Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 333 M’DZIKO lino tikhalamo

  1. Home   »  
  2. Hymn 333 M’DZIKO lino tikhalamo

Hymn 333 M’DZIKO lino tikhalamo

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 333 M’DZIKO lino tikhalamo

 

M’DZIKO lino tikhalamo
Utibvuta moyo,
Koma dziko la mtendere
Lili kwa Mulungu.

Watitsogolera Mbuye,
Komwe kwa Atate,
Ndimo tidzatsata naye
Moyo wathu wonse.

Ndi tsopano tilindira
M`dziko lathu lino;
Ntchito atipatsa Mlungu,
Tizigwira bwino.

Ngati zakuipa zathu
Zikatisautsa,
Tithaŵire kwa Mbuyathu,
Atipulumutsa.

Timpemphere kutipatsa
Mtima watsopano,
Kutithandizira kunka
Paulendo uno.

Post navigation

Previous: Hymn 332 NDIKONDWA kuganizirabe
Next: Hymn 334 KULI dziko labwino M’mwamba,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 823 M’mwambamo nyenyezi
  • Hymn 1323 M’manja mopanda kanthu,
  • Hymn 1144 Khalani duu! Ambuye adzatu;
  • Hymn 1515 Ndikachimwa, Bukuli
  • Hymn 74 IDZA wolema,
  • Hymn 1738 “Senzani mtanda wanuwo.”
  • Hymn 1718 Ona chikondi cha Mulungu,
  • Hymn 127 Mwazi wake ndi chitsime changa,
  • Hymn 234 Kwa kutha kwa moyo,
  • Hymn 1724 Ambuye mthandize inetu
  • Hymn 308 Ifetu kuchimwa, Mbuye,
  • Hymn 1408 Kodi mwalandira Yesu?
  • Hymn 254 PAMENE ndisawuka,
  • Hymn 1063 Pokhala mtendere mu mtimangamu,
  • Hymn 331 NDILI ndi kwathu ine,
  • Hymn 1200 Ambuye, m’imfamo
  • Hymn 311 Tifuna kuchita chifuniro chanu,
  • Hymn 303 Ona pamtanda Yesuyo
  • Hymn 1112 Masiku anga onse
  • Hymn 1549 Mtitsutse titachimwa
  • Hymn 310 MBUYE munditsogolere,
  • Hymn 279 Mbwere mudzamve nonse
  • Hymn 26 NDIKULEMEKEZA
  • Hymn 1667 Yesu wakukoma mtima,
  • Hymn 1053 Mtimatu wopirira ndi
  • Hymn 157 Mbuye, Mzimu Woyera
  • Hymn 342 Ambiri,
  • Hymn 1728 Zofuna zanga zonsezo
  • Hymn 21 Mbuye mtsitsimutse!
  • Hymn 83 Mpulumutsi Wokondedwa,
  • Hymn 875 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 1232 Ambuye ndinu Mbusa, Bwenzi, ndi Wansembe wanga,
  • Hymn 492 DZIKO lilipolo
  • Hymn 456 ANA inu, ana inu,
  • Hymn 726 Mundidzze ndi chikondi,
  • Hymn 325 Walira Yesu wolimbitsayo,
  • Hymn 1428 Penyetsetsa Yesu
  • Hymn 1085 “Khala mwa Ine,” ndinu mwini mphamvu,
  • Hymn 52 Mbwere Mzimu, mbwere!
  • Hymn 133 NSEMBE yake ya Kaini,
  • Hymn 721 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 674 Anthu onse taukani,
  • Hymn 481 Yesu wa Kumwamba,
  • Hymn 1749 Chifukwa chipulumutso
  • Hymn 209 Mdima ufika, dzuwa lalowa,
  • Hymn 472 YESU, ndikabwera
  • Hymn 734 Ndi mkate wanu, Yesu
  • Hymn 1809 Yampatsa Nowa yemwe,
  • Hymn 706 Tisaiwalire ‘bale
  • Hymn 4 INU Mulungu, tikuyamikani;
  • Hymn 1605 Yesu, dzina lokondwetsa
  • Hymn 833 Mundilimbitse ndikayese manda ngati mphasayi,
  • Hymn 43 GETSEMANI, Getsemani,
  • Hymn 1223 Ndidzaimba za Mulungu,
  • Hymn 327 NTCHITO yonse yakeyo
  • Hymn 581 Mtiphunzitse bwinotu,
  • Hymn 863 A! maliro m’Mpingo mwanu kulirira ‘balewo
  • Hymn 514 Osanatu, osana,
  • Hymn 222 NDILIKUMVA m’mtima mwanga
  • Hymn 107 MUBWERE kuno Mzimu ’Nu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version