Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 5 ATATE wa Kumwambako,

  1. Home   »  
  2. Hymn 5 ATATE wa Kumwambako,

Hymn 5 ATATE wa Kumwambako,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 5 ATATE wa Kumwambako,

 

ATATE wa Kumwambako,
Munawombola ife, ndi
Chikondi chanu chijacho;
Tiyamikira Inutu.

Ambuye Yesu Inutu,
Munabadwira anthu ’fe;
Munatifera tonse ’fe;
Tiyamikira Inutu.

Mzimu Woyera m’mtimamo
Tiyeretsedwe ndi Inutu;
Munatisunga bwinoli,
Tiyamikira Inutu.

Atate, Mwana, Mzimunso,
Ndinu Atatu, Mmodzitu
Ochimwa tikupemphani:
Mutikhululukire’fe

Post navigation

Previous: Hymn 1858 Ha! Chikondi cha Mulungu,
Next: Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1025 Ndikamayenda m’mdimamo,
  • Hymn 355 Tinafuna m’phirimo,
  • Hymn 1333 Idzatu kwa Yesuyo,
  • Hymn 1027 Tithawiranji ifetu?
  • Hymn 353 ATATE Wamkulu ndi Wamphamvu zonse,
  • Hymn 218 NDIPEREKA zanga zonse
  • Hymn 811 Wopulumutsa mudzetu;
  • Hymn 578 Falitsani mbiriyi,
  • Hymn 65 NLA Mlungu dzuŵali:
  • Hymn 1700 Ambuye Mwini moyo,
  • Hymn 129 WODALA ndiye munthuyo,
  • Hymn 767 Munali mwana, Yesu ‘Nu
  • Hymn 1383 Dzina lake tibukitsa,
  • Hymn 1788 Mtimanga, bwera kuti upumule
  • Hymn 182 YESU watidzera, watidzera,
  • Hymn 1613 A Mulungu
  • Hymn 1172 Adzabweranso
  • Hymn 1198 Mabala ake m’manja
  • Hymn 253 YESU ndinutu wanga m’njira zonse,
  • Hymn 944 Tiyeni nonsenu okonda Yesuyo,
  • Hymn 104 MUBWERE Mzimu Inu
  • Hymn 131 MAWU a Mulungu awa,
  • Hymn 980 Tiyeni ku nkhondo iyi,
  • Hymn 988 Ndikhumba Mzimu wanu
  • Hymn 223 Ndafoka, ndaipa,
  • Hymn 730 A! Yesu mwapangana
  • Hymn 1849 Nthawi zonse monga ‘Tate
  • Hymn 89 INDE, ndifuna kumvatu,
  • Hymn 585 Alanditsa,
  • Hymn 581 Mtiphunzitse bwinotu,
  • Hymn 301 Mwanawankhosa
  • Hymn 497 TILIKUIMBA nyimbo yomweyi,
  • Hymn 407 ADZAPAMBANA Yesu ponse
  • Hymn 1235 Yesu wathadi
  • Hymn 117 Atate wondipatsazo,
  • Hymn 533 Ananu, ziimbani,
  • Hymn 975 Tiyeni, Akristu inu,
  • Hymn 976 Muyendenso kunka komwe,
  • Hymn 1670 Bwenzi ndiye wakufera,
  • Hymn 1522 Tikaona bvuto,
  • Hymn 1568 Kudzoza kwanu kutipatsa
  • Hymn 244 TIMVE za anamwali khumi,
  • Hymn 1839 Yehova ndiye Mbusa wanga sin’ngasowe konse;
  • Hymn 1435 Ndiwe mlendo lero lino,
  • Hymn 276 MKRISTU, ulimbike
  • Hymn 1750 Ndi nyali yakuwalitsa
  • Hymn 102 Mzimu ndi mtsogoleri
  • Hymn 1050 Ndafoka inetu,
  • Hymn 1074 Mubweretu nomwe ‘Nu munatsika kalelo;
  • Hymn 559 Usikuwo woyerawo!
  • Hymn 493 Ndimalira kwa Inutu,
  • Hymn 143 Lero lino Mbuye Yesu
  • Hymn 567 M’nyumba zonse ponseponse
  • Hymn 348 CHIKHULUPIRIRO chathu
  • Hymn 1336 Mwamva mawu a Mulungu;
  • Hymn 709 Munthu aganize
  • Hymn 1384 Mphamvu yake inalenga
  • Hymn 114 Ndine Mbusayo wabwino,
  • Hymn 76 E, MOYO wanga’we
  • Hymn 1064 Moyowo

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version