Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 356 YESU Mbuye onani,

  1. Home   »  
  2. Hymn 356 YESU Mbuye onani,

Hymn 356 YESU Mbuye onani,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 356 YESU Mbuye onani,

 

YESU Mbuye onani,
Tadza poyitana Inu;
M’dzina lanu tifika,
Osekera kwa Atate.
M’khale nafe Inu nokha,
Tikayimba n’kupemphera.

Mbuye, Mzimu Woyera,
Munapatsa ana anu;
Kukalonga mumtima,
Mawu ndipo mvano womwe.
Zinthu zonse pansi pano,
Sizikondweretsa ife.

Mzimu, m’longe m’mtimamo,
Maphunziro achifundo;
Timve lero ndi mawa,
Ndi masiku onse: Yesu!
Ndipo M’mwamba tidzawona,
Tidazimva pansi pano.

Post navigation

Previous: Hymn 355 DZIKO lonse mlambire
Next: Hymn 357 TAMANDANI Mbuye,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1794 Mulungu awakonda anthu
  • Hymn 378 KWEZANI mitu yanuyo,
  • Hymn 1402 Mverani Iye ati: idzanitu;
  • Hymn 441 MBUYE, tikuthokozani,
  • Hymn 308 Ifetu kuchimwa, Mbuye,
  • Hymn 326 Yesu, Bwenzi la ochimwa,
  • Hymn 451 MLUNGU alinane;
  • Hymn 791 Anthu opembedzawo
  • Hymn 58 PAMTANDAPO Ambuyeyo
  • Hymn 443 Tchimo musalole,
  • Hymn 217 CHIPULUMUTSO chathu chayandika,
  • Hymn 879 Zokoma etu nthawizi”
  • Hymn 34 Yesu Mbuyetu, mwafera
  • Hymn 1655 Mbuye Yesu,
  • Hymn 1562 Mzimu Woyera, mudze mumitima mwathumo,
  • Hymn 741 Chakudya ichi chidzapita du,
  • Hymn 432 Ulendo ungoyamba
  • Hymn 1623 Adzatenga anthu ake
  • Hymn 1149 Chete! Chete!
  • Hymn 1735 “Sezani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 281 MBUYE, mwatiuza ’fe
  • Hymn 1704 Zintchito zakezi
  • Hymn 1015 Mbuye, mwatiuza ‘fe
  • Hymn 245 Ngakhale kuthengo
  • Hymn 421 Ine ndine mlendo
  • Hymn 410 MAWU akewo anamveka ponse,
  • Hymn 1451 Okoma ndiwo mawu
  • Hymn 454 Kapena m’mtima ndimakwiya,
  • Hymn 1659 Ndiye mtsamiro
  • Hymn 85 Mtima wanga wabvutika,
  • Hymn 810 Tsopano lino kwada bii,
  • Hymn 260 Angelo aitana,
  • Hymn 80 Utsegule mtimawo,
  • Hymn 336 KULINSO dziko lowala M’mwamba,
  • Hymn 1434 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 466 OSANATU, osana,
  • Hymn 1040 Ukafuna kulemera,
  • Hymn 303 MEMA nkhondoyo, wadza mdaniyo,
  • Hymn 485 POMPANO pandikonda
  • Hymn 392 Chimwemwe chomwe mpatseko
  • Hymn 96 Kodi mudzampembedza Mbuye
  • Hymn 583 Anabadwa,
  • Hymn 104 MUBWERE Mzimu Inu
  • Hymn 1253 Ndingopatsa Inu Mbuye
  • Hymn 876 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 72 YESU wakukoma mtima,
  • Hymn 1376 Akulu nonse ndi mafumu ‘nu,
  • Hymn 1269 Ndifoka ndi zoipazo,
  • Hymn 1176 Sandinyenga, salephera;
  • Hymn 120 Lekani kubvutika ndi zinthu za padziko,
  • Hymn 1076 Khalatu woyera,
  • Hymn 806 Kapena wina leroli
  • Hymn 345 ATATE, ndipempha
  • Hymn 965 Mundiuze, aulendo,
  • Hymn 922 Onse akulapawo
  • Hymn 522 Akazi anadza
  • Hymn 1054 Ndilira mtima wakulapa
  • Hymn 492 DZIKO lilipolo
  • Hymn 117 Atate wondipatsazo,
  • Hymn 160 MADALITSO ngati mvumbi,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version