Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 61 A! MUTU wakuyera,

  1. Home   »  
  2. Hymn 61 A! MUTU wakuyera,

Hymn 61 A! MUTU wakuyera,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 61 A! MUTU wakuyera,

 

A! MUTU wakuyera,
Wolaswa wachisoni,
Abveka Inu anthu
Ndi minga ya udani;
Ambuye mwafokatu
Ndi masauko aja,
Mwatuŵa m’maso mwanu
Mumayerera kale.

Ambuye Mwini moyo,
Kokoma mnafumako;
Ndizizwa pomva mawu
Umo mwachitiramo.
Chisoni chija chanu
Ncha pamachimo anga,
Mwasaukira Inu
Kupalamula kwanga.

Nditani! Bwezi langa
Kulemekeza Inu
Chifukwa cha chifundo
Ndi imfa ija yanu?
Mundikhalitse wanu,
Wokhulupira inu;
Musandilole konse
Kufulatira Inu.

Pakufa ine Mbuye
Mukhaletu pafupi,
Mundithandize ine,
E, mudzandimasula;
Ndipenyetsetsa Yesu,
Ambuye Mfumu yanga,
Ndikafa ndine wanu,
Ndikhale nanu m’Mwamba.

Post navigation

Previous: Hymn 60 ZATHEDWA zonsetu
Next: Hymn 62 AMBUYE Yesu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 179 TUMPHATUMPHA moyo wanga,
  • Hymn 423 MUNENE Mbuye, ’nenetu,
  • Hymn 1329 M’tali mutali m’phirimo
  • Hymn 326 TSIKU Iidzafika mbale,
  • Hymn 143 KONZA mtima iwe mbale,
  • Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe
  • Hymn 707 Dalitseni, Mbuye, zonse
  • Hymn 267 AMBUYE, thandizenitu
  • Hymn 200 YESU mundimve, ndikuliratu,
  • Hymn 2 YEHOVA Mthandizi,
  • Hymn 211 TIDZALAKALAKA kuwonana naye,
  • Hymn 482 TCHIMO musalole, musadziipitse,
  • Hymn 87 IDZANI nonse ’nu
  • Hymn 115 Mbulu wanding’amba m’nthiti,
  • Hymn 1471 Ukapenya kwa Yesu uliko moyoko,
  • Hymn 544 Zoopsya sitidziwapo
  • Hymn 1454 Ambuye, musendeze
  • Hymn 92 Ufuna kugwira ntchito yake?
  • Hymn 1023 Kodi m’njiramo ndimvadi
  • Hymn 1473 Anasenza pa bwanji uchimo wonsewo,
  • Hymn 502 Ndikonda mbiri yomwe
  • Hymn 1417 Atate ‘nu, atate ‘nu,
  • Hymn 304 POZUNZIDWA inu ponseponse
  • Hymn 1233 Tsopano ndibukitsabe chikondi chanu chija
  • Hymn 719 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 1432 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 127 Mwazi wake ndi chitsime changa,
  • Hymn 121 Imbira!
  • Hymn 1840 Ndiye M’busa wanga,
  • Hymn 1240 Ndilikuva m’mtima mwanga
  • Hymn 237 Munasiyatu
  • Hymn 982 Tiyeni Akristu,
  • Hymn 852 Munkhani zako zonsetu
  • Hymn 740 Tsopano nthawi yake phwandili,
  • Hymn 397 Yesu Mbusa, mutimvere,
  • Hymn 1212 Zina ndi zinanso
  • Hymn 73 Mu ulemerero tidzakhala m’yaya,
  • Hymn 1093 Odala ndi onsewo
  • Hymn 1331 Yesu wathu Mbuyeyo
  • Hymn 1834 Chisomo ndi zokoma zake sizileka konse;
  • Hymn 1685 Nla Mlungu dzuwali;
  • Hymn 142 Kukondwa kwa wodwalayo
  • Hymn 74 IDZA wolema,
  • Hymn 1305 Ndi ine pondibvutapo
  • Hymn 1788 Mtimanga, bwera kuti upumule
  • Hymn 1341 Tadza kukudyaku,
  • Hymn 1655 Mbuye Yesu,
  • Hymn 1616 Anafera
  • Hymn 1714 Tiyeni, dzalireni nane,
  • Hymn 13 Mtiwerengere m’Mwamba ndi oyera;
  • Hymn 687 Bukitsani mawunso
  • Hymn 334 Tsugulani mtima wanu
  • Hymn 258 MWA ine, moyo wanga ndi Yesu
  • Hymn 1635 Pakwitana Mbuye wanga,
  • Hymn 1712 E! Yesu Mbuye wangadi,
  • Hymn 1214 Mwamva Mzimu wakewo,
  • Hymn 188 Ine ndili ndi manyazi
  • Hymn 377 Yehova, Mbusa wangadi,
  • Hymn 109 MUTHIRE, Yesu, m’mtimanga
  • Hymn 210 Nyumba yodyera ilikudzaza;

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version