Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 64 LERO Kristu anauka,

  1. Home   »  
  2. Hymn 64 LERO Kristu anauka,

Hymn 64 LERO Kristu anauka,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 64 LERO Kristu anauka,

 

LERO Kristu anauka,
Aleluya.
Ndilo tsiku lokondwera.
Aleluya.
Iye kale anafera,
Aleluya.
Nawombola otaika,
Aleluya.

Timwimbire zomtamanda
Aleluya.
Ndiye Kristu wa Kumwamba
Aleluya.
Natsikira kumanda,
Aleluya.
Nalanditsa akuipa.
Aleluya

Koma masauko ake,
Aleluya.
Anatiwombola ife.
Aleluya.
Ndiye Mfumu ya mafumu,
Aleluya.
Mwana ndithu wa Mulungu.
Aleluya.

Timwimbire Mulungu wathu,
Aleluya.
Kuti atikonda ndithu:
Aleluya.
Mtamenso angelo inu,
Aleluya.
Ndiye ‘Tate, Mwana, Mzimu
Aleluya.

Post navigation

Previous: Hymn 60 ZATHEDWA zonsetu
Next: Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 84 LIDZE msanga dzuŵa lanu
  • Hymn 693 Adzapambana Yesu ponse
  • Hymn 244 TIMVE za anamwali khumi,
  • Hymn 1007 M’mene umauka m’mawa,
  • Hymn 1783 Tinasokera ngati nkhosa,
  • Hymn 1523 Atisangalatsa,
  • Hymn 33 OWONADI mtima,
  • Hymn 211 Chakudya ichi ndi cha iwenso,
  • Hymn 1071 Kumwamba Yesu mthandize,
  • Hymn 1066 Uchimo unapachikidwa pomwe
  • Hymn 13 PAPHIRI ndi padambo,
  • Hymn 1360 Ndi Aleluya imbirani
  • Hymn 716 Tibwezeretu bwanjiko?
  • Hymn 439 MLUNGU wathu mwatifitsa
  • Hymn 1255 Chitha nchiani kund’yeretsa?
  • Hymn 1068 Ambuye, thandizenitu
  • Hymn 825 Mpatse ana ‘ng’ono
  • Hymn 723 Mundimvere, Mbuye wanga
  • Hymn 1564 Mufike monga moto wakuotcha zomwezo.
  • Hymn 118 PANALI munthu amene,
  • Hymn 640 Anakwatira kale
  • Hymn 298 “Tadodoma, abusa,
  • Hymn 478 YESU atiuza tiŵale ’fe.
  • Hymn 1374 Inu mumvere anyamatawo,
  • Hymn 10 TSOPANO linoli,
  • Hymn 26 NDIKULEMEKEZA
  • Hymn 525 Afike masiku
  • Hymn 316 Ndikhazikike inetu,
  • Hymn 1120 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 1698 Chinkana dziko lonselo
  • Hymn 811 Wopulumutsa mudzetu;
  • Hymn 1691 Lero Kristu anauka, Aleluya,
  • Hymn 1315 Ambuye ‘naitana ‘ne:
  • Hymn 1485 Unachimwachimwa ndithu,
  • Hymn 1012 Ndi zipatsozo,
  • Hymn 1556 Mzimu Woyera, mudzetu kwa ine,
  • Hymn 408 ABALE nonse mulindiranji?
  • Hymn 470 Mutiletse tisaname
  • Hymn 1784 Komweko titasaukira,
  • Hymn 458 USIKUWO, woyerawo!
  • Hymn 1338 Munachita nthantha kale,
  • Hymn 702 Mbuye wathu mutipatsa
  • Hymn 555 Mkucha wake ndaniyo
  • Hymn 943 Onse aliko takonda kalelo,
  • Hymn 909 Ife tikondwera, ife tikondwera,
  • Hymn 187 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 87 IDZANI nonse ’nu
  • Hymn 1149 Chete! Chete!
  • Hymn 747 Tadzanitu, okhulupiradi,
  • Hymn 1369 Paphiri paja papakulupo,
  • Hymn 1608 Yesu, dzina lakukonda
  • Hymn 951 Ndi kale lonse mnandisunga ‘ne;
  • Hymn 234 Kwa kutha kwa moyo,
  • Hymn 306 Ona Mwanawanakhosayo
  • Hymn 408 Oipa tili tonsefe;
  • Hymn 410 MAWU akewo anamveka ponse,
  • Hymn 681 Ankhondo a Mulungu ‘nu, yendani m’njiramo,
  • Hymn 74 Ndipereka zanga zonse
  • Hymn 1715 Kodi misozi itisowa,
  • Hymn 960 Tilikupita kwathu kuja

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version