Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 64 LERO Kristu anauka,

  1. Home   »  
  2. Hymn 64 LERO Kristu anauka,

Hymn 64 LERO Kristu anauka,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 64 LERO Kristu anauka,

 

LERO Kristu anauka,
Aleluya.
Ndilo tsiku lokondwera.
Aleluya.
Iye kale anafera,
Aleluya.
Nawombola otaika,
Aleluya.

Timwimbire zomtamanda
Aleluya.
Ndiye Kristu wa Kumwamba
Aleluya.
Natsikira kumanda,
Aleluya.
Nalanditsa akuipa.
Aleluya

Koma masauko ake,
Aleluya.
Anatiwombola ife.
Aleluya.
Ndiye Mfumu ya mafumu,
Aleluya.
Mwana ndithu wa Mulungu.
Aleluya.

Timwimbire Mulungu wathu,
Aleluya.
Kuti atikonda ndithu:
Aleluya.
Mtamenso angelo inu,
Aleluya.
Ndiye ‘Tate, Mwana, Mzimu
Aleluya.

Post navigation

Previous: Hymn 63 POKUMBUKIRA mtandawo
Next: Hymn 65 NLA Mlungu dzuŵali:

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 168 NDINGANENE malilime,
  • Hymn 201 Ngati zakuipa zathu
  • Hymn 341 PAKUPEMPHERATU
  • Hymn 1742 Yesu ndinu moyo wathu,
  • Hymn 1430 Ndipo pakulowa
  • Hymn 449 Mzimu wakuipa
  • Hymn 475 MZINDA woyerawo
  • Hymn 435 ANAKWATIRA kale
  • Hymn 1104 Mndisungire mtima wanga,
  • Hymn 844 Pogona ife, amadzuka
  • Hymn 1460 Akuti anthu akumvera
  • Hymn 326 Yesu, Bwenzi la ochimwa,
  • Hymn 1326 A! Mbusa wathu amvatu
  • Hymn 1347 Akukonda, akukonda,
  • Hymn 20 CHIKONDI cha Mulungu wathu,
  • Hymn 468 Ife tikondana nanu,
  • Hymn 77 MMENE Yesu adzabwera,
  • Hymn 1824 Mulungu wathu Mmodzi yekha
  • Hymn 899 ‘Tate wa Kumwambako,
  • Hymn 937 Chitsime chachikondi
  • Hymn 295 AMBUYE wa Kumwamba,
  • Hymn 1311 Pothawira pena ‘yi,
  • Hymn 872 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 63 POKUMBUKIRA mtandawo
  • Hymn 1775 Oonadi mtima,
  • Hymn 395 Usiku uno mutisungedi,
  • Hymn 821 Aleluya!
  • Hymn 1118 Ndifuna Inu Yesu,
  • Hymn 1723 Unakhetsedwa mwazi do!
  • Hymn 490 YESU adza kuwerenga,
  • Hymn 194 AMBUYE’naitan’ne;
  • Hymn 1013 Tizifesa m’dzuwa,
  • Hymn 399 Tchimo lathu lonse, Yesu,
  • Hymn 480 TIANA ife tingofoka,
  • Hymn 1378 Tsopano linoli
  • Hymn 459 Aphunzitse anthuwo,
  • Hymn 1766 Ndilikulemekeza
  • Hymn 1816 Anatikondakonda ‘Ye,
  • Hymn 416 PALIBE wina Kumwamba,
  • Hymn 193 A! Kumwamba
  • Hymn 281 MBUYE, mwatiuza ’fe
  • Hymn 390 Lalowa dzuwa, kwada bii!
  • Hymn 74 Ndipereka zanga zonse
  • Hymn 277 Mbwere nonse muone
  • Hymn 611 Tidzakhala naye nthawi zonse ndi kuimbako,
  • Hymn 1184 Akondwerera nthawiyi
  • Hymn 1106 Mlungu ndi wachikhalire.
  • Hymn 179 Ndinachimwa poganiza
  • Hymn 35 Zonse za m’dziko zidzatha,
  • Hymn 311 VALANI zida tizinka kwathuko,
  • Hymn 1554 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 1334 Walandira inetu
  • Hymn 400 Dzuwa liwala, m’tulotu
  • Hymn 1835 Mtima wanga lemekeza
  • Hymn 30 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 558 Mwanayo wa Mulunguyo
  • Hymn 512 ‘Natipulumutsa
  • Hymn 96 MTIMA wanga uyamiketu,
  • Hymn 1810 Kalelo Mbuye Yesu
  • Hymn 466 OSANATU, osana,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version