Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 4 INU Mulungu, tikuyamikani;

  1. Home   »  
  2. Hymn 4 INU Mulungu, tikuyamikani;

Hymn 4 INU Mulungu, tikuyamikani;

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 4 INU Mulungu, tikuyamikani;

 

INU Mulungu, tikuyamikani;
Tivomereza ndinu Ambuyathu;
Ponse, atate, akugwadirani,

Nanu akukuzani amithenga,
Nanu zam’mwamba ndi zamphamvu zake,
Nanu angelo a mitundu yonse
Akuimbirani:

“Mbuye Woyera! E, Woyera nokha!
Mbuye Woyera! Mbuye wa makamu!
Ponse ulemu wanu ndi wodzaza;
Pansi ndi Kumwamba.”

Inu atumwi akumweka aja,
Ndi aneneri oyanjana omwe;
Ndi aunyinji anakuferani;
Akuyamikani.

Mpingo Woyera! wa kwa anthu onse;
Ukumverani, Mfumu ndi Atate,
Mwana woona wa ulemu wonse,
Mzimu, Nkhoswe yemwe.

Khristu Mfumuyo yaulemerero!
Mwana wosatha wa Atate ndinu!
Simunanyoza mimba ya Namwali;
Potipulumutsa.

Imfa mutagonjetsa ndi zoŵaŵa.
Njira munatsegula tikaloŵe;
Momwe mukhala Inu ndi Atate;
Mu ulemerero

Kumva milandu yathu mudzabwera;
Mutithandize, atumiki anu;
Mwatiwombola nawo mwazi wanu;
Mutipulumutse.

M’tiŵerengere
M’Mwamba ndi oyera;
Mutidalitse, ndi’fe anthu anu;
Moyo wosatha, mutipatse tonse;
Mutilamulire.

Tsiku ndi Tsiku timalemekeza;
Nanu tikukuzani osaleka;
Mbuye, m’tisunge tingachimwe lero;
M’tichitire nsisi.

Mbuye, chifundo chanu chitigwere;
Monga tikhulupi’ra inu nokha;
Takhulupi’ra zedi mwa’Nu, Mbuye;
Tisagome konse!

Post navigation

Previous: Hymn 3 TIMYAMIKIRE Mlunguyo,
Next: Hymn 5 ATATE wa Kumwambako,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 90 Ufuna kuleka kunyadako?
  • Hymn 626 Inde, ‘Tate, mtiyendetse
  • Hymn 967 Mbuye, ndapangana
  • Hymn 410 Ana ake angonga
  • Hymn 1156 Imfa ndi manda sitiopa ‘yi,
  • Hymn 871 Tiphatikane tonsefe okonda Yesu Kristu;
  • Hymn 1195 Wafunafuna ine
  • Hymn 793 Tikondwera kuti
  • Hymn 1206 Ndidzakukondani
  • Hymn 1055 E, mtima watsopano ndi
  • Hymn 165 Yendanitu m’ulemudi,
  • Hymn 148 PAKUPEMPHA ife pano,
  • Hymn 457 KALE m’mzinda wachifumu
  • Hymn 1594 Chikondano chakechi
  • Hymn 576 Kondwerani nonsenu
  • Hymn 1322 Ntchito zanga zonsezo
  • Hymn 455 Mdileke kulimbna ndi
  • Hymn 487 INE ndine mlendo
  • Hymn 307 Atate Wamkulu ndi wamphamvu zonse,
  • Hymn 335 Mtembenuke mtima wanu,
  • Hymn 418 M’manja Yesu wanga
  • Hymn 1733 Adzabwera Iyenso
  • Hymn 1668 Kumdziwitsa ndiko moyo,
  • Hymn 20 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 1207 Poyambapo ndakondwadi,
  • Hymn 148 Ndisauka, ndimasowa
  • Hymn 1116 Kwawo kwa Mbuyako
  • Hymn 1561 Mzimu Woyera, n’dzipereka ndense,
  • Hymn 118 Musaone zobvalazo,
  • Hymn 931 Tikagwidwa ndi chisoni,
  • Hymn 602 Mpulumutsi wakukoma,
  • Hymn 127 Mwazi wake ndi chitsime changa,
  • Hymn 207 Malo alimo m’nyumba ya Yesu,
  • Hymn 304 Imva kulira kwa Yesu
  • Hymn 467 Ife ana sitiopa,
  • Hymn 468 NDIKONDWA kuti
  • Hymn 1823 Opani Iye, nimuleke
  • Hymn 1713 Zochimwa zanga zonsezo
  • Hymn 479 ANYAMATA inutu,
  • Hymn 1769 Ndiye amachitira
  • Hymn 1603 Zina za Yesu m;Mwambamo,
  • Hymn 1032 Ntchito za Yesu gwira
  • Hymn 1177 Ndidziwitsitsa Yesu ndi wanga,
  • Hymn 629 Tinayenda muli mdima
  • Hymn 1686 Ndi mtima wonse mwimbedi
  • Hymn 1166 Masauko athu
  • Hymn 861 Mbuye, Mpingo wanu usauka kwa kukuludi;
  • Hymn 128 ANTHU m’maiko onse
  • Hymn 1111 Pamene ndilemedwa
  • Hymn 993 Pakumalizidwa
  • Hymn 559 Usikuwo woyerawo!
  • Hymn 1317 Ambuye naitana ‘ne:
  • Hymn 706 Tisaiwalire ‘bale
  • Hymn 327 NTCHITO yonse yakeyo
  • Hymn 1077 Khalatu woyera,
  • Hymn 258 Kazembe wanga m’matenda,
  • Hymn 879 Zokoma etu nthawizi”
  • Hymn 458 USIKUWO, woyerawo!
  • Hymn 1697 Onani m’mutu, m’manjanso
  • Hymn 1566 Mufike monga ngati mphepo yokokomayo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version