Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 438 TIYAMIKE Ambuye,

  1. Home   »  
  2. Hymn 438 TIYAMIKE Ambuye,

Hymn 438 TIYAMIKE Ambuye,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 438 TIYAMIKE Ambuye,

 

TIYAMIKE Ambuye,
Chifukwa chotilola,
Kulowa m’chaka chino m’tisunge;
Sitingathe ‘fe tokha,
Kuyenda m’chaka chonse;
Ambuye m’titsogoze,
M’tisunge.

M’tisunge, m’tisunge,
Yesu tikupemphani m’tisunge;
Ife timalephera kuyenda m’njira tokha;
Yesu tikupemphani m’tisunge.

Dziko lapansi pano timangoyenda chabe,
Wosaganiziranso za moyo;
Timaganiza kuti moyowu sudzathanso,
Ambuye m’tikumbutse leroli.

Moyowu ngwapafupi, monga kugwa kwa tsamba,
Monga kumanga mtolo m’tisunge;
Ambuye m’tidalitse,
Nthawi isanafike;
Kuti tingataike m’tisunge.

Post navigation

Previous: Hymn 420 FESANI mbewuzo,
Next: Hymn 441 MBUYE, tikuthokozani,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 722 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 996 Leka zakuipa zako,
  • Hymn 871 Tiphatikane tonsefe okonda Yesu Kristu;
  • Hymn 290 NAMONDWE wawuka,
  • Hymn 538 Iye anachoka kwawo,
  • Hymn 1603 Zina za Yesu m;Mwambamo,
  • Hymn 1555 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 14 MTIMA wanga uyamike,
  • Hymn 1714 Tiyeni, dzalireni nane,
  • Hymn 1790 Imfa ya anthu ake imkomera,
  • Hymn 795 Sitinanyalanyalaza
  • Hymn 67 PAMENEPO pokhala madzulo,
  • Hymn 107 MUBWERE kuno Mzimu ’Nu
  • Hymn 1740 Yesu, ndi chifundo chanu
  • Hymn 34 Yesu Mbuyetu, mwafera
  • Hymn 1610 Waleka koronayo,
  • Hymn 826 Mutonthoze mtima
  • Hymn 267 Usekere moyo wanga,
  • Hymn 1314 Mulungu ali nane!
  • Hymn 728 A! Yesu, ndapangana
  • Hymn 275 Mlungu akuyang’aniredi,
  • Hymn 1281 Ndikhulupirira, Yesu, mndibvomereko;
  • Hymn 277 Mbwere nonse muone
  • Hymn 171 M’manda munalibe
  • Hymn 1104 Mndisungire mtima wanga,
  • Hymn 475 MZINDA woyerawo
  • Hymn 860 Nthawi yina adzadzuka
  • Hymn 73 Mu ulemerero tidzakhala m’yaya,
  • Hymn 1777 Mulungu wamkulu
  • Hymn 1828 Timtamande Iye ndi moyo wathunso
  • Hymn 351 CHIYEMBEKEZO changacho,
  • Hymn 439 Nthawi yaubwana yatha,
  • Hymn 532 Ukondwere mtima wanga
  • Hymn 220 Kalekale ndinathawa,
  • Hymn 1614 Anabadwa,
  • Hymn 1519 M’Buku lakuyerali
  • Hymn 1235 Yesu wathadi
  • Hymn 374 NDI lokoma m’Mwambamo,
  • Hymn 452 MLUNGU, Inutu,
  • Hymn 1135 Mulungu anditsogolera,
  • Hymn 34 AMITHENGA a Mulungu,
  • Hymn 865 Pakubweradi Woyesa tidzamlaka ifetu;
  • Hymn 182 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 585 Alanditsa,
  • Hymn 898 Mndidziwitse ntchito yanga,
  • Hymn 181 Zonse ndinakonda kale
  • Hymn 88 Ufuna kuwomboledwa kodi?
  • Hymn 708 Peturo ‘nafusa Hananiya:
  • Hymn 1404 “Undipatsetu
  • Hymn 833 Mundilimbitse ndikayese manda ngati mphasayi,
  • Hymn 128 Yesu Mfumu, ine ndingadzafe
  • Hymn 762 “Ndi thupi lopatsidwali
  • Hymn 695 Pomveka konsekonse mbiri
  • Hymn 78 Ndipereka zanga zonse,
  • Hymn 454 TAONANI, m’kholamo,
  • Hymn 442 Posachedwa tilekana
  • Hymn 1040 Ukafuna kulemera,
  • Hymn 1198 Mabala ake m’manja
  • Hymn 1005 Mdani adza nazo mphamvu,
  • Hymn 1767 Ndiye anayang’ana

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version