Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 364 DZUŴA lapitira,

  1. Home   »  
  2. Hymn 364 DZUŴA lapitira,

Hymn 364 DZUŴA lapitira,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 364 DZUŴA lapitira,

 

DZUŴA lapitira,
Wadza mdimawo,
Mthunzi wamadzulo
Wagwa m’mwambamo.

M’mwambamo nyenyezi
Zithwanima mbee;
Zonse zili m’tulo
Pansi pali duu.

Yesu mutipatse
Tulo toti phee;
Ndi mdalitso wanu
Mndigonetse ’ne

Mpatse ana ’ng’ono
Alotemo mbee;
Anthu aulendo
Msungesungebe.

Mutonthoze mtima
Wopwetekawo;
Akutsata tchimo
Mletse onsewo.

Wonsewu usiku
Andisunge ’ne
Amithenga anu
Akuyera mbee.

Ndidzukanso m’maŵa,
Kucha koti mbuu,
Ndiyeretu mtima
M’maso mwanumo.

Titamadi ’Tate,
Mwana wakeyo,
Mzimu Woyeranso,
Nthaŵinthaŵizo.

Post navigation

Previous: Hymn 360 KRISTU wakuyeratu,
Next: Hymn 381 MONGA zomera zonsezo

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1629 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 1350 Mvera Yesu, mvera Yesu,
  • Hymn 1736 “Senzani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 485 Mukatiitana
  • Hymn 383 Zokoma ndi zakuyanja
  • Hymn 525 Afike masiku
  • Hymn 893 Mtima wanga ndikonzera,
  • Hymn 27 “Msanga ndidzabweratu,
  • Hymn 234 IMFA ndi mfumu ya mdimawo,
  • Hymn 833 Mundilimbitse ndikayese manda ngati mphasayi,
  • Hymn 978 Mtima wanu wonse ndithu
  • Hymn 1116 Kwawo kwa Mbuyako
  • Hymn 1459 Ambuye mulowetse
  • Hymn 972 Akristu limbikani,
  • Hymn 290 Ndi miyendo yathu iyinso njanu,
  • Hymn 1103 Ndakudani, mnandikonda
  • Hymn 444 Mpemphe Mbuye asunge
  • Hymn 1263 Mbuye, ndingogonj tere, Ndibvomerapo;
  • Hymn 552 Analira ndaniyo
  • Hymn 7 “Mbuye Woyera! E, Woyeranokha!
  • Hymn 770 Atate, muwapenye
  • Hymn 689 Anapeza Mwana
  • Hymn 1026 Inde nditaya chumacho,
  • Hymn 493 Ndimalira kwa Inutu,
  • Hymn 1816 Anatikondakonda ‘Ye,
  • Hymn 1622 Anthu onse amlambire
  • Hymn 138 SANGALATSA akusowa, masiku alikutha,
  • Hymn 1458 Satana ndi unyolo
  • Hymn 967 Mbuye, ndapangana
  • Hymn 160 MADALITSO ngati mvumbi,
  • Hymn 535 Mbuye timlemekeze,
  • Hymn 80 Utsegule mtimawo,
  • Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu
  • Hymn 1811 Tipulumuka mommo,
  • Hymn 20 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 168 Yendani mwaulemerero,
  • Hymn 1388 Tiimbire Mlungu wathu
  • Hymn 1547 Mtisangalatse m’zonse,
  • Hymn 996 Leka zakuipa zako,
  • Hymn 457 KALE m’mzinda wachifumu
  • Hymn 1677 Zomkweza zili m’Mwamba,Aleluya
  • Hymn 935 Mtima ukachita nkhawa
  • Hymn 815 Dzuwa lapita,
  • Hymn 372 DZUŴA la Mulungu
  • Hymn 1841 Kumadzi kuli njiratu andiyendetsa bwino,
  • Hymn 1322 Ntchito zanga zonsezo
  • Hymn 264 KHALATU woyera, pempheratu m’tseri;
  • Hymn 410 MAWU akewo anamveka ponse,
  • Hymn 46 INALIPO nthawi,
  • Hymn 1740 Yesu, ndi chifundo chanu
  • Hymn 361 Munka kangati kulawa
  • Hymn 49 Ndi ife akudziwa
  • Hymn 221 Yesu and’itana,
  • Hymn 1703 Zathedwa zonsetu
  • Hymn 1222 Bwenzi ndimamkomanayo
  • Hymn 885 Mndimvetse chisoni
  • Hymn 633 Tikasokera m’njira mutilondolere ndithu,
  • Hymn 727 Imfa ikandifikira,
  • Hymn 592 Kuti m’Mwambamo
  • Hymn 355 Tinafuna m’phirimo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version