Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 404 YANG’ANA mtanda wa Yesu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 404 YANG’ANA mtanda wa Yesu,

Hymn 404 YANG’ANA mtanda wa Yesu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 404 YANG’ANA mtanda wa Yesu,

 

YANG’ANA mtanda wa Yesu,
Upeze moyo;
Chuma cha dziko chidzatha,
Yang’ana kwa Yesu.

Poyang’ana kwa Yesu Mbuye,
Pakuwona pamtanda wake,
Moyo ulipo.

Yesu alira pamtanda,
Kulilira ‘fe;
Kuti tilape zoipa,
Zomwe tichitazi.

Ambuye anatifera,
Pamtanda paja;
Kuti tikapeze moyo,
Kumwamba kwa Yesu.

Post navigation

Previous: Hymn 400 ONA Mwana wa Nkhosa,
Next: Hymn 421 ANTHU ali m’mdima akuyitanitsa,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 23 Mvera mtima wanga ‘we
  • Hymn 287 POKONDWA ndi poona vuto
  • Hymn 1064 Moyowo
  • Hymn 685 Tamva mawu amwewo
  • Hymn 653 Nditsogolere m’njirayi
  • Hymn 341 PAKUPEMPHERATU
  • Hymn 12 Kumva milandu yathu mudzabwera
  • Hymn 1659 Ndiye mtsamiro
  • Hymn 251 Kuli chimwemwe m’dzuwalo
  • Hymn 4 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 22 Mbuye mtsitsimutse!
  • Hymn 963 Aulendo, munka kuti
  • Hymn 845 Ufumu wanu, Mbuye Yesu,
  • Hymn 587 Mutitsuke,
  • Hymn 469 Lero mkhale nafe ndithu,
  • Hymn 363 Funani Mlungu tsopano,
  • Hymn 994 Limba mtima mbale wanga,
  • Hymn 200 Ndi tsopano tilindira
  • Hymn 1694 Timwimbire Mlungu wathu, Aleluya
  • Hymn 216 Ndi misozi ndi chisoni
  • Hymn 141 Yenda iwe, yenda,
  • Hymn 207 Malo alimo m’nyumba ya Yesu,
  • Hymn 302 Anasenza m’thupi mwake;
  • Hymn 1136 Mulungu anditsogolera
  • Hymn 264 Bvinabvina moyo wanga,
  • Hymn 21 Mbuye mtsitsimutse!
  • Hymn 747 Tadzanitu, okhulupiradi,
  • Hymn 519 Mverani, aimba anawo,
  • Hymn 756 Sindili woyenera ‘ne,
  • Hymn 74 IDZA wolema,
  • Hymn 188 Ine ndili ndi manyazi
  • Hymn 602 Mpulumutsi wakukoma,
  • Hymn 283 AMBUYE m’chipululu,
  • Hymn 1371 Mitengo yaitalitali ‘nu
  • Hymn 417 M’BWERE Mlungu Mbuye wathu,
  • Hymn 1227 Ndiyamika Mbuye wanga
  • Hymn 1115 M’munda wa Mbuyako
  • Hymn 159 Kamwana Yesu ‘nabadwa,
  • Hymn 890 Kumbuka ‘bale ako
  • Hymn 234 IMFA ndi mfumu ya mdimawo,
  • Hymn 1027 Tithawiranji ifetu?
  • Hymn 1806 Nowayo anatuma,
  • Hymn 336 Perekani mtima wanu
  • Hymn 419 ANYAMATA a Mulungu,
  • Hymn 219 YESU Mbuyetu, mwafera
  • Hymn 1637 Tisaleke kugwirabe
  • Hymn 430 Tero tidzakwera
  • Hymn 222 NDILIKUMVA m’mtima mwanga
  • Hymn 943 Onse aliko takonda kalelo,
  • Hymn 483 NTHAŴI yaubwana yatha,
  • Hymn 1620 Aleluya,
  • Hymn 51 PANTHAWI yakufa Ambuye,
  • Hymn 562 Mwa ubwana wake wonse
  • Hymn 1561 Mzimu Woyera, n’dzipereka ndense,
  • Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,
  • Hymn 382 M’wabatize anzathuwa,
  • Hymn 281 Atate, ndipempha
  • Hymn 1416 Mbuye wanga ndilikumva,
  • Hymn 640 Anakwatira kale
  • Hymn 35 Zonse za m’dziko zidzatha,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version