Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 408 ABALE nonse mulindiranji?

  1. Home   »  
  2. Hymn 408 ABALE nonse mulindiranji?

Hymn 408 ABALE nonse mulindiranji?

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 408 ABALE nonse mulindiranji?

 

ABALE nonse mulindiranji?
Bweranitu kwa Yesuyo;
Ali kuyitana inu nonse,
Ndithu bweranitu.

Mvetsa mbale moyo ukutha,
Dziko lingonkabe;
Siya zonse bweratu we,
Yesu adzakondwa.

Tiyeni tonse tilimbiketu,
Kubukitsa Uthengawo;
Womwe Ambuye anadza nawo,
Tisakhale chete.

Tiyeni tifalitse mawuwo,
Tisabise Uthengawo;
Yesu anatiferatu tonse,
Kutipulumutsa.

Post navigation

Previous: Hymn 400 ONA Mwana wa Nkhosa,
Next: Hymn 421 ANTHU ali m’mdima akuyitanitsa,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1685 Nla Mlungu dzuwali;
  • Hymn 264 KHALATU woyera, pempheratu m’tseri;
  • Hymn 999 Amaliwongo ochuluka amalowa m’mtima
  • Hymn 1533 Ndipatsa inu mtimawu,
  • Hymn 1181 Adalitsika munthuyo
  • Hymn 481 USACHIMWE konse,
  • Hymn 1742 Yesu ndinu moyo wathu,
  • Hymn 832 Zochimwa za usana uno mndikhululukire ‘ne;
  • Hymn 1825 Zobvuta zoopsa ndi zosaukazi
  • Hymn 149 Ndisauka, sindikhoza
  • Hymn 419 M’manja a Yesu wanga
  • Hymn 1612 Adzadza indetu
  • Hymn 102 MZIMU Woyera, mudzetu kwa ine
  • Hymn 371 AMBUYE, tasonkhana
  • Hymn 232 Uchita kwombola,
  • Hymn 437 MULUNGU wa Yakobo Inu, mdyetsa anthu anu,
  • Hymn 224 LINDIKOMERA dzina la Ambuye Yesu wanga,
  • Hymn 180 Ndinachita mphulupulu,
  • Hymn 311 Tifuna kuchita chifuniro chanu,
  • Hymn 234 Kwa kutha kwa moyo,
  • Hymn 721 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 1853 Etu ine, etu ine,
  • Hymn 14 Tsiku ndi tsiku timalemekeza;
  • Hymn 1574 Anthu ose ndi mitundu
  • Hymn 581 Mtiphunzitse bwinotu,
  • Hymn 545 Anatifera tonsefe
  • Hymn 428 Tiyandika, Mbuye,
  • Hymn 723 Mundimvere, Mbuye wanga
  • Hymn 1664 Ndigwadira Inu, Yesu,
  • Hymn 304 POZUNZIDWA inu ponseponse
  • Hymn 1832 Za m’mdima, imfa, nkhondo ndi zoipa sindiopa;
  • Hymn 1807 Chithawa m’talitali
  • Hymn 497 Yesu andikonda ine,
  • Hymn 1199 Ndikhumba ine ndithu
  • Hymn 930 Leroli chisoni chokha,
  • Hymn 19 MULUNGU akhale nawo,
  • Hymn 689 Anapeza Mwana
  • Hymn 1360 Ndi Aleluya imbirani
  • Hymn 1342 Tadza kumtsinjeku
  • Hymn 121 Imbira!
  • Hymn 307 ABALE anga ine ndikupita,
  • Hymn 417 M’BWERE Mlungu Mbuye wathu,
  • Hymn 244 Ndidze pafupi pa
  • Hymn 312 NDIMAYENDA paulendo
  • Hymn 629 Tinayenda muli mdima
  • Hymn 1043 Mbiri yake ubukitse,
  • Hymn 1801 Nafuna kwaononga
  • Hymn 428 MBUYE mtsitsimutse
  • Hymn 399 Tchimo lathu lonse, Yesu,
  • Hymn 126 Mwa ine, moyo wanga ndi Yesu
  • Hymn 421 Ine ndine mlendo
  • Hymn 203 Pamtandapo, pamtanda,
  • Hymn 947 Akristu tonsefe, tikondwe m’Dzikoli
  • Hymn 376 Adzadalitsa ‘fe
  • Hymn 1592 Tsono mubwere inunso,
  • Hymn 378 Ku madzi ake odikha
  • Hymn 181 Zonse ndinakonda kale
  • Hymn 1190 Aleluya, mlemekeze,
  • Hymn 216 NDISAUKA, ndinachimwa,
  • Hymn 870 Satana apambana tikayamba kusiyana;

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version