Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 428 MBUYE mtsitsimutse

  1. Home   »  
  2. Hymn 428 MBUYE mtsitsimutse

Hymn 428 MBUYE mtsitsimutse

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 428 MBUYE mtsitsimutse

 

MBUYE mtsitsimutse
Ntchito zonse zanu!
Utsani anthu akufa
Ndi mawu a mphamvu.

Mbuye mtsitsimutse
Ntchito zonse zanu!
Tauzirani pa ife
Ndi mweya wa Mzimu

Mbuye mtsitsimutse
Ntchito m’mitimamo!
Mumvetse njala kwa Inu—
Mutikhutitsenso.

Mbuye mtsitsimutse
Ntchito m’kati mwa anthu!
Chikondi chawo chikule
Muchikolezetu.

Mbuye mtsitsimutse!
Mawu alimbike,
Pamene aphunzitsidwa
Onsewa amvere!

Mbuye mtsitsimutse!
Mzimu adzazetu!
Kwa ife kudzakhala mwayi,
Kwa Inu ulemu.

Post navigation

Previous: Hymn 420 FESANI mbewuzo,
Next: Hymn 441 MBUYE, tikuthokozani,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 809 Madzulo aja kalelo
  • Hymn 937 Chitsime chachikondi
  • Hymn 346 Aitana,
  • Hymn 1268 Mundilandiretu,
  • Hymn 1856 Mzimu, msandipitirire,
  • Hymn 699 Inu wakudzatu
  • Hymn 378 KWEZANI mitu yanuyo,
  • Hymn 369 Lowani m’nyumba mwakemu
  • Hymn 131 MAWU a Mulungu awa,
  • Hymn 227 Kasupe ali wodzaza
  • Hymn 1508 Mundinyemere ‘ne
  • Hymn 1440 Yesu alindira,
  • Hymn 1775 Oonadi mtima,
  • Hymn 86 IYE wokhulupilira Yesu,
  • Hymn 16 MTIMA wanga lemekeza,
  • Hymn 988 Ndikhumba Mzimu wanu
  • Hymn 556 Ndani pachimpandocho
  • Hymn 879 Zokoma etu nthawizi”
  • Hymn 170 M’manda naukamo
  • Hymn 89 INDE, ndifuna kumvatu,
  • Hymn 1473 Anasenza pa bwanji uchimo wonsewo,
  • Hymn 966 Kodi inu, aulendo,
  • Hymn 22 Mbuye mtsitsimutse!
  • Hymn 278 TITHAŴIRENJI ifetu
  • Hymn 1719 Ku Mzinda wakuyerawo
  • Hymn 178 ZAMBIRI zogona m’kholamo,
  • Hymn 1142 Tidzathawira kuti ‘fe
  • Hymn 299 “Posunga nkhosa ife
  • Hymn 343 Auke,
  • Hymn 196 NDI inetu sinditha’yi
  • Hymn 316 NDAMVATU kuti tifika komweko
  • Hymn 901 Musatifikitsemo
  • Hymn 840 Ambuye munapatsa tsiku
  • Hymn 119 M’BUKU la moyotu Mbuye,
  • Hymn 1039 Usafune chuma chokha,
  • Hymn 1667 Yesu wakukoma mtima,
  • Hymn 1161 Wapumitsa mtima wanga,
  • Hymn 1475 Anathera pamtanda zintchito zonsezi
  • Hymn 366 MADZULO aja kalero
  • Hymn 1433 Lero lino ndi labwino;
  • Hymn 735 Mwa chikho chokumbutsa
  • Hymn 500 Mbuye Yesu andisunga
  • Hymn 58 PAMTANDAPO Ambuyeyo
  • Hymn 1706 Pamutu minga kwe!
  • Hymn 1614 Anabadwa,
  • Hymn 497 Yesu andikonda ine,
  • Hymn 711 Ife tonse tichenjere
  • Hymn 335 KWATHU sipadziko, ndingopitilira,
  • Hymn 470 Mutiletse tisaname
  • Hymn 1020 Ngati umtsata Mpulumutsi wakoyo,
  • Hymn 306 Ona Mwanawanakhosayo
  • Hymn 167 KODI mwalandira Yesu?
  • Hymn 943 Onse aliko takonda kalelo,
  • Hymn 417 M’BWERE Mlungu Mbuye wathu,
  • Hymn 1546 Mubwere Mzimu Inu
  • Hymn 196 Tidzimba komweko nyimbo
  • Hymn 486 MPULUMUTSI Yesu,
  • Hymn 1277 Kuti mukhululukira tchimo langalo
  • Hymn 1390 Nditamatu Ambuyangayu,
  • Hymn 557 Usikuwo woyerawo!

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version