Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 70 LAMBIRA, Mfumuyo,

  1. Home   »  
  2. Hymn 70 LAMBIRA, Mfumuyo,

Hymn 70 LAMBIRA, Mfumuyo,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 70 LAMBIRA, Mfumuyo,

 

LAMBIRA, Mfumuyo,
Ndi Yesu Mbuyathu,
Tamvani nyimbo za ‘mithenga aKumwambako;
Nafenso pansipa
Tim’yamikire ’Ye,
Ndi Mpulumutsi wathu wotifera kalero.

Lambira Yesuyo,
Wokonda tonsefe;
Mabala ake achikondi awonekabe;
Tisayiwale ’yi
Zoŵaŵa zakezo,
Tileke kum’chimwira, kum’sautsa Yesuyo.

Lambira Yesuyo,
Uthenga wakewu
Uyanjanitsa anthu onse m’dziko munomo:
Amaiŵala za
Kudana kwawoko,
Nayamikira Mfumu yamtendere monsemo.

Lambira Mfumuyo
Wolenga zonsezi:
Nyenyezi, dziko, dzuŵa, mwezi ndi mitamboyi;
Tikweze dzinalo
La Mbuye Yesuyo,
Tim’yamikire pansi pano ndi Kumwambako.

Post navigation

Previous: Hymn 60 ZATHEDWA zonsetu
Next: Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 411 Yesu adza kukundika
  • Hymn 1443 Ambuye Yesu anatsira
  • Hymn 70 Mbuye ndinu bwenzi langa ndithu,
  • Hymn 647 Tiyamike Mlungu ‘Tate,
  • Hymn 927 Pakutsazikana nanu
  • Hymn 432 KRISTU ndiye Mwala wathu,
  • Hymn 697 Zolengedwa zonse zidze
  • Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 916 Akondwerera anthu
  • Hymn 496 MBUYE dalitsani Afirika.
  • Hymn 991 Ndi zapansi pano
  • Hymn 1411 Yesu akuitanani
  • Hymn 1268 Mundilandiretu,
  • Hymn 224 LINDIKOMERA dzina la Ambuye Yesu wanga,
  • Hymn 528 Amithenga ‘naimba pamlengapo,
  • Hymn 744 Kristu ndi mwini moyo wathuwu,
  • Hymn 344 ’TATE, ’Nu.
  • Hymn 978 Mtima wanu wonse ndithu
  • Hymn 340 PEMPHERA m’mbanda kucha,
  • Hymn 1326 A! Mbusa wathu amvatu
  • Hymn 1360 Ndi Aleluya imbirani
  • Hymn 1617 Anadzuka,
  • Hymn 406 M’MENE umauka m’maŵa,
  • Hymn 229 Woba wakufa ‘napenya
  • Hymn 322 Walira Yesu m’dziko linoli,
  • Hymn 1831 M’mitsinje yamtendere mtima wanga aumwetsa;
  • Hymn 154 SING’ANGA ‘mkulu ndiye Yesu,
  • Hymn 306 YAMBA ulendo mnzanga,
  • Hymn 601 Akaona masautso
  • Hymn 1353 Ambuye Yesu, Inutu
  • Hymn 205 KWA Inu Yesu ndilira,
  • Hymn 1562 Mzimu Woyera, mudze mumitima mwathumo,
  • Hymn 1420 Abale ‘nu, abale ‘nu,
  • Hymn 439 MLUNGU wathu mwatifitsa
  • Hymn 1529 Mndithandize kukondana
  • Hymn 1300 Poyenda m’mdima bii,
  • Hymn 567 M’nyumba zonse ponseponse
  • Hymn 64 LERO Kristu anauka,
  • Hymn 909 Ife tikondwera, ife tikondwera,
  • Hymn 1748 Ambuye tsopano lino,
  • Hymn 1294 Wakuba uja nachiona,
  • Hymn 1203 Zambiri zangazo
  • Hymn 841 Mukhale, mukhale,
  • Hymn 1740 Yesu, ndi chifundo chanu
  • Hymn 498 AMBUYE, mtidalitsetu,
  • Hymn 1143 Tikhale ndithu pomwepo;
  • Hymn 1190 Aleluya, mlemekeze,
  • Hymn 457 Palibe mwana wakuchepa
  • Hymn 1058 Chimwemwe chija chamumtima
  • Hymn 1597 Timchimwira kopambana,
  • Hymn 1664 Ndigwadira Inu, Yesu,
  • Hymn 285 Ndipempha, Ambuye,
  • Hymn 1125 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 431 AKAPANDA kumanga,
  • Hymn 1538 Mzimu Woyera, mudzetu
  • Hymn 724 Ndine mlendo pansi pano,
  • Hymn 895 Ndikabwera ndi katundu
  • Hymn 1376 Akulu nonse ndi mafumu ‘nu,
  • Hymn 262 “KHALA mwa Ine,” Yesu anatero;
  • Hymn 272 Ankhondowo poona

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version