Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 71 DZIKO lino lapansi, ndilibetu abwenzi,

  1. Home   »  
  2. Hymn 71 DZIKO lino lapansi, ndilibetu abwenzi,

Hymn 71 DZIKO lino lapansi, ndilibetu abwenzi,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 71 DZIKO lino lapansi, ndilibetu abwenzi,

 

DZIKO lino lapansi, ndilibetu abwenzi,
Ndili ndekha mpanjira n’kwaŵenitu;
Ndilibetu chakudya, ndilibetu chakumwa,
Ndingoyenda mpanjira n’kwaŵenitu.

N’kwawenitu,
N’kwawenitu,
Dziko lino sikwathu
N’kwaŵenitu.

Dziko lino lapansi mavuto ndi osatha,
Ine sindingalithe n’kwaŵenitu;
Ukasowa chumacho, abwenzi akuthawa,
Koma kwathu satero n’kwaŵenitu.

Anyamata, ‘sungwana
Samaopa Mulungu,
Sichifukwa chinanso n’kwaŵenitu;
Abambo ndi amayi
Samaopa Mulungu,
Sichifukwa chinanso n’kwaŵenitu.

Tiyeni abale ‘fe tiyang’ane kwa Yesu,
Yemwe angatipatse moyowotu;
Moyo uno wam’dziko abale ndi wozunza,
Moyo wokoma ndiwo wa Yesuyo.

Post navigation

Previous: Hymn 70 LAMBIRA, Mfumuyo,
Next: Hymn 72 YESU wakukoma mtima,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1631 Mudzabwera, mudzabwera;
  • Hymn 407 Zochimwa sizilowako,
  • Hymn 282 Ine ndili munthu
  • Hymn 1491 Zokandweretsa m’dzikomu
  • Hymn 536 Ana inu, myamikeni
  • Hymn 124 Aliponso adani am’kati ndi akunja;
  • Hymn 358 MLUNGU ali muno,
  • Hymn 986 Tiyeni anzathu
  • Hymn 140 NDINAMIRA m’machimo, wosaonekanso,
  • Hymn 311 Tifuna kuchita chifuniro chanu,
  • Hymn 1733 Adzabwera Iyenso
  • Hymn 1632 Ndi chiyembekezo ichi
  • Hymn 204 NDASIYA zonse ndi Yesu kalelo,
  • Hymn 526 Mnandidzera, Ambuye,
  • Hymn 1569 Mtima wodetsa mukonzere,
  • Hymn 1019 Tsata, tsata, nditsatadi Yesu;
  • Hymn 1536 Ndilira Mzimu leroli,
  • Hymn 337 ‘Tate ‘Nu,
  • Hymn 94 KHAMULO liliko
  • Hymn 872 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 1331 Yesu wathu Mbuyeyo
  • Hymn 264 Bvinabvina moyo wanga,
  • Hymn 990 Poyesedwa ine
  • Hymn 264 KHALATU woyera, pempheratu m’tseri;
  • Hymn 1428 Penyetsetsa Yesu
  • Hymn 1586 Mbuye Yesu timtamanda
  • Hymn 1461 Sing’anga ‘mkulu ndiye Yesu,
  • Hymn 51 PANTHAWI yakufa Ambuye,
  • Hymn 1662 Msandipitire, Yesu,
  • Hymn 265 Imbirira moyo wanga,
  • Hymn 892 Tilibe madalitso
  • Hymn 1070 Mthandize Mbuye, timvetu,
  • Hymn 98 Ndidzamwona maso ndi maso
  • Hymn 171 IWE tiye, iwe tiye,
  • Hymn 113 Likalira llipengalo,
  • Hymn 101 MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,
  • Hymn 279 MBUYE, nditsate bwanjiko?
  • Hymn 921 Komwe Mbusa kwawoko
  • Hymn 603 Mzimu wanu Wakuyera,
  • Hymn 434 Zondipingitsa zonse
  • Hymn 1119 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 1670 Bwenzi ndiye wakufera,
  • Hymn 236 Omvana ndi Yesu,
  • Hymn 854 Timlemekeze Mlunguyu
  • Hymn 189 MLENDO ali pakhomo,
  • Hymn 7 “Mbuye Woyera! E, Woyeranokha!
  • Hymn 1104 Mndisungire mtima wanga,
  • Hymn 464 AKAZI anadza kwa Yesu ndi anawo,
  • Hymn 175 A! MBUSA wathu amvatu
  • Hymn 740 Tsopano nthawi yake phwandili,
  • Hymn 354 Tinafunafunatu,
  • Hymn 718 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 937 Chitsime chachikondi
  • Hymn 1430 Ndipo pakulowa
  • Hymn 810 Tsopano lino kwada bii,
  • Hymn 1284 Kale ndinalira Inu,
  • Hymn 473 YESU wa Kumwamba,
  • Hymn 258 Kazembe wanga m’matenda,
  • Hymn 345 Ubwere,
  • Hymn 230 Ndisamba ndiyera,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version