Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 416 PALIBE wina Kumwamba,

  1. Home   »  
  2. Hymn 416 PALIBE wina Kumwamba,

Hymn 416 PALIBE wina Kumwamba,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 416 PALIBE wina Kumwamba,

 

PALIBE wina Kumwamba,
Ndinutu Mbuyanga;
Pakati pa mayesero,
Thandizeni Ambuye.

Zonse zam’dziko zidzatha,
Monga Mawu anenera;
Ufumu wanu sudzatha,
Wamuyaya, Wamuyaya.

Palibe wina m’dzikoli,
Ndinutu Mbuyanga;
Pakati pamayesero,
Thandizeni Ambuye.

Nyimbo zonse tidzayimba,
Zanutu Mbuyanga;
Pakati pamayesero,
Thandizeni Ambuye.

Post navigation

Previous: Hymn 400 ONA Mwana wa Nkhosa,
Next: Hymn 421 ANTHU ali m’mdima akuyitanitsa,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1803 Nowayo nayendamo,
  • Hymn 1386 Ndi chifundo atipenya
  • Hymn 153 NDAKUMANA ndi bwenzi lokomalo,
  • Hymn 1780 Titame Mlungu Wakumwamba,
  • Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 123 MULI ndi ludzu, idzani
  • Hymn 1187 M’mitima mwathu mwakhala mbee!
  • Hymn 193 A! Kumwamba
  • Hymn 214 KUNALI munthu ku Yeriko,
  • Hymn 712 Mulungu akondadi leroli
  • Hymn 423 Koma azibvala
  • Hymn 1230 Lichiza mzimu wophwetekwa ukakhale bata,
  • Hymn 1493 Mbiri yakalelomwe
  • Hymn 1042 Zonse umazinyadira
  • Hymn 1124 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 1236 Mbuye ndimva leroli
  • Hymn 350 MBUYE ndayima pano,
  • Hymn 135 Kudziwa ukudziwa,
  • Hymn 1540 Pankhope pathu mthirepo
  • Hymn 497 TILIKUIMBA nyimbo yomweyi,
  • Hymn 1407 Tula mtolo wako
  • Hymn 1408 Kodi mwalandira Yesu?
  • Hymn 838 E, tsiku lonse Inu ndifunitsa;
  • Hymn 101 Lodala tsiku lomwelo
  • Hymn 716 Tibwezeretu bwanjiko?
  • Hymn 1052 Ndilira mtima wotamanda
  • Hymn 212 Onse am’Mwamba ali mowemo,
  • Hymn 1695 Pokumbukira mtandawo
  • Hymn 437 MULUNGU wa Yakobo Inu, mdyetsa anthu anu,
  • Hymn 1406 Kodi ukafuna
  • Hymn 13 Mtiwerengere m’Mwamba ndi oyera;
  • Hymn 194 Kuli dziko labwino m’Mwamba
  • Hymn 4 INU Mulungu, tikuyamikani;
  • Hymn 746 Imfa ndi mdima zinathawa zii!
  • Hymn 104 MUBWERE Mzimu Inu
  • Hymn 1515 Ndikachimwa, Bukuli
  • Hymn 1603 Zina za Yesu m;Mwambamo,
  • Hymn 1387 Amaweta nyama zonse,
  • Hymn 339 Tipempha,
  • Hymn 68 Kwathu ndidzaimba nyimbo
  • Hymn 1765 Zoonazi amithenga
  • Hymn 228 Ataya zoipa,
  • Hymn 489 YESU ndiye Bwenzi lathu,
  • Hymn 247 Tsono poukanso
  • Hymn 1190 Aleluya, mlemekeze,
  • Hymn 1727 Pokumbukira mtandawo
  • Hymn 1268 Mundilandiretu,
  • Hymn 569 Tiimbe ndi kulalikira
  • Hymn 1702 Pakufa ine Mbuye
  • Hymn 213 INE ndili ndi manyazi
  • Hymn 1409 Kodi mufunatu Yesu?
  • Hymn 1841 Kumadzi kuli njiratu andiyendetsa bwino,
  • Hymn 915 Mumzinda wa Mulungu
  • Hymn 955 Komwe ndi chimwemwe ine
  • Hymn 20 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 622 Tiyamikira ‘Tate,
  • Hymn 705 Tikhaletu nawo, Mbuye,
  • Hymn 1196 E! chikondi ndithu,
  • Hymn 369 Lowani m’nyumba mwakemu
  • Hymn 579 Pochezera m’dambomo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version