Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 28 AMBUYE ngwodalitsika,

  1. Home   »  
  2. Hymn 28 AMBUYE ngwodalitsika,

Hymn 28 AMBUYE ngwodalitsika,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 28 AMBUYE ngwodalitsika,

 

AMBUYE ngwodalitsika,
Mulungu wa Israyeli ndiye,
Poti anayang’ana naŵawombola anthu ake,

Napulumutsa tonse mwapfuko la Davide mwana wake;
Monga analankhula mwa aneneri ake,

Adzatipulumutsa kudzanja la onse akutida,
Ndipo adzachitira akulu chifundo ndi chisoni.

Ndiye akumbukira pangani loyera lake lija,
Ndi chilumbiro chake cha kwa atate Abrahamu,

Choti timtumikire osaŵaopa ’dani athu,
Ndi kuyeranso mtima mwa chilungamo nsiku zonse.

Mwana, adzakuyesa mneneritu wa Wamkulukulu,
Ndiwe udzakonzera njira ya Mbuye Wakumwamba.

Udzadziŵitsa anthu za Mpulumutsi wawo yemwe
Aŵakhululukira
Nafafaniza tchimo lawo,

Poti Mulungu wathu ali ndi mtima wachifundo.
Ndiye kumwamba komwe
Ationetsa mbanda kucha,

Poŵalitsira omwe ali mumdima ndi muimfa,
Ndi potilunjikitsa tonse munjira yamtendere.

Post navigation

Previous: Hymn 20 CHIKONDI cha Mulungu wathu,
Next: Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 83 MBUYEYO adzabwera,
  • Hymn 48 Ngakhale alemera
  • Hymn 425 AKRISTU ndi abale, tiziyenderana tonse,
  • Hymn 1001 Mafumu atiuza tikaletse ukapolo,
  • Hymn 1050 Ndafoka inetu,
  • Hymn 567 M’nyumba zonse ponseponse
  • Hymn 630 Ena atsagana nafe
  • Hymn 259 Zoipa zakanikadi,
  • Hymn 1587 Nditama Mlungu m’mtimamo,
  • Hymn 295 AMBUYE wa Kumwamba,
  • Hymn 554 Iye ndani pamtanda
  • Hymn 1096 Tifuna Inu, Mbuye,
  • Hymn 1662 Msandipitire, Yesu,
  • Hymn 69 Kwathu sipadziko, ndingopitirira,
  • Hymn 1436 Inde, lero lino Yesu
  • Hymn 1361 Ndi Aleluya imbirani
  • Hymn 53 Dalitsani mafumu athu,
  • Hymn 1474 Zilepheradi zonse kugula moyowo,
  • Hymn 790 Zimbalame zonsezi
  • Hymn 845 Ufumu wanu, Mbuye Yesu,
  • Hymn 841 Mukhale, mukhale,
  • Hymn 337 PADZIKO pano tikhalira M’moyo wosauka;
  • Hymn 6 LEMEKEZA Mulungu ’Tate,
  • Hymn 1519 M’Buku lakuyerali
  • Hymn 901 Musatifikitsemo
  • Hymn 1445 Tiyeni tonse, tinkeko
  • Hymn 2 YEHOVA Mthandizi,
  • Hymn 735 Mwa chikho chokumbutsa
  • Hymn 1065 Ngakhale Satana andizunza ‘ne,
  • Hymn 325 KODI uli ndi chisoni
  • Hymn 412 Kudzachera tsiku lijalo
  • Hymn 1355 Atate, Mwana, Mzimunso,
  • Hymn 442 MASIKA a m’dziko Mbuye,
  • Hymn 220 Kalekale ndinathawa,
  • Hymn 446 YAMIKANI nonse ’nu,
  • Hymn 1400 Tulani zoipazi, idzanitu,
  • Hymn 104 MUBWERE Mzimu Inu
  • Hymn 994 Limba mtima mbale wanga,
  • Hymn 604 ‘Tate, Mwana, Mzimu, ndinu
  • Hymn 332 NDIKONDWA kuganizirabe
  • Hymn 467 Ife ana sitiopa,
  • Hymn 1363 Tamani Ambuye,
  • Hymn 1654 Mbuye, mutsaganetu
  • Hymn 494 YESU Mbusa, mutimvere,
  • Hymn 400 Dzuwa liwala, m’tulotu
  • Hymn 1063 Pokhala mtendere mu mtimangamu,
  • Hymn 22 MU ZONSE abale yamikani,
  • Hymn 1303 Aa! Mulungu wanga,
  • Hymn 1056 Mkhalidwe wanu mundipatse,
  • Hymn 222 Ndilikudzatu,
  • Hymn 819 Lero tigone,
  • Hymn 459 Aphunzitse anthuwo,
  • Hymn 1724 Ambuye mthandize inetu
  • Hymn 326 TSIKU Iidzafika mbale,
  • Hymn 696 Ufumu wake udalitsa
  • Hymn 1581 Ndi nyimbo yabwino
  • Hymn 1719 Ku Mzinda wakuyerawo
  • Hymn 1182 Chikhulupiro chomwenso
  • Hymn 882 Kodi tikulema nazo
  • Hymn 416 Woyenera ndani kunka

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version