Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 422 DZIKO lonse lapansi,

  1. Home   »  
  2. Hymn 422 DZIKO lonse lapansi,

Hymn 422 DZIKO lonse lapansi,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 422 DZIKO lonse lapansi,

 

DZIKO lonse lapansi,
Linachimwa kwa Mlungu,
Chilango chake ndicho cha imfa;
Koma podza Yesuyo,
Anathetsa mlanduwo;
Potifera ife pamtandapo.

Onani,
Mwana wa Nkhosa,
Wachotsa tchimo lonse pansipa;
Ndiye Yesu Mfumuyo,
Ndiye Mpulumutsiyo;
Wotifera ife pamtandapo.

Tsono mmene tadziwa,
Kuti ndife ochimwa,
Tiyeni tinke kwa Ambuyewo;
Tisachite manyazi,
Tiwauze tchimolo;
Iwo adzatikhululukira.

Wotikhululukira,
Adzatiwuza tonse,
Kuti tisadzachimwenso ndithu;
Zakale zatha ndithu,
Zatsala zatsopano;
Tasamba mwazi wake tayera.

Post navigation

Previous: Hymn 420 FESANI mbewuzo,
Next: Hymn 441 MBUYE, tikuthokozani,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 308 AULENDO, munka kuti
  • Hymn 384 USIKU uja kalero,
  • Hymn 1612 Adzadza indetu
  • Hymn 346 Aitana,
  • Hymn 766 Monga zomera zonsezo
  • Hymn 1818 Kuzani Mlungu m’Mwambamo
  • Hymn 936 Ukatha moyo wanga
  • Hymn 12 NDITAMATU Ambuyangayu,
  • Hymn 806 Kapena wina leroli
  • Hymn 1511 Mndidalitsere ‘ne
  • Hymn 415 PAMAYIKO pali mdima,
  • Hymn 458 USIKUWO, woyerawo!
  • Hymn 404 Dzuwa la lero lonseli
  • Hymn 617 Nthawi yina Mbuyeyu
  • Hymn 6 Nanu akukuzani amithenga,
  • Hymn 378 Ku madzi ake odikha
  • Hymn 1 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 1137 Masiku ena pali mdima,
  • Hymn 66 Chisomocho chachotsadi
  • Hymn 872 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,
  • Hymn 1693 Koma masauko ake Aleluya
  • Hymn 1474 Zilepheradi zonse kugula moyowo,
  • Hymn 1569 Mtima wodetsa mukonzere,
  • Hymn 899 ‘Tate wa Kumwambako,
  • Hymn 31 MULUNGU Wamkulu,
  • Hymn 331 Yesu ndimafuna Inu,
  • Hymn 473 Mzinda woyerawo!
  • Hymn 612 Oyamika Mlungu mbwere,
  • Hymn 875 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 622 Tiyamikira ‘Tate,
  • Hymn 24 “Ndakupeza womanga,
  • Hymn 1772 Iye amakhutitsa
  • Hymn 633 Tikasokera m’njira mutilondolere ndithu,
  • Hymn 62 Tchimo lonse ligonjera
  • Hymn 575 Taonani m’kholamo
  • Hymn 57 Ife tiyembekezera Yesu,
  • Hymn 339 Tipempha,
  • Hymn 257 NJIRA yanga sindiziŵa,
  • Hymn 249 MBUYANGA Yesu, mundigwire
  • Hymn 477 YESU, muli pa chimpando
  • Hymn 318 Ambuye, muli nazo zambirizi,
  • Hymn 78 Ndipereka zanga zonse,
  • Hymn 252 MTIMA wa Mbuyako,
  • Hymn 466 OSANATU, osana,
  • Hymn 379 Anditsogolera m’njira
  • Hymn 281 MBUYE, mwatiuza ’fe
  • Hymn 1158 Yesu ndiye Mbuye wanga,
  • Hymn 201 Ngati zakuipa zathu
  • Hymn 1115 M’munda wa Mbuyako
  • Hymn 985 Zonse zapadziko
  • Hymn 601 Akaona masautso
  • Hymn 1630 Anthu anu amafoka,
  • Hymn 1835 Mtima wanga lemekeza
  • Hymn 415 Tidzalandirabe komwe
  • Hymn 733 Ndimamva ludzu Yesu,
  • Hymn 358 MLUNGU ali muno,
  • Hymn 118 Musaone zobvalazo,
  • Hymn 477 Mpulumutsi, Mbusa wathu,
  • Hymn 986 Tiyeni anzathu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version