Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 71 DZIKO lino lapansi, ndilibetu abwenzi,

  1. Home   »  
  2. Hymn 71 DZIKO lino lapansi, ndilibetu abwenzi,

Hymn 71 DZIKO lino lapansi, ndilibetu abwenzi,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 71 DZIKO lino lapansi, ndilibetu abwenzi,

 

DZIKO lino lapansi, ndilibetu abwenzi,
Ndili ndekha mpanjira n’kwaŵenitu;
Ndilibetu chakudya, ndilibetu chakumwa,
Ndingoyenda mpanjira n’kwaŵenitu.

N’kwawenitu,
N’kwawenitu,
Dziko lino sikwathu
N’kwaŵenitu.

Dziko lino lapansi mavuto ndi osatha,
Ine sindingalithe n’kwaŵenitu;
Ukasowa chumacho, abwenzi akuthawa,
Koma kwathu satero n’kwaŵenitu.

Anyamata, ‘sungwana
Samaopa Mulungu,
Sichifukwa chinanso n’kwaŵenitu;
Abambo ndi amayi
Samaopa Mulungu,
Sichifukwa chinanso n’kwaŵenitu.

Tiyeni abale ‘fe tiyang’ane kwa Yesu,
Yemwe angatipatse moyowotu;
Moyo uno wam’dziko abale ndi wozunza,
Moyo wokoma ndiwo wa Yesuyo.

Post navigation

Previous: Hymn 60 ZATHEDWA zonsetu
Next: Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1656 Inu mundibisadi
  • Hymn 1729 Munthu Wazisoniyo
  • Hymn 125 Aliponso mabvuto, ena ndi oipa;
  • Hymn 211 Chakudya ichi ndi cha iwenso,
  • Hymn 605 Chifukwa cha zokoma mtima zonse za ulerezo,
  • Hymn 91 NDITAME Mlungu m’mtimamo,
  • Hymn 1220 Bwenzi ndinamkomanayo
  • Hymn 28 AMBUYE ngwodalitsika,
  • Hymn 69 Kwathu sipadziko, ndingopitirira,
  • Hymn 230 AMBUYANGA Yesu,
  • Hymn 1496 Mawu amveke bwino,
  • Hymn 1157 Mtendere wapambana m’Mwambamo
  • Hymn 1129 Mbuyanga Yesu, ndikapanda Inu
  • Hymn 1237 Ine kanthu ndilibe
  • Hymn 328 KULIBE vuto
  • Hymn 1484 Idzatu, idzatu
  • Hymn 1147 Khalani duu! Pakufa ifetu,
  • Hymn 984 Mpingo wa Mulungu
  • Hymn 900 Mutipatse leroli
  • Hymn 325 Walira Yesu wolimbitsayo,
  • Hymn 782 Aleluya, aleluya,
  • Hymn 597 Mlungu ali nane
  • Hymn 1097 Njira yanga sindidziwa,
  • Hymn 613 Dziko lonse nla Mulungu
  • Hymn 285 Ndipempha, Ambuye,
  • Hymn 1077 Khalatu woyera,
  • Hymn 450 YESU, munditsogoza
  • Hymn 856 Kuunika kuoneka
  • Hymn 1568 Kudzoza kwanu kutipatsa
  • Hymn 489 YESU ndiye Bwenzi lathu,
  • Hymn 1739 Ife timakufunani
  • Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda
  • Hymn 1252 Pakukumbukira zanga
  • Hymn 1123 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 214 KUNALI munthu ku Yeriko,
  • Hymn 276 MKRISTU, ulimbike
  • Hymn 393 Tilikuimba nyimbo yomweyi,
  • Hymn 1101 Ngati mtima sumakonda
  • Hymn 1341 Tadza kukudyaku,
  • Hymn 981 Tiyeni Akristu,
  • Hymn 429 M’DZANJA lanu Ambuye,
  • Hymn 808 Atipsinjadi masoka,
  • Hymn 1736 “Senzani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 946 Ngakhale enawo aleke kwimbako,
  • Hymn 3 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 301 Mwanawankhosa
  • Hymn 535 Mbuye timlemekeze,
  • Hymn 308 Ifetu kuchimwa, Mbuye,
  • Hymn 173 MWAMVA Mawu a Mulungu;
  • Hymn 126 Mwa ine, moyo wanga ndi Yesu
  • Hymn 455 Mdileke kulimbna ndi
  • Hymn 1381 Ndi mitima yokondwera
  • Hymn 934 Mnamwalira Inu paja,
  • Hymn 684 Zipata zatsegudwa mbee! Za m’dziko monsemo;
  • Hymn 263 AMBUYE mundisunge
  • Hymn 1401 Imvani mawu ake, idzanitu,
  • Hymn 1320 Ndayang’anira Mbuyeyo,
  • Hymn 840 Ambuye munapatsa tsiku
  • Hymn 321 PAKUONA imfayo
  • Hymn 1161 Wapumitsa mtima wanga,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version