Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 39 MUNASIYATU dziko lanulo,

  1. Home   »  
  2. Hymn 39 MUNASIYATU dziko lanulo,

Hymn 39 MUNASIYATU dziko lanulo,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 39 MUNASIYATU dziko lanulo,

 

MUNASIYATU dziko lanulo,
E, chifukwa cha íne;
Ndi ku Betlehemuko,
Pakubadwa Inu,
M’nyumba zawo nakukanani.

Mbuye Yesu, lowani ‘mtima,
Nyumba yanu ndi mtima’nga;
Mbuye Yesu, lowani ‘mtima,
Nyumba yanu ndi mtima’nga.

Akumwambako nayimbitsatu,
Kukulemekezaní;
Koma monga mwana,
M’dziko munabadwa,
Munadzíchepetsadi.

Nyama za mthengo ndi mbalamezo,
Zili namo mogonamo;
Koma Mwana Mlungu,
Analibe nyumba,
M’mapululu nagonatu.

Munadzera ndi mawu amoyo,
Akupulumutsa anthu;
Anakaníza,
Anasautsa,
Anapachika Inu.

Mmene mubwera kutiŵeruza,
Ndi angelo oyimbira;
Mundiitane,
Muti, “Idza ‘we,
Khala nane Kumwamba.”

Mtima wanga udzakondwera,
Mmene mundilandiranso;
Mtima wanga udzakondwera,
Mmene mundilandiranso.

Post navigation

Previous: Hymn 38 ANGELO ayimba,
Next: Hymn 40 KAMWANA Yesu ’nabadwa,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 982 Tiyeni Akristu,
  • Hymn 794 Ambuye, tasonkhana
  • Hymn 166 Yendani, Munthu Wachisoni,
  • Hymn 184 LEKANI kubvutika ndi zinthu za padziko,
  • Hymn 674 Anthu onse taukani,
  • Hymn 1346 Ndaima pano, ndaima pakhomo:Lowa, lowa, lowa, lowa!
  • Hymn 244 Ndidze pafupi pa
  • Hymn 416 Woyenera ndani kunka
  • Hymn 33 OWONADI mtima,
  • Hymn 1389 Tithawire kwa Mulungu,
  • Hymn 432 KRISTU ndiye Mwala wathu,
  • Hymn 1300 Poyenda m’mdima bii,
  • Hymn 1766 Ndilikulemekeza
  • Hymn 1031 Gwira zintchito zako,
  • Hymn 1492 Sakukanani Yesudi,
  • Hymn 1165 Dzanja la Mulungu
  • Hymn 1450 Ndi angelo akumwamba
  • Hymn 940 Ndamvatu kuti tifika komweko
  • Hymn 949 Mundiwalire m’njira mwangamo,
  • Hymn 578 Falitsani mbiriyi,
  • Hymn 733 Ndimamva ludzu Yesu,
  • Hymn 808 Atipsinjadi masoka,
  • Hymn 1366 Sititha ifedi
  • Hymn 696 Ufumu wake udalitsa
  • Hymn 21 Mbuye mtsitsimutse!
  • Hymn 557 Usikuwo woyerawo!
  • Hymn 1593 Wina atikonda ife,
  • Hymn 1276 Ndikhulupirira, Yesu, Inu nokhadi
  • Hymn 143 Lero lino Mbuye Yesu
  • Hymn 1382 E, chifundo chake chonse
  • Hymn 530 Munaneneratu mawu a moyonso
  • Hymn 1631 Mudzabwera, mudzabwera;
  • Hymn 1660 Ndikakhumudwa
  • Hymn 663 Anyamata a Mulungu,
  • Hymn 1414 Zonse zinathedwadi;
  • Hymn 616 Dziko lathu lonseli
  • Hymn 227 NDIM’KONDE Kristuyo,
  • Hymn 1248 ‘Dzanitu Wamphamvu yonse,
  • Hymn 1105 Khala chete mtima wanga
  • Hymn 800 Yesu munadzukanso
  • Hymn 244 TIMVE za anamwali khumi,
  • Hymn 1063 Pokhala mtendere mu mtimangamu,
  • Hymn 1386 Ndi chifundo atipenya
  • Hymn 80 Utsegule mtimawo,
  • Hymn 780 Kwezani mitu yanuyo,
  • Hymn 182 YESU watidzera, watidzera,
  • Hymn 60 Chitetezo chachikulu
  • Hymn 163 Mukonda nyimbo za ana,
  • Hymn 199 Watitsogolera Mbuye,
  • Hymn 236 Omvana ndi Yesu,
  • Hymn 235 Kumwamba ndikaimbanso
  • Hymn 1070 Mthandize Mbuye, timvetu,
  • Hymn 1030 Tioperanji ifetu?
  • Hymn 564 Ndi chifukwa atikonda,
  • Hymn 384 Mulungu akhale nawo
  • Hymn 465 Yesu atiuza tiwale pa
  • Hymn 1364 Uzani zamphamvu,
  • Hymn 1403 ‘Mvani liwu lomwe
  • Hymn 818 Mkhululukire,
  • Hymn 843 M’maiko monse, zisi zomwe,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version