Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 356 YESU Mbuye onani,

  1. Home   »  
  2. Hymn 356 YESU Mbuye onani,

Hymn 356 YESU Mbuye onani,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 356 YESU Mbuye onani,

 

YESU Mbuye onani,
Tadza poyitana Inu;
M’dzina lanu tifika,
Osekera kwa Atate.
M’khale nafe Inu nokha,
Tikayimba n’kupemphera.

Mbuye, Mzimu Woyera,
Munapatsa ana anu;
Kukalonga mumtima,
Mawu ndipo mvano womwe.
Zinthu zonse pansi pano,
Sizikondweretsa ife.

Mzimu, m’longe m’mtimamo,
Maphunziro achifundo;
Timve lero ndi mawa,
Ndi masiku onse: Yesu!
Ndipo M’mwamba tidzawona,
Tidazimva pansi pano.

Post navigation

Previous: Hymn 340 PEMPHERA m’mbanda kucha,
Next: Hymn 361 AMBUYE munapatsa tsiku

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1642 M’khola mwa ng’ombe ku Betelehemu
  • Hymn 143 Lero lino Mbuye Yesu
  • Hymn 1594 Chikondano chakechi
  • Hymn 148 Ndisauka, ndimasowa
  • Hymn 1009 Ndi m’kutero udzadziwa
  • Hymn 559 Usikuwo woyerawo!
  • Hymn 1796 Ndikhulupira mwa Ambuye
  • Hymn 494 Yesu, E, ndikufunani,
  • Hymn 842 Tipempha kuti Mpingo wanu
  • Hymn 126 DAVIDE kubusa kuja,
  • Hymn 1777 Mulungu wamkulu
  • Hymn 236 Omvana ndi Yesu,
  • Hymn 173 Mema nkhondoyo, wadza mdaniyo,
  • Hymn 1794 Mulungu awakonda anthu
  • Hymn 455 Mdileke kulimbna ndi
  • Hymn 370 Pakuti Mbuye Mlunguyo
  • Hymn 1464 Nditama Nsembe ya Mulungu,
  • Hymn 139 MLUNGU anapatsa moyo,
  • Hymn 1420 Abale ‘nu, abale ‘nu,
  • Hymn 421 Ine ndine mlendo
  • Hymn 1564 Mufike monga moto wakuotcha zomwezo.
  • Hymn 717 Ambuye zathu zonsezi
  • Hymn 1809 Yampatsa Nowa yemwe,
  • Hymn 244 Ndidze pafupi pa
  • Hymn 1672 Lambira Mfumuyo,
  • Hymn 1548 Mtitsitsimutse ife
  • Hymn 1495 Simbani bwinobwino
  • Hymn 288 HAYA! ’nzanga taonani
  • Hymn 688 Anthu akum’mawa
  • Hymn 239 TILI ndi mtendere
  • Hymn 1283 Yesu ndikhulupirira
  • Hymn 337 ‘Tate ‘Nu,
  • Hymn 478 Ndife ana, mutikonda,
  • Hymn 856 Kuunika kuoneka
  • Hymn 58 PAMTANDAPO Ambuyeyo
  • Hymn 1226 Wandipatsa moyo wake,
  • Hymn 731 Mundionetse, Yesu,
  • Hymn 1540 Pankhope pathu mthirepo
  • Hymn 1530 Mndilimbitse ndipirire
  • Hymn 1437 Yesu ndi wokonda;
  • Hymn 54 MUNTHU wazisoniyo,
  • Hymn 1703 Zathedwa zonsetu
  • Hymn 1083 “Khala mwa Ine,” Yesu anatero;
  • Hymn 1012 Ndi zipatsozo,
  • Hymn 629 Tinayenda muli mdima
  • Hymn 18 POKHALA Inu
  • Hymn 1387 Amaweta nyama zonse,
  • Hymn 428 Tiyandika, Mbuye,
  • Hymn 391 Mufafanize m’bukumo
  • Hymn 1310 Yesu wondikondadi,
  • Hymn 341 Ayenda,
  • Hymn 766 Monga zomera zonsezo
  • Hymn 598 Mlungu ali nane;
  • Hymn 1612 Adzadza indetu
  • Hymn 1129 Mbuyanga Yesu, ndikapanda Inu
  • Hymn 1798 Mukondwe anthu a Mulungu,
  • Hymn 466 OSANATU, osana,
  • Hymn 1316 Ndabwera kwa Ambuyeyo:
  • Hymn 831 Mundikumbutse, ndikapanda tulo, za Kumwambako;
  • Hymn 677 Ponse padakhala mdima

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version