Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 334 KULI dziko labwino M’mwamba,

  1. Home   »  
  2. Hymn 334 KULI dziko labwino M’mwamba,

Hymn 334 KULI dziko labwino M’mwamba,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 334 KULI dziko labwino M’mwamba,

 

KULI dziko labwino M’mwamba,
Lakuwala koposa dzuwa;
Yesu watikonzera malo,
Pokhalira ife komweko.

Bwinoli tipita,
Tikomana mwa dziko lija;
Bwinoli tipita,
Tikomana mwa dziko lija.

Tidzayimba komweko nyimbo,
Za abwino omvera Yesu;
Sitidzamva chisoni ife,
Tidzakondwa masiku onse.

Tidzatama Atate wathu,
Kuti Iye ‘napatsa Yesu;
Kuchotsera zochimwa zonse,
Ndikutidalitsatu ife.

Post navigation

Previous: Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga
Next: Hymn 341 PAKUPEMPHERATU

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 945 Tiyeni pamodzi,
  • Hymn 833 Mundilimbitse ndikayese manda ngati mphasayi,
  • Hymn 1206 Ndidzakukondani
  • Hymn 73 Mu ulemerero tidzakhala m’yaya,
  • Hymn 1248 ‘Dzanitu Wamphamvu yonse,
  • Hymn 1043 Mbiri yake ubukitse,
  • Hymn 1802 Mulungu anatuma,
  • Hymn 896 Mbuye, ndinalema ine,
  • Hymn 679 Zipata zachitsulo zitseguke zonse mbee!
  • Hymn 328 KULIBE vuto
  • Hymn 332 Perekani mtima wanu,
  • Hymn 1029 Nkhawa tilibe; Yesuyo
  • Hymn 16 MTIMA wanga lemekeza,
  • Hymn 1576 Khamulo liliko
  • Hymn 1364 Uzani zamphamvu,
  • Hymn 303 Ona pamtanda Yesuyo
  • Hymn 1369 Paphiri paja papakulupo,
  • Hymn 471 YESU Mbuye ’Nu wofatsa
  • Hymn 707 Dalitseni, Mbuye, zonse
  • Hymn 1630 Anthu anu amafoka,
  • Hymn 258 MWA ine, moyo wanga ndi Yesu
  • Hymn 216 Ndi misozi ndi chisoni
  • Hymn 235 ADALITSIKA munthuyo,
  • Hymn 286 ZOVUTA zoopsya ndi zosaukazi
  • Hymn 124 PAMTANDAPO, pamtanda,
  • Hymn 688 Anthu akum’mawa
  • Hymn 31 Tamandani mbuye,
  • Hymn 616 Dziko lathu lonseli
  • Hymn 1132 Mlungu adzandilandila,
  • Hymn 14 Tsiku ndi tsiku timalemekeza;
  • Hymn 1660 Ndikakhumudwa
  • Hymn 680 Mbendera yake ikupiza m’mlengalengamo,
  • Hymn 1564 Mufike monga moto wakuotcha zomwezo.
  • Hymn 178 ZAMBIRI zogona m’kholamo,
  • Hymn 236 Omvana ndi Yesu,
  • Hymn 163 MALO anachepa,
  • Hymn 1052 Ndilira mtima wotamanda
  • Hymn 1226 Wandipatsa moyo wake,
  • Hymn 401 Dzuwa la lero lonseli
  • Hymn 1484 Idzatu, idzatu
  • Hymn 320 Ambuye, wakuti ndi mwaziwo
  • Hymn 1496 Mawu amveke bwino,
  • Hymn 1227 Ndiyamika Mbuye wanga
  • Hymn 717 Ambuye zathu zonsezi
  • Hymn 430 MLUNGU akuyang’aniredí,
  • Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,
  • Hymn 690 Mu ulemerero,
  • Hymn 272 AMBUYE, ndifuna nditsukenitu;
  • Hymn 958 Ndikalowa m’mtsinje muja,
  • Hymn 117 CHOLIMBITSA mtima ndi chonditsogolera;
  • Hymn 641 Awiri aimamu,
  • Hymn 219 Mtenderewo wosanyenga
  • Hymn 477 YESU, muli pa chimpando
  • Hymn 493 DZUŴA li
  • Hymn 1775 Oonadi mtima,
  • Hymn 1742 Yesu ndinu moyo wathu,
  • Hymn 359 TADZUKA mzimu wanga ‘we,
  • Hymn 1210 Kumwamba ndidzanenadi
  • Hymn 504 Pakumyamika Iye
  • Hymn 1559 Wotsogolera, munditsogolere

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version