Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 70 LAMBIRA, Mfumuyo,

  1. Home   »  
  2. Hymn 70 LAMBIRA, Mfumuyo,

Hymn 70 LAMBIRA, Mfumuyo,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 70 LAMBIRA, Mfumuyo,

 

LAMBIRA, Mfumuyo,
Ndi Yesu Mbuyathu,
Tamvani nyimbo za ‘mithenga aKumwambako;
Nafenso pansipa
Tim’yamikire ’Ye,
Ndi Mpulumutsi wathu wotifera kalero.

Lambira Yesuyo,
Wokonda tonsefe;
Mabala ake achikondi awonekabe;
Tisayiwale ’yi
Zoŵaŵa zakezo,
Tileke kum’chimwira, kum’sautsa Yesuyo.

Lambira Yesuyo,
Uthenga wakewu
Uyanjanitsa anthu onse m’dziko munomo:
Amaiŵala za
Kudana kwawoko,
Nayamikira Mfumu yamtendere monsemo.

Lambira Mfumuyo
Wolenga zonsezi:
Nyenyezi, dziko, dzuŵa, mwezi ndi mitamboyi;
Tikweze dzinalo
La Mbuye Yesuyo,
Tim’yamikire pansi pano ndi Kumwambako.

Post navigation

Previous: Hymn 69 KONDWERANI dzuŵa lino,
Next: Hymn 71 DZIKO lino lapansi, ndilibetu abwenzi,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1699 A! Mutu wakuyera,
  • Hymn 1519 M’Buku lakuyerali
  • Hymn 1368 Mitambo inu yakumwambako,
  • Hymn 969 Akathira nsembe
  • Hymn 482 TCHIMO musalole, musadziipitse,
  • Hymn 1135 Mulungu anditsogolera,
  • Hymn 795 Sitinanyalanyalaza
  • Hymn 1182 Chikhulupiro chomwenso
  • Hymn 1593 Wina atikonda ife,
  • Hymn 839 Adani sindiopa mukalipo;
  • Hymn 1377 Ndi amithenga akumwambako,
  • Hymn 111 Nkhope yake ‘kabisika,
  • Hymn 766 Monga zomera zonsezo
  • Hymn 745 Anatifera nsembe Iyeyo,
  • Hymn 232 Uchita kwombola,
  • Hymn 931 Tikagwidwa ndi chisoni,
  • Hymn 1275 Mtima ‘we siya ndi Yesu nsonizi,
  • Hymn 189 MLENDO ali pakhomo,
  • Hymn 152 Inde, Yesu, mundikonda,
  • Hymn 1069 Zochimwa zathu m’mtimamo
  • Hymn 947 Akristu tonsefe, tikondwe m’Dzikoli
  • Hymn 308 Ifetu kuchimwa, Mbuye,
  • Hymn 919 ‘Tate, mwa kusunga kwanu
  • Hymn 1320 Ndayang’anira Mbuyeyo,
  • Hymn 281 MBUYE, mwatiuza ’fe
  • Hymn 757 Sindili woyenera ‘ne;
  • Hymn 1724 Ambuye mthandize inetu
  • Hymn 1249 Tsirizani ntchito yanu
  • Hymn 248 Pena pakufadi,
  • Hymn 1076 Khalatu woyera,
  • Hymn 872 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 1511 Mndidalitsere ‘ne
  • Hymn 1520 Mbuye, Mawu anu
  • Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,
  • Hymn 1252 Pakukumbukira zanga
  • Hymn 59 IMVANI uthenga,
  • Hymn 936 Ukatha moyo wanga
  • Hymn 1017 Tisasungaluke ‘yi,
  • Hymn 308 AULENDO, munka kuti
  • Hymn 330 N’LOKOMA Dziko langa!
  • Hymn 1641 Pakufika asonkhanitsa
  • Hymn 604 ‘Tate, Mwana, Mzimu, ndinu
  • Hymn 698 Polenga dzikoli,
  • Hymn 464 Yesu atiuza tiyambemo,
  • Hymn 417 M’manja a Yesu wanga
  • Hymn 849 Tadzuka mzimu wanga’we
  • Hymn 239 Akumwambawo
  • Hymn 125 ODALA ali iwo,
  • Hymn 398 Lero lino mwatipatsa
  • Hymn 612 Oyamika Mlungu mbwere,
  • Hymn 992 Mukandipweteka,
  • Hymn 636 Yehova Mlungu wathu,
  • Hymn 1837 Mbuye ndiye wachifundo,
  • Hymn 1482 Tsopano inu ‘dzanitu,
  • Hymn 1001 Mafumu atiuza tikaletse ukapolo,
  • Hymn 183 Mlemekeze, bukitsani,
  • Hymn 489 Yesu, ndikabwera,
  • Hymn 1680 Aleluya, Aleluya, Aleluya!
  • Hymn 674 Anthu onse taukani,
  • Hymn 16 MTIMA wanga lemekeza,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version