Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 82 YANG’ANANI, anthu onse,

  1. Home   »  
  2. Hymn 82 YANG’ANANI, anthu onse,

Hymn 82 YANG’ANANI, anthu onse,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 82 YANG’ANANI, anthu onse,

 

YANG’ANANI, anthu onse,
Yesu Mbuye wathuyo:
Alinkudza ndi ulemu,
Kuoneka m’Mwambamo.

Anthu onse am’lambire
Yesu Mwana wa Mulungu
Alinkudza ndi ulemu
Wopambana, indetu.

Adzatenga anthu ake
Akumvera pansipo
Iwo adzakhala naye
M’dziko la Kumwambako.

Koma anthu onse omwe
Anamnyoza pansipo,
Nthaŵi Yesu alinkudza
Adzaopa m’mtimamo.

Ife tonse tikumbuke
Mawu ake onsewo;
Timuyang’anire Iye,
Yesu Mbuye wathuyo.

Post navigation

Previous: Hymn 80 KUDZA kwa Mbuye
Next: Hymn 101 MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1056 Mkhalidwe wanu mundipatse,
  • Hymn 1578 Onsewa ‘nachimwa
  • Hymn 427 AULENDO amayenda
  • Hymn 75 Ndiperekatu
  • Hymn 916 Akondwerera anthu
  • Hymn 1624 Koma anthu onse omwe
  • Hymn 53 AMBUYE Yesu anamva chisoni,
  • Hymn 454 Kapena m’mtima ndimakwiya,
  • Hymn 1405 Ati: “Undiuze
  • Hymn 1701 Nditani Bwenzi langa
  • Hymn 391 MUNDIMVERE, Mbuye wanga
  • Hymn 82 YANG’ANANI, anthu onse,
  • Hymn 144 AMENE adzavomereza ndithu,
  • Hymn 1776 Tiyeni timgwadire
  • Hymn 1314 Mulungu ali nane!
  • Hymn 223 Ndafoka, ndaipa,
  • Hymn 652 Munene Mbuye ‘nenetu,
  • Hymn 111 Nkhope yake ‘kabisika,
  • Hymn 296 TIYENI Akhristu,
  • Hymn 260 ODALA ndi onsewo,
  • Hymn 1512 Cholimbitsa mtima ndi
  • Hymn 58 PAMTANDAPO Ambuyeyo
  • Hymn 83 Mpulumutsi Wokondedwa,
  • Hymn 45 IFE timakufunani
  • Hymn 457 Palibe mwana wakuchepa
  • Hymn 373 NYUMBA ya Mulungu, ili pano,
  • Hymn 1008 Wakuchezacheza naye
  • Hymn 138 Kumva ulikumva, ulikumva,
  • Hymn 161 LERO lino mbale wanga,
  • Hymn 483 Ndife akuchoka,
  • Hymn 730 A! Yesu mwapangana
  • Hymn 1285 Yesu, n’kupatsani zonse,
  • Hymn 1241 Ati: Mwana, kumbukira
  • Hymn 978 Mtima wanu wonse ndithu
  • Hymn 1716 Anena mawu m’mtanda momwe,
  • Hymn 753 Getsemane ndionako
  • Hymn 612 Oyamika Mlungu mbwere,
  • Hymn 846 Kristu wakuyeratu,
  • Hymn 273 Mlungu akuyang’aniredi
  • Hymn 941 Ndi Mbuyeyo tikhalamo,
  • Hymn 707 Dalitseni, Mbuye, zonse
  • Hymn 1007 M’mene umauka m’mawa,
  • Hymn 17 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 837 Koma kalelo mnakhalitsa pano,
  • Hymn 399 Tchimo lathu lonse, Yesu,
  • Hymn 94 KHAMULO liliko
  • Hymn 737 Mommuno, Mbuye, tionanetu,
  • Hymn 1130 Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja
  • Hymn 290 NAMONDWE wawuka,
  • Hymn 98 YESU, Bwenzi la ochimwa,
  • Hymn 76 Ndipereka zanga zonse
  • Hymn 348 CHIKHULUPIRIRO chathu
  • Hymn 401 Dzuwa la lero lonseli
  • Hymn 1081 Ndikabisala mwanu
  • Hymn 103 Bwenzi lathu ndinutu,
  • Hymn 158 WOCHIMWA iwe, bweratu,
  • Hymn 1554 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 1208 Kalelo! Kalelo!
  • Hymn 1237 Ine kanthu ndilibe
  • Hymn 793 Tikondwera kuti

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version