Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 404 YANG’ANA mtanda wa Yesu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 404 YANG’ANA mtanda wa Yesu,

Hymn 404 YANG’ANA mtanda wa Yesu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 404 YANG’ANA mtanda wa Yesu,

 

YANG’ANA mtanda wa Yesu,
Upeze moyo;
Chuma cha dziko chidzatha,
Yang’ana kwa Yesu.

Poyang’ana kwa Yesu Mbuye,
Pakuwona pamtanda wake,
Moyo ulipo.

Yesu alira pamtanda,
Kulilira ‘fe;
Kuti tilape zoipa,
Zomwe tichitazi.

Ambuye anatifera,
Pamtanda paja;
Kuti tikapeze moyo,
Kumwamba kwa Yesu.

Post navigation

Previous: Hymn 403 NDIYIMBA ndi chimwemwe lero,
Next: Hymn 405 POLENGA dzikoli

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1011 M’mawa tizifesa
  • Hymn 521 Apunzitsi, ana omwe,
  • Hymn 1402 Mverani Iye ati: idzanitu;
  • Hymn 26 NDIKULEMEKEZA
  • Hymn 102 Mzimu ndi mtsogoleri
  • Hymn 266 MBUYE ndamva mwawazira
  • Hymn 108 MBUYE wondipulumutsa,
  • Hymn 805 Madzulo ano mkhaletu
  • Hymn 461 Inu nonse anzanga,
  • Hymn 1140 Paja athira Yesutu
  • Hymn 1005 Mdani adza nazo mphamvu,
  • Hymn 1387 Amaweta nyama zonse,
  • Hymn 854 Timlemekeze Mlunguyu
  • Hymn 76 Ndipereka zanga zonse
  • Hymn 408 Oipa tili tonsefe;
  • Hymn 779 Yesu Mbuye wanga,
  • Hymn 616 Dziko lathu lonseli
  • Hymn 837 Koma kalelo mnakhalitsa pano,
  • Hymn 61 A! MUTU wakuyera,
  • Hymn 351 CHIYEMBEKEZO changacho,
  • Hymn 353 Anatuma Mtetezi,
  • Hymn 1488 Musawalole mawuwo
  • Hymn 897 Ndine mlendo pansi pano,
  • Hymn 1219 Bwenzi ndinamkomanayo
  • Hymn 511 Ntchito zake zatha,
  • Hymn 801 Lero mwatipatsa moyo,
  • Hymn 1318 Ndibwera kwa Ambuyeyo,
  • Hymn 185 NDINE Mbusayo wabwino,
  • Hymn 638 Ndi Mzimutu Woyera
  • Hymn 690 Mu ulemerero,
  • Hymn 812 Ndi ena sanamvera ‘yi,
  • Hymn 1382 E, chifundo chake chonse
  • Hymn 481 Yesu wa Kumwamba,
  • Hymn 477 Mpulumutsi, Mbusa wathu,
  • Hymn 1749 Chifukwa chipulumutso
  • Hymn 1538 Mzimu Woyera, mudzetu
  • Hymn 1155 Abale angakhale m’talimo
  • Hymn 109 MUTHIRE, Yesu, m’mtimanga
  • Hymn 1558 Wosangalatsa, ine ndikalira
  • Hymn 442 MASIKA a m’dziko Mbuye,
  • Hymn 882 Kodi tikulema nazo
  • Hymn 860 Nthawi yina adzadzuka
  • Hymn 411 Yesu adza kukundika
  • Hymn 415 Tidzalandirabe komwe
  • Hymn 1000 Amatininkha zida zoteteza mtima, ndizo:
  • Hymn 1346 Ndaima pano, ndaima pakhomo:Lowa, lowa, lowa, lowa!
  • Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,
  • Hymn 399 M’KHOLA mwa ng’ombe ku Betlehemu
  • Hymn 284 MAVUTO ndi ambiri,
  • Hymn 482 TCHIMO musalole, musadziipitse,
  • Hymn 1431 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 1845 Zabwino ndi zokoma zinditsata chitsatire;
  • Hymn 403 Dzuwa liwala, m’tulotu
  • Hymn 991 Ndi zapansi pano
  • Hymn 303 Ona pamtanda Yesuyo
  • Hymn 366 MADZULO aja kalero
  • Hymn 460 KULI kaphiri m’talimo
  • Hymn 298 “Tadodoma, abusa,
  • Hymn 469 Lero mkhale nafe ndithu,
  • Hymn 1725 Zochimwa zanga zonsezo

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version