Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 405 POLENGA dzikoli

  1. Home   »  
  2. Hymn 405 POLENGA dzikoli

Hymn 405 POLENGA dzikoli

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 405 POLENGA dzikoli

 

POLENGA dzikoli
Pakumva Inudi,
Kwayeratu;
Mumve pempheroli,
Ndipo pamenepo
Palibe mawuwo,
Muŵaletu.

Inu wakudzatu
Kuŵachiritsadi
Anthendawo,
Kupatsa moyowo,
Kuona m’masomo,
Pa anthu onsewo
Muŵaletu.

Mzimu woonadi
Ndi wachikondicho,
Idzanitu;
Muunikirepo
Pali zamdimazo,
Pa dziko ponsepo
Muŵaletu.

Inu atatuwo,
Wodala Mlunguyo,
Timveretu;
Pa dziko ponsepo
Muchotse mdimawo,
Mutume Mawuwo,
Muŵaletu.

Post navigation

Previous: Hymn 400 ONA Mwana wa Nkhosa,
Next: Hymn 421 ANTHU ali m’mdima akuyitanitsa,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 491 KWA Yesu ndi kwabwinoko,
  • Hymn 1447 Yesu ngwachifundodi,
  • Hymn 522 Akazi anadza
  • Hymn 283 AMBUYE m’chipululu,
  • Hymn 1015 Mbuye, mwatiuza ‘fe
  • Hymn 79 PAKWITANA Mbuye wanga
  • Hymn 195 Bwinoli tipita,
  • Hymn 1417 Atate ‘nu, atate ‘nu,
  • Hymn 1688 Mulibe m’mandamu,
  • Hymn 1163 Tili ndi mtendere
  • Hymn 157 Mbuye, Mzimu Woyera
  • Hymn 617 Nthawi yina Mbuyeyu
  • Hymn 1553 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 994 Limba mtima mbale wanga,
  • Hymn 1243 Kodi mayi wobereka
  • Hymn 478 YESU atiuza tiŵale ’fe.
  • Hymn 356 Tinafena m’nyanjamo,
  • Hymn 1353 Ambuye Yesu, Inutu
  • Hymn 466 Yesu, muli pa chimpando
  • Hymn 210 PEREKANI mtima wanu,
  • Hymn 1745 Yesu aitana ife:
  • Hymn 272 Ankhondowo poona
  • Hymn 1675 Lambira Mfumuyo
  • Hymn 1259 Ndikhulupirira bwino
  • Hymn 756 Sindili woyenera ‘ne,
  • Hymn 237 SINDINANYENGEDWA konse
  • Hymn 1670 Bwenzi ndiye wakufera,
  • Hymn 289 Ndi manja athu awa nawo nganu,
  • Hymn 1376 Akulu nonse ndi mafumu ‘nu,
  • Hymn 1248 ‘Dzanitu Wamphamvu yonse,
  • Hymn 895 Ndikabwera ndi katundu
  • Hymn 58 Titasokera tinabwerera,
  • Hymn 1000 Amatininkha zida zoteteza mtima, ndizo:
  • Hymn 158 WOCHIMWA iwe, bweratu,
  • Hymn 475 Mbuye ndikhaletu
  • Hymn 201 NDILINKUDZA kwa Ambuye,
  • Hymn 1348 Akupeza, akupeza,
  • Hymn 951 Ndi kale lonse mnandisunga ‘ne;
  • Hymn 1558 Wosangalatsa, ine ndikalira
  • Hymn 1497 Simbani mobwereza,
  • Hymn 158 Mzimu, mlonge m’mtimamo
  • Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,
  • Hymn 216 NDISAUKA, ndinachimwa,
  • Hymn 1527 Ndiye Mzimu Wakuyera
  • Hymn 1103 Ndakudani, mnandikonda
  • Hymn 1625 Ife tonse tikumbuke
  • Hymn 562 Mwa ubwana wake wonse
  • Hymn 1125 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 435 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 1358 Lemekeza Mfumu yathu,
  • Hymn 132 MVERA mtima wanga ’we
  • Hymn 657 Ambuye, ndi chikondi tho!
  • Hymn 2 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 455 Mdileke kulimbna ndi
  • Hymn 447 Usachimwe konse,
  • Hymn 594 Monga may’ asusuza
  • Hymn 1701 Nditani Bwenzi langa
  • Hymn 596 Mlungu ali nane;
  • Hymn 1025 Ndikamayenda m’mdimamo,
  • Hymn 279 Mbwere mudzamve nonse

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version