Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 413 ZIPATA zachitsulo zitseguke zonse mbee!

  1. Home   »  
  2. Hymn 413 ZIPATA zachitsulo zitseguke zonse mbee!

Hymn 413 ZIPATA zachitsulo zitseguke zonse mbee!

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 413 ZIPATA zachitsulo zitseguke zonse mbee!

 

ZIPATA zachitsulo zitseguke zonse mbee!
Ambuye wa Kumwambako aloŵe momwemo.

Mbendera yake ikupiza m’mlengalengamo,
Kufana ndi nyenyezi younika m’mdimamo.

Ankondo a Mulungu ’nu,
Yendani m’njiramo,
Mitima yanu yonseyo iyeretsedwe mbuu!

Tsatani Mbuye Yesuyo ndi mtanda wakewo;
Mlaliketu Uthenga kwa anthu onsewo.

Musamaopa kanthu ’yi tamani Yesuyo;
Kaimbireni nyimboyi ndi mphamvu zonse.

Zipata zatsegudwa mbee! za m’dziko monsemo;
Ambuye wapambanatu ndi mtanda wakewo.

Post navigation

Previous: Hymn 412 MOYO uli pafupi,
Next: Hymn 414 INU bambo, inu mayi,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 241 MTENDERE uli m’mtima mwathumu,
  • Hymn 1468 Zobvala zake zonse
  • Hymn 140 NDINAMIRA m’machimo, wosaonekanso,
  • Hymn 271 Pomwalira Mbuyeyo
  • Hymn 415 PAMAYIKO pali mdima,
  • Hymn 1425 Apempha malo Ambuye;
  • Hymn 1704 Zintchito zakezi
  • Hymn 281 MBUYE, mwatiuza ’fe
  • Hymn 426 Mpulumutsi Yesu,
  • Hymn 1786 Ndikonda Mlungu pomva Mbuye wanga
  • Hymn 1368 Mitambo inu yakumwambako,
  • Hymn 1032 Ntchito za Yesu gwira
  • Hymn 541 Ana inu, yamikani
  • Hymn 1311 Pothawira pena ‘yi,
  • Hymn 1649 Kutenga inetu, kutenga inetu
  • Hymn 249 Amen, Amen, Amen.
  • Hymn 1379 Mulungu yemweyo
  • Hymn 1331 Yesu wathu Mbuyeyo
  • Hymn 430 Tero tidzakwera
  • Hymn 420 Mtima umabisala
  • Hymn 835 Mukhale ndine, dzuwalo lalowa,
  • Hymn 1502 Kodi ulikulemedwa
  • Hymn 395 AMBUYE, Mwini zonsezi,
  • Hymn 245 KHALANI duu! Ambuye adzatu;
  • Hymn 932 Munabvala thupi lathu,
  • Hymn 1099 Sindidziwatu zamawa,
  • Hymn 1234 Ati Yesu Mbuyeyo:
  • Hymn 239 Akumwambawo
  • Hymn 315 Munagwa pa Atumwiwo;
  • Hymn 1030 Tioperanji ifetu?
  • Hymn 980 Tiyeni ku nkhondo iyi,
  • Hymn 118 Musaone zobvalazo,
  • Hymn 648 Mulungu wa Kumwamba,
  • Hymn 276 MKRISTU, ulimbike
  • Hymn 27 LEMEKEZANI Yehova,
  • Hymn 254 Adzanena kwa anthuwo
  • Hymn 1657 Mbuye, mutsaganebe
  • Hymn 135 USANABADWE, Yeremiya,
  • Hymn 482 Ndinu wakuyera,
  • Hymn 119 Tamverani anthu inu,
  • Hymn 347 Mfumu iyi,
  • Hymn 1027 Tithawiranji ifetu?
  • Hymn 754 Ndi mtanda uli m’maso mbuu,
  • Hymn 696 Ufumu wake udalitsa
  • Hymn 250 MBUYANGA Yesu,
  • Hymn 369 LERO mwatipatsa moyo,
  • Hymn 353 Anatuma Mtetezi,
  • Hymn 284 MAVUTO ndi ambiri,
  • Hymn 1355 Atate, Mwana, Mzimunso,
  • Hymn 1474 Zilepheradi zonse kugula moyowo,
  • Hymn 1627 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 1256 Chitsime ndi chokoma
  • Hymn 1404 “Undipatsetu
  • Hymn 1285 Yesu, n’kupatsani zonse,
  • Hymn 1688 Mulibe m’mandamu,
  • Hymn 226 BWENZI ndinamkomanayo
  • Hymn 1505 Ndikampeza, ndikamtsata
  • Hymn 682 Tsatani Mbuye Yesuyo ndi mtanda wakewo;
  • Hymn 411 TAMVA mawu omwewo,
  • Hymn 231 Mwazi wa Yesu wokondwa

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version