Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 39 MUNASIYATU dziko lanulo,

  1. Home   »  
  2. Hymn 39 MUNASIYATU dziko lanulo,

Hymn 39 MUNASIYATU dziko lanulo,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 39 MUNASIYATU dziko lanulo,

 

MUNASIYATU dziko lanulo,
E, chifukwa cha íne;
Ndi ku Betlehemuko,
Pakubadwa Inu,
M’nyumba zawo nakukanani.

Mbuye Yesu, lowani ‘mtima,
Nyumba yanu ndi mtima’nga;
Mbuye Yesu, lowani ‘mtima,
Nyumba yanu ndi mtima’nga.

Akumwambako nayimbitsatu,
Kukulemekezaní;
Koma monga mwana,
M’dziko munabadwa,
Munadzíchepetsadi.

Nyama za mthengo ndi mbalamezo,
Zili namo mogonamo;
Koma Mwana Mlungu,
Analibe nyumba,
M’mapululu nagonatu.

Munadzera ndi mawu amoyo,
Akupulumutsa anthu;
Anakaníza,
Anasautsa,
Anapachika Inu.

Mmene mubwera kutiŵeruza,
Ndi angelo oyimbira;
Mundiitane,
Muti, “Idza ‘we,
Khala nane Kumwamba.”

Mtima wanga udzakondwera,
Mmene mundilandiranso;
Mtima wanga udzakondwera,
Mmene mundilandiranso.

Post navigation

Previous: Hymn 20 CHIKONDI cha Mulungu wathu,
Next: Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 48 Ngakhale alemera
  • Hymn 1311 Pothawira pena ‘yi,
  • Hymn 302 NDIDZE pafupi pa
  • Hymn 1348 Akupeza, akupeza,
  • Hymn 1092 Ndimamva njala kuno, Yesu,
  • Hymn 1403 ‘Mvani liwu lomwe
  • Hymn 620 Mphatso zonse zathu
  • Hymn 506 Ndikondwa kuti Yesu akonda,
  • Hymn 861 Mbuye, Mpingo wanu usauka kwa kukuludi;
  • Hymn 1631 Mudzabwera, mudzabwera;
  • Hymn 102 Mzimu ndi mtsogoleri
  • Hymn 1494 Mbiri yakalelomwe,
  • Hymn 1451 Okoma ndiwo mawu
  • Hymn 365 Monga m’Mwamba mupambana
  • Hymn 650 Tikondwa tonse ndi kukuthokazani Nu
  • Hymn 101 MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,
  • Hymn 829 Titamadi ‘Tate,
  • Hymn 1361 Ndi Aleluya imbirani
  • Hymn 927 Pakutsazikana nanu
  • Hymn 1385 Anatsogolera kale
  • Hymn 958 Ndikalowa m’mtsinje muja,
  • Hymn 289 ANATILEMBA Yesu tikagwire nkhondo yake,
  • Hymn 661 Tamva aku Makedonyako atero,
  • Hymn 1769 Ndiye amachitira
  • Hymn 476 MBUYE, tili ana anu,
  • Hymn 1597 Timchimwira kopambana,
  • Hymn 490 Yesu, ndikabwera
  • Hymn 1847 Ife tonse, ife tonse,
  • Hymn 833 Mundilimbitse ndikayese manda ngati mphasayi,
  • Hymn 1511 Mndidalitsere ‘ne
  • Hymn 1333 Idzatu kwa Yesuyo,
  • Hymn 834 Tiyamike Mlungu wotipatsa zachifundozi,
  • Hymn 65 Chisomo chodabwitsacho
  • Hymn 934 Mnamwalira Inu paja,
  • Hymn 686 Imbadi za Iyeyo,
  • Hymn 889 Pemphera m’mbanda kucha,
  • Hymn 1854 Tate msandipitirire,
  • Hymn 421 Ine ndine mlendo
  • Hymn 54 MUNTHU wazisoniyo,
  • Hymn 700 Mzimu woonadi
  • Hymn 943 Onse aliko takonda kalelo,
  • Hymn 1016 Mbuye, mwatiuza ‘fe
  • Hymn 472 Amakumbukira zonse
  • Hymn 255 Pakuona imfayo
  • Hymn 1153 Mtendere uli m’mtima mwathumu,
  • Hymn 969 Akathira nsembe
  • Hymn 886 Chikondi, chimwemwe,
  • Hymn 247 MULUNGU anditsogolera,
  • Hymn 1765 Zoonazi amithenga
  • Hymn 1642 M’khola mwa ng’ombe ku Betelehemu
  • Hymn 1652 Mabala ajawo
  • Hymn 558 Mwanayo wa Mulunguyo
  • Hymn 1107 Anthu onse pansi pano
  • Hymn 522 Akazi anadza
  • Hymn 38 Kodi mubvutidwa naye katundu?
  • Hymn 115 NTHAWI ija ya Sauli,
  • Hymn 501 Yesu andikonda ine;
  • Hymn 349 Aitana,
  • Hymn 835 Mukhale ndine, dzuwalo lalowa,
  • Hymn 359 Tonse timyamiketu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version