Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 333 M’DZIKO lino tikhalamo

  1. Home   »  
  2. Hymn 333 M’DZIKO lino tikhalamo

Hymn 333 M’DZIKO lino tikhalamo

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 333 M’DZIKO lino tikhalamo

 

M’DZIKO lino tikhalamo
Utibvuta moyo,
Koma dziko la mtendere
Lili kwa Mulungu.

Watitsogolera Mbuye,
Komwe kwa Atate,
Ndimo tidzatsata naye
Moyo wathu wonse.

Ndi tsopano tilindira
M`dziko lathu lino;
Ntchito atipatsa Mlungu,
Tizigwira bwino.

Ngati zakuipa zathu
Zikatisautsa,
Tithaŵire kwa Mbuyathu,
Atipulumutsa.

Timpemphere kutipatsa
Mtima watsopano,
Kutithandizira kunka
Paulendo uno.

Post navigation

Previous: Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga
Next: Hymn 341 PAKUPEMPHERATU

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1374 Inu mumvere anyamatawo,
  • Hymn 1170 Pamtanda wake
  • Hymn 1360 Ndi Aleluya imbirani
  • Hymn 377 Yehova, Mbusa wangadi,
  • Hymn 37 YESU analikhanda
  • Hymn 487 INE ndine mlendo
  • Hymn 256 NGATI mtima sumakonda
  • Hymn 1607 Yesu, dzina ndi lomweli
  • Hymn 31 MULUNGU Wamkulu,
  • Hymn 917 Ndi nkhondo ikaleka
  • Hymn 212 Onse am’Mwamba ali mowemo,
  • Hymn 1453 Mukana Iye bwanji,
  • Hymn 976 Muyendenso kunka komwe,
  • Hymn 1108 Khala chete mtima wanga,
  • Hymn 219 YESU Mbuyetu, mwafera
  • Hymn 1644 Popachikidwa pa Golgotapo
  • Hymn 472 Amakumbukira zonse
  • Hymn 56 KU Mzinda wakuyerawo
  • Hymn 810 Tsopano lino kwada bii,
  • Hymn 322 Walira Yesu m’dziko linoli,
  • Hymn 275 Mlungu akuyang’aniredi,
  • Hymn 1505 Ndikampeza, ndikamtsata
  • Hymn 1721 Mapazi ake namvatu
  • Hymn 1316 Ndabwera kwa Ambuyeyo:
  • Hymn 1206 Ndidzakukondani
  • Hymn 1594 Chikondano chakechi
  • Hymn 193 THANTHWE long’ambikatu,
  • Hymn 147 MUSAŴALOLE mawuwo
  • Hymn 310 Tafika kwa inu mutiunikire,
  • Hymn 302 Anasenza m’thupi mwake;
  • Hymn 281 Atate, ndipempha
  • Hymn 965 Mundiuze, aulendo,
  • Hymn 444 YEMWE afesa nalira,
  • Hymn 1422 Abwenzi ‘nu, abwenzi ‘nu,
  • Hymn 1212 Zina ndi zinanso
  • Hymn 1826 Amadyetsa Iye mbalame zam’mwamba,
  • Hymn 958 Ndikalowa m’mtsinje muja,
  • Hymn 1084 “Khala mwa Ine,” munachotsa tsoka,
  • Hymn 865 Pakubweradi Woyesa tidzamlaka ifetu;
  • Hymn 1515 Ndikachimwa, Bukuli
  • Hymn 20 CHIKONDI cha Mulungu wathu,
  • Hymn 1798 Mukondwe anthu a Mulungu,
  • Hymn 1476 Mipingo iyo idzatu,
  • Hymn 403 NDIYIMBA ndi chimwemwe lero,
  • Hymn 165 ATATE,’nu, atate ’nu,
  • Hymn 1395 Mulungu ali nane!
  • Hymn 212 NDI MISOZI, ndi chisoni,
  • Hymn 476 MBUYE, tili ana anu,
  • Hymn 1606 Yesu, dzina lakufatsa,
  • Hymn 121 MULUNGU, anthu ’fe
  • Hymn 1456 Pakuti anthu akumvera
  • Hymn 225 Yesu akhazika
  • Hymn 348 CHIKHULUPIRIRO chathu
  • Hymn 404 Dzuwa la lero lonseli
  • Hymn 713 Ambuye, Mwini zonsezi,
  • Hymn 1068 Ambuye, thandizenitu
  • Hymn 66 Chisomocho chachotsadi
  • Hymn 346 Aitana,
  • Hymn 108 Tikondwera ife tonse
  • Hymn 687 Bukitsani mawunso

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version