Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 354 ATATE, tifika pamaso panu;

  1. Home   »  
  2. Hymn 354 ATATE, tifika pamaso panu;

Hymn 354 ATATE, tifika pamaso panu;

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 354 ATATE, tifika pamaso panu;

 

ATATE, tifika pamaso panu;
Mukomane ndi ife, Mbuye wathu.

Mitima yathu iyi nayo njanu,
Muiyeretse, muikonze Mbuye.

Ndi maso athu awa nawo nganu,
Muŵapenyetse zinthu zanu zokha.

Ndi manja athu awa nawo nganu,
Agwiretu ntchito yanu yokhayo.

Ndi miyendo yathu iyinso njanu,
Ithamange m’ntchito yanu yokhayo.

Ndi milomo yathu iyinso njanu,
Ilalike Mawu anu kwa onse.

Ndi makutu athu awanso nganu,
Muŵamvetse Mawu anu okhawo.

Tidziperekadi konse kwa Inu
Tikakhale anthu anu okhawo.

Post navigation

Previous: Hymn 340 PEMPHERA m’mbanda kucha,
Next: Hymn 361 AMBUYE munapatsa tsiku

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1389 Tithawire kwa Mulungu,
  • Hymn 1319 Ambuye naitana ‘ne:
  • Hymn 81 Imva mawu akewo,
  • Hymn 18 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 497 TILIKUIMBA nyimbo yomweyi,
  • Hymn 1741 Yesu munalaswa m’mtima,
  • Hymn 980 Tiyeni ku nkhondo iyi,
  • Hymn 668 Achisoni, obvutidwa,
  • Hymn 604 ‘Tate, Mwana, Mzimu, ndinu
  • Hymn 743 Mudze, anthuni, talawani ‘nu
  • Hymn 131 Lolani ana, mumve Mlungu,
  • Hymn 1331 Yesu wathu Mbuyeyo
  • Hymn 1129 Mbuyanga Yesu, ndikapanda Inu
  • Hymn 1180 Ndine kapolo wa Mbuye wanga;
  • Hymn 1021 Kunsi kudambo, pena m’mwamba m’phirimo,
  • Hymn 1429 Penyetsetsa Yesu
  • Hymn 1401 Imvani mawu ake, idzanitu,
  • Hymn 1704 Zintchito zakezi
  • Hymn 78 Ndipereka zanga zonse,
  • Hymn 1048 Kumwamba ndiona Ambuyangayo,
  • Hymn 1852 Mbuye ndamva mwawazira
  • Hymn 207 Malo alimo m’nyumba ya Yesu,
  • Hymn 1188 Akumangidwa ndi mzimuwo,
  • Hymn 1204 Ambuyanga Yesu,
  • Hymn 1301 Moyo ukatha zi,
  • Hymn 309 Mwa Mzimu mulowe mumitima yathu,
  • Hymn 1343 M’dzina la Yesuyo
  • Hymn 1577 “Kwa Iye atikonda
  • Hymn 89 INDE, ndifuna kumvatu,
  • Hymn 1747 Yesu aitana ife;
  • Hymn 1475 Anathera pamtanda zintchito zonsezi
  • Hymn 408 Oipa tili tonsefe;
  • Hymn 1504 Kodi ali ndi chilemba
  • Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,
  • Hymn 1744 Kale ophunzira ake
  • Hymn 166 Yendani, Munthu Wachisoni,
  • Hymn 1661 Ndimachitira
  • Hymn 135 Kudziwa ukudziwa,
  • Hymn 156 OKOMA ndiwo mawu
  • Hymn 1624 Koma anthu onse omwe
  • Hymn 755 Pamene padzakhalapo
  • Hymn 440 Yesu wakufatsa mtima
  • Hymn 223 ATI Yesu Mbuyeyo:
  • Hymn 355 DZIKO lonse mlambire
  • Hymn 170 YESU ponong’oneza, idzanitu;
  • Hymn 1736 “Senzani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 967 Mbuye, ndapangana
  • Hymn 229 Woba wakufa ‘napenya
  • Hymn 1079 Khalatu woyera,
  • Hymn 454 TAONANI, m’kholamo,
  • Hymn 937 Chitsime chachikondi
  • Hymn 39 Poyang’ana ena ndi ndalamatu,
  • Hymn 602 Mpulumutsi wakukoma,
  • Hymn 331 Yesu ndimafuna Inu,
  • Hymn 780 Kwezani mitu yanuyo,
  • Hymn 888 Polowa ndi Inu
  • Hymn 1314 Mulungu ali nane!
  • Hymn 857 Mlungu amaunikira
  • Hymn 1083 “Khala mwa Ine,” Yesu anatero;
  • Hymn 1700 Ambuye Mwini moyo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version