Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 94 KHAMULO liliko

  1. Home   »  
  2. Hymn 94 KHAMULO liliko

Hymn 94 KHAMULO liliko

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 94 KHAMULO liliko

 

KHAMULO liliko
Kumwambako mbuu!
Pakukhala ndi Yesu
Aimbirako:

Kwa Iye atikonda
Natsuka ’fe mbuu!
E! kukhale ulemu
Kwa Mbuyathuyu.

Onsewa ’nachimwa
Nadetsedwa bii,
Nthaŵi yino ayera
Naimbiradi:

Akhala mafumu
Kwa Mbuyathuyo,
Anawombola onse
Ndi mwaziwo pyu!

Akadakhalabe
Osaukako
Ngati Yesu sakana
Wombolatuwo.

Ndi nyimbo yabwino
Tidzamtamako,
Kuti ena pakumva
Amuyimbirenso:

Post navigation

Previous: Hymn 80 KUDZA kwa Mbuye
Next: Hymn 101 MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1656 Inu mundibisadi
  • Hymn 1105 Khala chete mtima wanga
  • Hymn 1002 Haya! ‘Nzanga taonani Yoonekayo
  • Hymn 1289 Ndinasokeratu kutaliko,
  • Hymn 842 Tipempha kuti Mpingo wanu
  • Hymn 367 MPULUMUTSI, tikagona
  • Hymn 1344 Yamba ulendowo
  • Hymn 98 YESU, Bwenzi la ochimwa,
  • Hymn 317 Zambiri zagona m’kholamo,
  • Hymn 1434 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 1277 Kuti mukhululukira tchimo langalo
  • Hymn 216 NDISAUKA, ndinachimwa,
  • Hymn 96 Kodi mudzampembedza Mbuye
  • Hymn 1623 Adzatenga anthu ake
  • Hymn 1734 “Senzani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 972 Akristu limbikani,
  • Hymn 418 UDINDO wolalikira Uthenga,
  • Hymn 1215 Ndimkonde Kristuyo,
  • Hymn 759 Ndilawako tsopanoli
  • Hymn 440 Yesu wakufatsa mtima
  • Hymn 369 Lowani m’nyumba mwakemu
  • Hymn 735 Mwa chikho chokumbutsa
  • Hymn 1261 Kale ndinakana Inu, Ndinathawatu;
  • Hymn 53 Dalitsani mafumu athu,
  • Hymn 244 TIMVE za anamwali khumi,
  • Hymn 189 MLENDO ali pakhomo,
  • Hymn 1580 Akadakhalabe
  • Hymn 308 AULENDO, munka kuti
  • Hymn 1515 Ndikachimwa, Bukuli
  • Hymn 803 Mulungu wanga, Dzuwatu
  • Hymn 16 Chikhulupiriro chathu
  • Hymn 478 YESU atiuza tiŵale ’fe.
  • Hymn 1752 Napulumutsa tonse
  • Hymn 1698 Chinkana dziko lonselo
  • Hymn 178 Machimo anga ngambiri
  • Hymn 815 Dzuwa lapita,
  • Hymn 634 Mtifungatire ndi mapiko paulendo pathu,
  • Hymn 515 Kuphiri la ‘Zitona,
  • Hymn 1356 Lemekeza Mlungu ‘Tate,
  • Hymn 1221 Bwenzi ndinamkomanayo,
  • Hymn 129 WODALA ndiye munthuyo,
  • Hymn 413 Yesu ndiye Bwenzi lathu,
  • Hymn 19 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 716 Tibwezeretu bwanjiko?
  • Hymn 346 PEMPHERO ndiko kufuna,
  • Hymn 1263 Mbuye, ndingogonj tere, Ndibvomerapo;
  • Hymn 1380 Tilemekezetu
  • Hymn 257 Ndinasiya amayi,
  • Hymn 152 AMBUYE wathu Yesu
  • Hymn 45 IFE timakufunani
  • Hymn 1179 N’kamvera Yesu ndikakondwera,
  • Hymn 125 ODALA ali iwo,
  • Hymn 937 Chitsime chachikondi
  • Hymn 313 MUNDIŴALIRE m’njira mwangamo,
  • Hymn 864 Ndi chikondi mtithandize kuigwira nkhondoyi;
  • Hymn 1587 Nditama Mlungu m’mtimamo,
  • Hymn 1341 Tadza kukudyaku,
  • Hymn 334 Tsugulani mtima wanu
  • Hymn 1270 Ndayesa kudzikonzadi,
  • Hymn 174 Haya, anzathu, itilinda nkhondo;

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version