Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 438 TIYAMIKE Ambuye,

  1. Home   »  
  2. Hymn 438 TIYAMIKE Ambuye,

Hymn 438 TIYAMIKE Ambuye,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 438 TIYAMIKE Ambuye,

 

TIYAMIKE Ambuye,
Chifukwa chotilola,
Kulowa m’chaka chino m’tisunge;
Sitingathe ‘fe tokha,
Kuyenda m’chaka chonse;
Ambuye m’titsogoze,
M’tisunge.

M’tisunge, m’tisunge,
Yesu tikupemphani m’tisunge;
Ife timalephera kuyenda m’njira tokha;
Yesu tikupemphani m’tisunge.

Dziko lapansi pano timangoyenda chabe,
Wosaganiziranso za moyo;
Timaganiza kuti moyowu sudzathanso,
Ambuye m’tikumbutse leroli.

Moyowu ngwapafupi, monga kugwa kwa tsamba,
Monga kumanga mtolo m’tisunge;
Ambuye m’tidalitse,
Nthawi isanafike;
Kuti tingataike m’tisunge.

Post navigation

Previous: Hymn 437 MULUNGU wa Yakobo Inu, mdyetsa anthu anu,
Next: Hymn 439 MLUNGU wathu mwatifitsa

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1103 Ndakudani, mnandikonda
  • Hymn 101 Lodala tsiku lomwelo
  • Hymn 368 MULUNGU wanga, Dzuŵatu
  • Hymn 1180 Ndine kapolo wa Mbuye wanga;
  • Hymn 1279 Kuti munditsogolera paulendopo;
  • Hymn 1579 Akhala mafumu
  • Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda
  • Hymn 528 Amithenga ‘naimba pamlengapo,
  • Hymn 566 Ana inu, ana inu,
  • Hymn 204 Kumandako, kumanda
  • Hymn 454 TAONANI, m’kholamo,
  • Hymn 655 Ndiphunzitseni, Mbuyetu,
  • Hymn 128 ANTHU m’maiko onse
  • Hymn 1335 Wandifera Yesuyo
  • Hymn 309 Mwa Mzimu mulowe mumitima yathu,
  • Hymn 1717 Mtima wangawe, uyenera
  • Hymn 478 YESU atiuza tiŵale ’fe.
  • Hymn 875 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 438 TIYAMIKE Ambuye,
  • Hymn 1160 Ndinakhala wakuipa,
  • Hymn 386 MONGATU mawu anuwo,
  • Hymn 410 Ana ake angonga
  • Hymn 687 Bukitsani mawunso
  • Hymn 427 AULENDO amayenda
  • Hymn 369 Lowani m’nyumba mwakemu
  • Hymn 885 Mndimvetse chisoni
  • Hymn 57 TIYENI, dzalireni nane,
  • Hymn 91 NDITAME Mlungu m’mtimamo,
  • Hymn 903 Iwo salekana, iwo salekana,
  • Hymn 332 NDIKONDWA kuganizirabe
  • Hymn 978 Mtima wanu wonse ndithu
  • Hymn 1565 Mufike monga ngati njiwa yamtenderewo,
  • Hymn 1102 Dziko lonse ndilitaya;
  • Hymn 645 Kristu ndiye mwala wathu,
  • Hymn 646 Mudalitse nyumba yathu;
  • Hymn 1153 Mtendere uli m’mtima mwathumu,
  • Hymn 464 AKAZI anadza kwa Yesu ndi anawo,
  • Hymn 499 ‘Nafera Mbuye wanga
  • Hymn 127 Mwazi wake ndi chitsime changa,
  • Hymn 273 Mlungu akuyang’aniredi
  • Hymn 1479 Ndi Yesu yemwe kalelo
  • Hymn 1827 Abramu kalelo anamvera bwino;
  • Hymn 1821 Angelo amazinga nyumba
  • Hymn 747 Tadzanitu, okhulupiradi,
  • Hymn 248 Pena pakufadi,
  • Hymn 380 Ndipyola kodi chikhwawa
  • Hymn 814 Mutichiritse ifenso
  • Hymn 264 KHALATU woyera, pempheratu m’tseri;
  • Hymn 102 Mzimu ndi mtsogoleri
  • Hymn 1322 Ntchito zanga zonsezo
  • Hymn 1403 ‘Mvani liwu lomwe
  • Hymn 935 Mtima ukachita nkhawa
  • Hymn 49 Ndi ife akudziwa
  • Hymn 963 Aulendo, munka kuti
  • Hymn 267 AMBUYE, thandizenitu
  • Hymn 14 MTIMA wanga uyamike,
  • Hymn 1633 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 752 Chakudya chakumwambachi
  • Hymn 1603 Zina za Yesu m;Mwambamo,
  • Hymn 1430 Ndipo pakulowa

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version