Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 428 MBUYE mtsitsimutse

  1. Home   »  
  2. Hymn 428 MBUYE mtsitsimutse

Hymn 428 MBUYE mtsitsimutse

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 428 MBUYE mtsitsimutse

 

MBUYE mtsitsimutse
Ntchito zonse zanu!
Utsani anthu akufa
Ndi mawu a mphamvu.

Mbuye mtsitsimutse
Ntchito zonse zanu!
Tauzirani pa ife
Ndi mweya wa Mzimu

Mbuye mtsitsimutse
Ntchito m’mitimamo!
Mumvetse njala kwa Inu—
Mutikhutitsenso.

Mbuye mtsitsimutse
Ntchito m’kati mwa anthu!
Chikondi chawo chikule
Muchikolezetu.

Mbuye mtsitsimutse!
Mawu alimbike,
Pamene aphunzitsidwa
Onsewa amvere!

Mbuye mtsitsimutse!
Mzimu adzazetu!
Kwa ife kudzakhala mwayi,
Kwa Inu ulemu.

Post navigation

Previous: Hymn 427 AULENDO amayenda
Next: Hymn 429 M’DZANJA lanu Ambuye,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1235 Yesu wathadi
  • Hymn 1032 Ntchito za Yesu gwira
  • Hymn 1129 Mbuyanga Yesu, ndikapanda Inu
  • Hymn 1721 Mapazi ake namvatu
  • Hymn 834 Tiyamike Mlungu wotipatsa zachifundozi,
  • Hymn 1186 Yesu anafa pamtandapo,
  • Hymn 817 Tibvomereze,
  • Hymn 147 MUSAŴALOLE mawuwo
  • Hymn 835 Mukhale ndine, dzuwalo lalowa,
  • Hymn 391 Mufafanize m’bukumo
  • Hymn 247 Tsono poukanso
  • Hymn 1452 Inu akutopawo,
  • Hymn 1037 Mapemphero athu
  • Hymn 1157 Mtendere wapambana m’Mwambamo
  • Hymn 1370 Mphepo yay’kulu yakuombayo,
  • Hymn 1830 Ndiye M’busa wanga
  • Hymn 1241 Ati: Mwana, kumbukira
  • Hymn 207 Malo alimo m’nyumba ya Yesu,
  • Hymn 909 Ife tikondwera, ife tikondwera,
  • Hymn 1787 Mulungu wanga ndiye wachifundo
  • Hymn 151 UKAPENYA kwa Yesu uliko moyoko,
  • Hymn 466 OSANATU, osana,
  • Hymn 724 Ndine mlendo pansi pano,
  • Hymn 1388 Tiimbire Mlungu wathu
  • Hymn 836 Kamoyo kanga katha lero lino,
  • Hymn 368 MULUNGU wanga, Dzuŵatu
  • Hymn 422 DZIKO lonse lapansi,
  • Hymn 846 Kristu wakuyeratu,
  • Hymn 609 Zanu zapansi nzokoma Mbuye; tikondwera ‘fe,
  • Hymn 90 WINA atikonda ife,
  • Hymn 924 Kodi uli ndi chisoni
  • Hymn 211 Chakudya ichi ndi cha iwenso,
  • Hymn 470 YESU andikonda ine,
  • Hymn 688 Anthu akum’mawa
  • Hymn 720 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 1302 Ndi inetu sinditha ‘yi
  • Hymn 1708 Pakugomedwapo
  • Hymn 1006 Yesu ati, “Ndidza msanga!”
  • Hymn 1088 Mndiyandikitse nanu, Yesu,
  • Hymn 380 Ndipyola kodi chikhwawa
  • Hymn 1717 Mtima wangawe, uyenera
  • Hymn 1771 Iye natsitsa kunsi
  • Hymn 165 Yendanitu m’ulemudi,
  • Hymn 960 Tilikupita kwathu kuja
  • Hymn 1122 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 13 Mtiwerengere m’Mwamba ndi oyera;
  • Hymn 1125 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 99 Tsopano ndimwona Iye
  • Hymn 1008 Wakuchezacheza naye
  • Hymn 854 Timlemekeze Mlunguyu
  • Hymn 276 MKRISTU, ulimbike
  • Hymn 490 Yesu, ndikabwera
  • Hymn 1565 Mufike monga ngati njiwa yamtenderewo,
  • Hymn 157 INU nonse ovutidwa,
  • Hymn 464 AKAZI anadza kwa Yesu ndi anawo,
  • Hymn 92 Ufuna kugwira ntchito yake?
  • Hymn 694 Sadalekeza kuyamika
  • Hymn 280 Tisonkhane tonsefe,
  • Hymn 64 Mantha, nkhawa, ndi chisoni
  • Hymn 14 Tsiku ndi tsiku timalemekeza;

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version