Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 336 KULINSO dziko lowala M’mwamba,

  1. Home   »  
  2. Hymn 336 KULINSO dziko lowala M’mwamba,

Hymn 336 KULINSO dziko lowala M’mwamba,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 336 KULINSO dziko lowala M’mwamba,

 

KULINSO dziko lowala M’mwamba,
Kunthawi zosatha;
Komwe kulibe mdima bii,
Yesu ndiye nyaliyo.

Mtandawo tidzasenza,
Korona tidzavala,
Pamodzi ndi oyera,
M’dziko la Kumwambako.

Chikondi chake cha Mlengi wathu,
Natuma Yesuyo;
Kudzatifera tonsefe,
Ndikutipatsa moyo.

Mulitu ulemelero M’mwamba,
Kwa anthu omvera;
Omwe akonda Yesuyo,
Ndikugwira ntchitoyo.

Post navigation

Previous: Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga
Next: Hymn 341 PAKUPEMPHERATU

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 655 Ndiphunzitseni, Mbuyetu,
  • Hymn 177 Tate, ndili mwana wanu,
  • Hymn 1102 Dziko lonse ndilitaya;
  • Hymn 958 Ndikalowa m’mtsinje muja,
  • Hymn 1791 Tiimbe nyimbo zotamanda
  • Hymn 1465 Akulu inu m’bwere nonse,
  • Hymn 529 Zili nazotu nkhwimba zirombozo,
  • Hymn 1610 Waleka koronayo,
  • Hymn 730 A! Yesu mwapangana
  • Hymn 65 NLA Mlungu dzuŵali:
  • Hymn 563 Ndipo Mwana uyu Yesu
  • Hymn 499 ‘Nafera Mbuye wanga
  • Hymn 1420 Abale ‘nu, abale ‘nu,
  • Hymn 195 YESU wondikondadi,
  • Hymn 1181 Adalitsika munthuyo
  • Hymn 333 M’DZIKO lino tikhalamo
  • Hymn 1405 Ati: “Undiuze
  • Hymn 275 Mlungu akuyang’aniredi,
  • Hymn 1019 Tsata, tsata, nditsatadi Yesu;
  • Hymn 1313 Zindichulukirazi
  • Hymn 119 Tamverani anthu inu,
  • Hymn 593 Yesu, munditsogoza
  • Hymn 661 Tamva aku Makedonyako atero,
  • Hymn 699 Inu wakudzatu
  • Hymn 396 Mtitsogolere nthawi zonsezo;
  • Hymn 257 Ndinasiya amayi,
  • Hymn 117 Atate wondipatsazo,
  • Hymn 27 “Msanga ndidzabweratu,
  • Hymn 213 Mawu a Yesu ati: “Msangatu
  • Hymn 1801 Nafuna kwaononga
  • Hymn 132 MVERA mtima wanga ’we
  • Hymn 252 M’dziko lino chimwemwecho
  • Hymn 1675 Lambira Mfumuyo
  • Hymn 150 MIPINGO iyo idzatu,
  • Hymn 1130 Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja
  • Hymn 1048 Kumwamba ndiona Ambuyangayo,
  • Hymn 811 Wopulumutsa mudzetu;
  • Hymn 1139 Namondwe akawombabe,
  • Hymn 476 MBUYE, tili ana anu,
  • Hymn 411 TAMVA mawu omwewo,
  • Hymn 99 Tsopano ndimwona Iye
  • Hymn 479 ANYAMATA inutu,
  • Hymn 753 Getsemane ndionako
  • Hymn 1249 Tsirizani ntchito yanu
  • Hymn 203 NTHAWI yathadi bwerera mbale,
  • Hymn 1734 “Senzani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 172 TADZA kukudyaku,
  • Hymn 201 NDILINKUDZA kwa Ambuye,
  • Hymn 196 Tidzimba komweko nyimbo
  • Hymn 687 Bukitsani mawunso
  • Hymn 1703 Zathedwa zonsetu
  • Hymn 194 AMBUYE’naitan’ne;
  • Hymn 167 Yendanitu, Wansembe wathu,
  • Hymn 182 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 1099 Sindidziwatu zamawa,
  • Hymn 562 Mwa ubwana wake wonse
  • Hymn 794 Ambuye, tasonkhana
  • Hymn 210 Nyumba yodyera ilikudzaza;
  • Hymn 1097 Njira yanga sindidziwa,
  • Hymn 168 Yendani mwaulemerero,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version