Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 4 INU Mulungu, tikuyamikani;

  1. Home   »  
  2. Hymn 4 INU Mulungu, tikuyamikani;

Hymn 4 INU Mulungu, tikuyamikani;

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 4 INU Mulungu, tikuyamikani;

 

INU Mulungu, tikuyamikani;
Tivomereza ndinu Ambuyathu;
Ponse, atate, akugwadirani,

Nanu akukuzani amithenga,
Nanu zam’mwamba ndi zamphamvu zake,
Nanu angelo a mitundu yonse
Akuimbirani:

“Mbuye Woyera! E, Woyera nokha!
Mbuye Woyera! Mbuye wa makamu!
Ponse ulemu wanu ndi wodzaza;
Pansi ndi Kumwamba.”

Inu atumwi akumweka aja,
Ndi aneneri oyanjana omwe;
Ndi aunyinji anakuferani;
Akuyamikani.

Mpingo Woyera! wa kwa anthu onse;
Ukumverani, Mfumu ndi Atate,
Mwana woona wa ulemu wonse,
Mzimu, Nkhoswe yemwe.

Khristu Mfumuyo yaulemerero!
Mwana wosatha wa Atate ndinu!
Simunanyoza mimba ya Namwali;
Potipulumutsa.

Imfa mutagonjetsa ndi zoŵaŵa.
Njira munatsegula tikaloŵe;
Momwe mukhala Inu ndi Atate;
Mu ulemerero

Kumva milandu yathu mudzabwera;
Mutithandize, atumiki anu;
Mwatiwombola nawo mwazi wanu;
Mutipulumutse.

M’tiŵerengere
M’Mwamba ndi oyera;
Mutidalitse, ndi’fe anthu anu;
Moyo wosatha, mutipatse tonse;
Mutilamulire.

Tsiku ndi Tsiku timalemekeza;
Nanu tikukuzani osaleka;
Mbuye, m’tisunge tingachimwe lero;
M’tichitire nsisi.

Mbuye, chifundo chanu chitigwere;
Monga tikhulupi’ra inu nokha;
Takhulupi’ra zedi mwa’Nu, Mbuye;
Tisagome konse!

Post navigation

Previous: Hymn 1858 Ha! Chikondi cha Mulungu,
Next: Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1272 Muyambe ntchito yanuyi,
  • Hymn 293 Tidziperekadi konse kwa Inu
  • Hymn 781 Tatsegukani inutu,
  • Hymn 1759 Powalitsira omwe
  • Hymn 467 Ife ana sitiopa,
  • Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 405 POLENGA dzikoli
  • Hymn 286 ZOVUTA zoopsya ndi zosaukazi
  • Hymn 1640 Alinkudza Ambuye Yesu
  • Hymn 1839 Yehova ndiye Mbusa wanga sin’ngasowe konse;
  • Hymn 1204 Ambuyanga Yesu,
  • Hymn 1525 Mbuye, mtiphunzitse
  • Hymn 1664 Ndigwadira Inu, Yesu,
  • Hymn 993 Pakumalizidwa
  • Hymn 486 MPULUMUTSI Yesu,
  • Hymn 609 Zanu zapansi nzokoma Mbuye; tikondwera ‘fe,
  • Hymn 282 INU muli mehere,
  • Hymn 485 POMPANO pandikonda
  • Hymn 487 INE ndine mlendo
  • Hymn 1688 Mulibe m’mandamu,
  • Hymn 487 Yesu, ndikabwera
  • Hymn 1556 Mzimu Woyera, mudzetu kwa ine,
  • Hymn 415 Tidzalandirabe komwe
  • Hymn 280 Tisonkhane tonsefe,
  • Hymn 1852 Mbuye ndamva mwawazira
  • Hymn 426 MBUYE, Mpingo wanu usauka kwakukuludi;
  • Hymn 1359 Ndi Aleluya imbirani
  • Hymn 1698 Chinkana dziko lonselo
  • Hymn 312 NDIMAYENDA paulendo
  • Hymn 1494 Mbiri yakalelomwe,
  • Hymn 8 Nanu Atumwi akumveka aja,
  • Hymn 293 LIMBA mtima mbale wanga
  • Hymn 1623 Adzatenga anthu ake
  • Hymn 1316 Ndabwera kwa Ambuyeyo:
  • Hymn 1735 “Sezani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 1540 Pankhope pathu mthirepo
  • Hymn 750 Yesu Mbuyathu, Inu nomwe ‘Nu,
  • Hymn 1481 Timsankhe Yesu Mbuyeyo,
  • Hymn 124 PAMTANDAPO, pamtanda,
  • Hymn 1804 Mulungu anatuma,
  • Hymn 1287 Wadza Yesu wandidzoza,
  • Hymn 1004 A! mizimu yakuipa
  • Hymn 637 Mbuyathu wokondedwa,
  • Hymn 745 Anatifera nsembe Iyeyo,
  • Hymn 517 “Osana m’Mwambamwamba!”
  • Hymn 40 Padziko pano tikhalira
  • Hymn 315 Munagwa pa Atumwiwo;
  • Hymn 707 Dalitseni, Mbuye, zonse
  • Hymn 1234 Ati Yesu Mbuyeyo:
  • Hymn 453 A! MULUNGU
  • Hymn 362 Imvani Yesu akuti:
  • Hymn 976 Muyendenso kunka komwe,
  • Hymn 783 Antchito a Mulungu ‘nu
  • Hymn 137 Yesu Mpulumutsi, Mpulumutsi
  • Hymn 772 Muwalimbikitse onse
  • Hymn 329 Yesu atonthoza mtima
  • Hymn 86 Mwandipatulira ine,
  • Hymn 1396 Ndi maso Ambuyathu
  • Hymn 737 Mommuno, Mbuye, tionanetu,
  • Hymn 1167 Mulungu wanga,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version