Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 79 PAKWITANA Mbuye wanga

  1. Home   »  
  2. Hymn 79 PAKWITANA Mbuye wanga

Hymn 79 PAKWITANA Mbuye wanga

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 79 PAKWITANA Mbuye wanga

 

PAKWITANA Mbuye wanga
Potsiriza dzikoli,
Pakufika tsiku la kuŵalalo,
Posonkhana akumvera,
Pakuona Yesuyo,
Ndidzakondwerera naye komweko.

Pakuyiitana Mbuye wanga,
Pakuyiitana Mbuye wanga,
Pakuyiitana Mbuye wanga,
Ndidzakondwerera naye komweko.

Potuluka m’manda mwawo
Anthu ake onsewo,
Tidzasanganatu nawo nthaŵiyo.
Pakuluka osankhidwa,
Kunka naye Yesuyo,
Ndidzakondwerera naye komweko.

Tisaleke kugwirabe
Ntchito ya Mulunguyo,
Tibukitse mbiri yake m’dzikoli,
Ndi podzatha moyo wathu
Ndi zintchito zathuzo,
Tidzakondwerera naye komweko.

Post navigation

Previous: Hymn 60 ZATHEDWA zonsetu
Next: Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1093 Odala ndi onsewo
  • Hymn 776 Tikondwereratu
  • Hymn 80 KUDZA kwa Mbuye
  • Hymn 903 Iwo salekana, iwo salekana,
  • Hymn 1788 Mtimanga, bwera kuti upumule
  • Hymn 433 MULUNGU wa Kumwamba bwera kunoku
  • Hymn 207 AMBUYE ndamvatu Mawu anu,
  • Hymn 1054 Ndilira mtima wakulapa
  • Hymn 233 M’mene ndapenya mwazi wa
  • Hymn 145 MBIRI yakale lomwe
  • Hymn 358 Dzina lake Yesuyo,
  • Hymn 244 Ndidze pafupi pa
  • Hymn 118 Musaone zobvalazo,
  • Hymn 683 Musamaopa kanthu ‘yi, tamani Yesuyo;
  • Hymn 1245 Ine ndidzakuonetsa
  • Hymn 614 Adzabwera Mbuye wathu
  • Hymn 410 Ana ake angonga
  • Hymn 639 Mulungu mwa Atatu,
  • Hymn 1629 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 1526 Mbuye wondipulumutsa
  • Hymn 967 Mbuye, ndapangana
  • Hymn 13 PAPHIRI ndi padambo,
  • Hymn 278 TITHAŴIRENJI ifetu
  • Hymn 1392 Mlungu kuona athiratu
  • Hymn 1101 Ngati mtima sumakonda
  • Hymn 44 NTHAWIYO anam’gwira Yesu,
  • Hymn 415 Tidzalandirabe komwe
  • Hymn 1427 Penyetsetsa Yesu,
  • Hymn 392 ANU Mbuye ndifetu!
  • Hymn 732 1 Ndinamva njala, Yesu,
  • Hymn 634 Mtifungatire ndi mapiko paulendo pathu,
  • Hymn 860 Nthawi yina adzadzuka
  • Hymn 259 CHISOMO chodabwitsacho,
  • Hymn 307 Atate Wamkulu ndi wamphamvu zonse,
  • Hymn 525 Afike masiku
  • Hymn 891 Akakusowa malo
  • Hymn 1073 Mwa ine myatse moto wanu wakuyera mbuu,
  • Hymn 1057 Ndilira ine kukayenda
  • Hymn 235 ADALITSIKA munthuyo,
  • Hymn 411 TAMVA mawu omwewo,
  • Hymn 1827 Abramu kalelo anamvera bwino;
  • Hymn 1583 Dzina la Yesuyo
  • Hymn 226 BWENZI ndinamkomanayo
  • Hymn 153 Pemphero ndiko kufuna,
  • Hymn 688 Anthu akum’mawa
  • Hymn 285 DZIKO lino lapansi,
  • Hymn 1456 Pakuti anthu akumvera
  • Hymn 1789 Nditani ine kubwezera Mbuye
  • Hymn 812 Ndi ena sanamvera ‘yi,
  • Hymn 109 MUTHIRE, Yesu, m’mtimanga
  • Hymn 1497 Simbani mobwereza,
  • Hymn 103 Bwenzi lathu ndinutu,
  • Hymn 1579 Akhala mafumu
  • Hymn 52 POTULUKA m’mudzimo
  • Hymn 836 Kamoyo kanga katha lero lino,
  • Hymn 1332 Imba kawiri ndi kawirinso,
  • Hymn 284 Yesu Mfumu Inu
  • Hymn 1208 Kalelo! Kalelo!
  • Hymn 1856 Mzimu, msandipitirire,
  • Hymn 745 Anatifera nsembe Iyeyo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version