Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 39 MUNASIYATU dziko lanulo,

  1. Home   »  
  2. Hymn 39 MUNASIYATU dziko lanulo,

Hymn 39 MUNASIYATU dziko lanulo,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 39 MUNASIYATU dziko lanulo,

 

MUNASIYATU dziko lanulo,
E, chifukwa cha íne;
Ndi ku Betlehemuko,
Pakubadwa Inu,
M’nyumba zawo nakukanani.

Mbuye Yesu, lowani ‘mtima,
Nyumba yanu ndi mtima’nga;
Mbuye Yesu, lowani ‘mtima,
Nyumba yanu ndi mtima’nga.

Akumwambako nayimbitsatu,
Kukulemekezaní;
Koma monga mwana,
M’dziko munabadwa,
Munadzíchepetsadi.

Nyama za mthengo ndi mbalamezo,
Zili namo mogonamo;
Koma Mwana Mlungu,
Analibe nyumba,
M’mapululu nagonatu.

Munadzera ndi mawu amoyo,
Akupulumutsa anthu;
Anakaníza,
Anasautsa,
Anapachika Inu.

Mmene mubwera kutiŵeruza,
Ndi angelo oyimbira;
Mundiitane,
Muti, “Idza ‘we,
Khala nane Kumwamba.”

Mtima wanga udzakondwera,
Mmene mundilandiranso;
Mtima wanga udzakondwera,
Mmene mundilandiranso.

Post navigation

Previous: Hymn 20 CHIKONDI cha Mulungu wathu,
Next: Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1577 “Kwa Iye atikonda
  • Hymn 332 NDIKONDWA kuganizirabe
  • Hymn 355 DZIKO lonse mlambire
  • Hymn 407 Zochimwa sizilowako,
  • Hymn 1719 Ku Mzinda wakuyerawo
  • Hymn 1223 Ndidzaimba za Mulungu,
  • Hymn 712 Mulungu akondadi leroli
  • Hymn 1564 Mufike monga moto wakuotcha zomwezo.
  • Hymn 1724 Ambuye mthandize inetu
  • Hymn 1077 Khalatu woyera,
  • Hymn 120 MUNDINYEMERE ’ne
  • Hymn 167 KODI mwalandira Yesu?
  • Hymn 1814 Thupi lamwazi wathu’li
  • Hymn 201 Ngati zakuipa zathu
  • Hymn 336 Perekani mtima wanu
  • Hymn 1858 Ha! Chikondi cha Mulungu,
  • Hymn 668 Achisoni, obvutidwa,
  • Hymn 537 Aleluya! Aleluya!
  • Hymn 114 Ndine Mbusayo wabwino,
  • Hymn 1157 Mtendere wapambana m’Mwambamo
  • Hymn 471 Mbuye, tili ana anu,
  • Hymn 1242 Ku zoipa zonse zako,
  • Hymn 371 Mulungu, anthu ‘fe
  • Hymn 366 MADZULO aja kalero
  • Hymn 1587 Nditama Mlungu m’mtimamo,
  • Hymn 945 Tiyeni pamodzi,
  • Hymn 121 MULUNGU, anthu ’fe
  • Hymn 767 Munali mwana, Yesu ‘Nu
  • Hymn 771 Tsopano alandira
  • Hymn 445 TILIMALIMA m’minda,
  • Hymn 504 Pakumyamika Iye
  • Hymn 708 Peturo ‘nafusa Hananiya:
  • Hymn 1343 M’dzina la Yesuyo
  • Hymn 1643 Kufuna inetu, kufuna inetu,
  • Hymn 64 LERO Kristu anauka,
  • Hymn 256 Ndilira, ndilira,
  • Hymn 399 Tchimo lathu lonse, Yesu,
  • Hymn 1306 Ndi ine ndasaukadi,
  • Hymn 1297 Kumwamba komwe n’dzaimbira
  • Hymn 745 Anatifera nsembe Iyeyo,
  • Hymn 134 INU ansembe ngakhale mufunsa,
  • Hymn 417 M’manja a Yesu wanga
  • Hymn 1006 Yesu ati, “Ndidza msanga!”
  • Hymn 211 TIDZALAKALAKA kuwonana naye,
  • Hymn 88 Yesu, dzina lakukonda,
  • Hymn 1383 Dzina lake tibukitsa,
  • Hymn 315 YENDANI munjira yake,
  • Hymn 1615 Anakonda,
  • Hymn 525 Afike masiku
  • Hymn 392 ANU Mbuye ndifetu!
  • Hymn 416 PALIBE wina Kumwamba,
  • Hymn 550 Wosauka Iyedi
  • Hymn 794 Ambuye, tasonkhana
  • Hymn 259 CHISOMO chodabwitsacho,
  • Hymn 460 E! ang’ono ndifetu,
  • Hymn 953 Ichi chindisangalatsa
  • Hymn 327 NTCHITO yonse yakeyo
  • Hymn 1822 Lawani chikondano chake;
  • Hymn 748 Ndiye wa moyo wonse Mwiniyo,
  • Hymn 1661 Ndimachitira

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version