Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 404 YANG’ANA mtanda wa Yesu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 404 YANG’ANA mtanda wa Yesu,

Hymn 404 YANG’ANA mtanda wa Yesu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 404 YANG’ANA mtanda wa Yesu,

 

YANG’ANA mtanda wa Yesu,
Upeze moyo;
Chuma cha dziko chidzatha,
Yang’ana kwa Yesu.

Poyang’ana kwa Yesu Mbuye,
Pakuwona pamtanda wake,
Moyo ulipo.

Yesu alira pamtanda,
Kulilira ‘fe;
Kuti tilape zoipa,
Zomwe tichitazi.

Ambuye anatifera,
Pamtanda paja;
Kuti tikapeze moyo,
Kumwamba kwa Yesu.

Post navigation

Previous: Hymn 400 ONA Mwana wa Nkhosa,
Next: Hymn 421 ANTHU ali m’mdima akuyitanitsa,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 151 Inde, Yesu, mulandira,
  • Hymn 252 MTIMA wa Mbuyako,
  • Hymn 358 MLUNGU ali muno,
  • Hymn 1102 Dziko lonse ndilitaya;
  • Hymn 369 LERO mwatipatsa moyo,
  • Hymn 46 O! ufulu tigwirizane
  • Hymn 971 Ndinu Mbusa wanga;
  • Hymn 324 Walira Yesu pazobvutazo,
  • Hymn 1343 M’dzina la Yesuyo
  • Hymn 1626 Mbuye Yesu adzabwera,
  • Hymn 1731 Ife tinachimwadi,
  • Hymn 57 TIYENI, dzalireni nane,
  • Hymn 1751 Mbuye ngwodalitsika,
  • Hymn 860 Nthawi yina adzadzuka
  • Hymn 1160 Ndinakhala wakuipa,
  • Hymn 317 Zambiri zagona m’kholamo,
  • Hymn 1437 Yesu ndi wokonda;
  • Hymn 1633 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 411 TAMVA mawu omwewo,
  • Hymn 778 Mwini madalitso,
  • Hymn 506 Ndikondwa kuti Yesu akonda,
  • Hymn 804 Muchotse zonse zoti bii
  • Hymn 301 Mwanawankhosa
  • Hymn 106 Ife, tapulumukadi,
  • Hymn 209 M’NDILANDIRE ine Mbuye
  • Hymn 1531 Kudzirala ndi kufatsa,
  • Hymn 1170 Pamtanda wake
  • Hymn 1164 Tikakhulupira
  • Hymn 362 Imvani Yesu akuti:
  • Hymn 215 TATE ndili mwana wanu,
  • Hymn 1788 Mtimanga, bwera kuti upumule
  • Hymn 549 Ndiye Mbuye, Mfumu yanga,
  • Hymn 51 PANTHAWI yakufa Ambuye,
  • Hymn 145 Kale ndinafuna
  • Hymn 465 ANA a Yerusalemu
  • Hymn 912 Makomo afanana
  • Hymn 11 NDI mitima yokondwera,
  • Hymn 447 OYAMIKA Mlungu m’bwere,
  • Hymn 1592 Tsono mubwere inunso,
  • Hymn 1613 A Mulungu
  • Hymn 117 CHOLIMBITSA mtima ndi chonditsogolera;
  • Hymn 1493 Mbiri yakalelomwe
  • Hymn 351 CHIYEMBEKEZO changacho,
  • Hymn 1093 Odala ndi onsewo
  • Hymn 81 Imva mawu akewo,
  • Hymn 1320 Ndayang’anira Mbuyeyo,
  • Hymn 1811 Tipulumuka mommo,
  • Hymn 50 Akhristu nyamulani
  • Hymn 1375 Ndi anamwali obvekedwa mbuu!
  • Hymn 86 Mwandipatulira ine,
  • Hymn 482 TCHIMO musalole, musadziipitse,
  • Hymn 277 Mbwere nonse muone
  • Hymn 1654 Mbuye, mutsaganetu
  • Hymn 54 Dalitsani mafuko onse,
  • Hymn 1292 Wolapa mtima simunyozadi,
  • Hymn 678 Ibukike mbiri yanu,
  • Hymn 436 YEHOVA Mlungu wathu,
  • Hymn 723 Mundimvere, Mbuye wanga
  • Hymn 1361 Ndi Aleluya imbirani
  • Hymn 1120 Ndifuna Yesuyo

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version