Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 61 A! MUTU wakuyera,

  1. Home   »  
  2. Hymn 61 A! MUTU wakuyera,

Hymn 61 A! MUTU wakuyera,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 61 A! MUTU wakuyera,

 

A! MUTU wakuyera,
Wolaswa wachisoni,
Abveka Inu anthu
Ndi minga ya udani;
Ambuye mwafokatu
Ndi masauko aja,
Mwatuŵa m’maso mwanu
Mumayerera kale.

Ambuye Mwini moyo,
Kokoma mnafumako;
Ndizizwa pomva mawu
Umo mwachitiramo.
Chisoni chija chanu
Ncha pamachimo anga,
Mwasaukira Inu
Kupalamula kwanga.

Nditani! Bwezi langa
Kulemekeza Inu
Chifukwa cha chifundo
Ndi imfa ija yanu?
Mundikhalitse wanu,
Wokhulupira inu;
Musandilole konse
Kufulatira Inu.

Pakufa ine Mbuye
Mukhaletu pafupi,
Mundithandize ine,
E, mudzandimasula;
Ndipenyetsetsa Yesu,
Ambuye Mfumu yanga,
Ndikafa ndine wanu,
Ndikhale nanu m’Mwamba.

Post navigation

Previous: Hymn 60 ZATHEDWA zonsetu
Next: Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 404 Dzuwa la lero lonseli
  • Hymn 888 Polowa ndi Inu
  • Hymn 660 Tumizani kuunikako,
  • Hymn 306 Ona Mwanawanakhosayo
  • Hymn 1115 M’munda wa Mbuyako
  • Hymn 452 MLUNGU, Inutu,
  • Hymn 1771 Iye natsitsa kunsi
  • Hymn 1426 Wina panalibe
  • Hymn 334 KULI dziko labwino M’mwamba,
  • Hymn 1509 Mkate wamoyowo
  • Hymn 401 A MULUNGU,
  • Hymn 478 YESU atiuza tiŵale ’fe.
  • Hymn 1596 Anamnyoza pansi pano,
  • Hymn 76 Ndipereka zanga zonse
  • Hymn 1288 Yesu mundimve, ndikuliratu,
  • Hymn 1637 Tisaleke kugwirabe
  • Hymn 147 MUSAŴALOLE mawuwo
  • Hymn 1616 Anafera
  • Hymn 879 Zokoma etu nthawizi”
  • Hymn 473 YESU wa Kumwamba,
  • Hymn 343 Auke,
  • Hymn 420 Mtima umabisala
  • Hymn 1181 Adalitsika munthuyo
  • Hymn 1400 Tulani zoipazi, idzanitu,
  • Hymn 1672 Lambira Mfumuyo,
  • Hymn 1225 Ndinachita mphulupulu,
  • Hymn 662 Tisaleme pakuchita zabwinozi,
  • Hymn 402 M’mtima mwangamu mlowemo,
  • Hymn 485 POMPANO pandikonda
  • Hymn 450 Koma usalole
  • Hymn 206 YESU, mulikundipempha
  • Hymn 891 Akakusowa malo
  • Hymn 187 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 317 Zambiri zagona m’kholamo,
  • Hymn 1333 Idzatu kwa Yesuyo,
  • Hymn 1287 Wadza Yesu wandidzoza,
  • Hymn 1039 Usafune chuma chokha,
  • Hymn 1241 Ati: Mwana, kumbukira
  • Hymn 359 Tonse timyamiketu,
  • Hymn 436 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 292 NDIPULUMUTSENI Mbuye,
  • Hymn 388 Ambuye, Mzimu wanu
  • Hymn 398 Lero lino mwatipatsa
  • Hymn 894 Mbuye, ndinu Mfumu yanga
  • Hymn 1622 Anthu onse amlambire
  • Hymn 1072 Mudzaze Yesu mtima wanga ndi chikondicho,
  • Hymn 637 Mbuyathu wokondedwa,
  • Hymn 446 Yesu alandira
  • Hymn 1586 Mbuye Yesu timtamanda
  • Hymn 209 M’NDILANDIRE ine Mbuye
  • Hymn 1840 Ndiye M’busa wanga,
  • Hymn 483 Ndife akuchoka,
  • Hymn 97 TIYAMIKE Mlunguyo,
  • Hymn 230 Ndisamba ndiyera,
  • Hymn 106 MZIMU Woyera, mudzetu,
  • Hymn 1765 Zoonazi amithenga
  • Hymn 1526 Mbuye wondipulumutsa
  • Hymn 1141 Pakulekana ifetu
  • Hymn 701 Inu Atatuwo,
  • Hymn 1020 Ngati umtsata Mpulumutsi wakoyo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version