation

Previous: Hymn 50 PAUSIKU uja,
Next: Hymn 52 POTULUKA m’mudzimo

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1225 Ndinachita mphulupulu,
  • Hymn 1685 Nla Mlungu dzuwali;
  • Hymn 632 Tsopano tipereka mapemphero athu ano,
  • Hymn 1323 M’manja mopanda kanthu,
  • Hymn 892 Tilibe madalitso
  • Hymn 497 TILIKUIMBA nyimbo yomweyi,
  • Hymn 1602 M’mawu a Yesu Mbuyeyo,
  • Hymn 96 MTIMA wanga uyamiketu,
  • Hymn 444 Mpemphe Mbuye asunge
  • Hymn 799 Inu Mlungu kalelo
  • Hymn 589 Koma ineyu
  • Hymn 746 Imfa ndi mdima zinathawa zii!
  • Hymn 266 Ukondwere moyo wanga,
  • Hymn 668 Achisoni, obvutidwa,
  • Hymn 1321 Thanthwe long’ambikatu,
  • Hymn 878 Zokoma inde nthawizi
  • Hymn 1560 Mthandizi ndinu, mndithangate ine
  • Hymn 1480 Afika Yesu leroli,
  • Hymn 1192 Pamtanda woopsa
  • Hymn 165 ATATE,’nu, atate ’nu,
  • Hymn 910 Nlokoma Dziko langa!
  • Hymn 418 M’manja Yesu wanga
  • Hymn 1032 Ntchito za Yesu gwira
  • Hymn 1769 Ndiye amachitira
  • Hymn 689 Anapeza Mwana
  • Hymn 1857 Ndinagona mwa zoipa,
  • Hymn 333 Perekani, perekani
  • Hymn 1591 Sizitha ntchito zangazo,
  • Hymn 1833 Podwala ine pobvutidwa Andisamalira;
  • Hymn 392 Chimwemwe chomwe mpatseko
  • Hymn 77 MMENE Yesu adzabwera,
  • Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu
  • Hymn 1402 Mverani Iye ati: idzanitu;
  • Hymn 550 Wosauka Iyedi
  • Hymn 1709 Pamtandapo Ambuyeyo anafera ifetu,
  • Hymn 768 Ndi ife tinga mbewuzo
  • Hymn 1131 M’mene ine ndisauka
  • Hymn 1136 Mulungu anditsogolera
  • Hymn 135 USANABADWE, Yeremiya,
  • Hymn 314 E, moto wanu woyera
  • Hymn 1482 Tsopano inu ‘dzanitu,
  • Hymn 1463 Zoipa zakhululukidwa,
  • Hymn 344 ’TATE, ’Nu.
  • Hymn 1571 Tamani mphamvu ya Yesu,
  • Hymn 215 TATE ndili mwana wanu,
  • Hymn 15 YEHOVA ndiye Mbusa wanga,
  • Hymn 86 IYE wokhulupilira Yesu,
  • Hymn 1549 Mtitsutse titachimwa
  • Hymn 1546 Mubwere Mzimu Inu
  • Hymn 951 Ndi kale lonse mnandisunga ‘ne;
  • Hymn 175 Mlungu mverani, mphamvu patseni,
  • Hymn 120 Lekani kubvutika ndi zinthu za padziko,
  • Hymn 254 Adzanena kwa anthuwo
  • Hymn 1237 Ine kanthu ndilibe
  • Hymn 608 Maluwa abwino aphuka m’mapiri ndi m’madambomo,
  • Hymn 925 Kodi umadandaula:
  • Hymn 453 Tiana ta Ambuye tili
  • Hymn 740 Tsopano nthawi yake phwandili,
  • Hymn 930 Leroli chisoni chokha,
  • Hymn 191 Sindifuna Mbuye wina,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version