Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 329 MUMZINDA wa Mulungu

  1. Home   »  
  2. Hymn 329 MUMZINDA wa Mulungu

Hymn 329 MUMZINDA wa Mulungu

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 329 MUMZINDA wa Mulungu

 

MUMZINDA wa Mulungu
Moyera mulimo,
Ndiye amathu omwe
Olera ifewo;
Mitima yathu yomwe
Ikondwereratu,
Nikhala nawo Mzinda
Wakukongolawu.

Akondwerera anthu Zokoma zonsezi
Za midzi ya padziko
Lapansi lonseli;
Mtendere wake koma
Wa Mzinda wathuwo
Upambanditsa zonse
Zapansi pomwepo.

Ndi nkhondo ikaleka
Kwa Mlungu komweko,
Ndi ukapolo watha,
Udani wathanso;
Ndi zakuopsa zonse
Ndi zosauka zii!
Ndi mwayi wa kwa Mlungu
Udzoza mutu tho!

Post navigation

Previous: Hymn 328 KULIBE vuto
Next: Hymn 330 N’LOKOMA Dziko langa!

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 402 M’mtima mwangamu mlowemo,
  • Hymn 933 M’mene imfa yathu idza,
  • Hymn 204 Kumandako, kumanda
  • Hymn 633 Tikasokera m’njira mutilondolere ndithu,
  • Hymn 1853 Etu ine, etu ine,
  • Hymn 1418 Khulupirani kuti mukalowe m’Mwambamo,
  • Hymn 990 Poyesedwa ine
  • Hymn 222 Ndilikudzatu,
  • Hymn 124 PAMTANDAPO, pamtanda,
  • Hymn 1479 Ndi Yesu yemwe kalelo
  • Hymn 279 Mbwere mudzamve nonse
  • Hymn 584 Ndi angelo,
  • Hymn 945 Tiyeni pamodzi,
  • Hymn 685 Tamva mawu amwewo
  • Hymn 481 Yesu wa Kumwamba,
  • Hymn 1272 Muyambe ntchito yanuyi,
  • Hymn 1217 Chisoni chonsecho
  • Hymn 326 TSIKU Iidzafika mbale,
  • Hymn 867 Akristu ndi abale, tiziyenderana tonse,
  • Hymn 1299 Mzimu mndipatseko,
  • Hymn 574 A! Yesu Mbuye wakuyera,
  • Hymn 433 MULUNGU wa Kumwamba bwera kunoku
  • Hymn 169 M’manda nagonamo
  • Hymn 1695 Pokumbukira mtandawo
  • Hymn 1513 M’Bukuli ine ndi
  • Hymn 383 Zokoma ndi zakuyanja
  • Hymn 117 CHOLIMBITSA mtima ndi chonditsogolera;
  • Hymn 344 M’watame,
  • Hymn 1128 Mbuyanga Yesu, mundisunge ine
  • Hymn 1068 Ambuye, thandizenitu
  • Hymn 1585 Dzina ili ndi lokoma
  • Hymn 445 Mlewe oipawo,
  • Hymn 82 Mlendo wa Kumwambayo
  • Hymn 46 O! ufulu tigwirizane
  • Hymn 51 Mbuye dalitsani Afrika,
  • Hymn 215 TATE ndili mwana wanu,
  • Hymn 26 NDIKULEMEKEZA
  • Hymn 301 MBUYE, ndapangana
  • Hymn 294 POYESEDWA ine
  • Hymn 395 Usiku uno mutisungedi,
  • Hymn 274 E! tidzakomanansotu
  • Hymn 359 TADZUKA mzimu wanga ‘we,
  • Hymn 1335 Wandifera Yesuyo
  • Hymn 763 Ndiponso m’manja chikhocho
  • Hymn 1608 Yesu, dzina lakukonda
  • Hymn 238 MULUNGU wanga,
  • Hymn 1795 A! chikondi chachikulu
  • Hymn 1457 Ndidziwa kuti Yesu
  • Hymn 936 Ukatha moyo wanga
  • Hymn 461 ANA inu, myamikeni
  • Hymn 1828 Timtamande Iye ndi moyo wathunso
  • Hymn 123 Koma mudzisungire chuma cha Kumwamba
  • Hymn 229 Woba wakufa ‘napenya
  • Hymn 43 GETSEMANI, Getsemani,
  • Hymn 1571 Tamani mphamvu ya Yesu,
  • Hymn 1630 Anthu anu amafoka,
  • Hymn 656 Ndipumulire panupo,
  • Hymn 669 Anyamata limikani,
  • Hymn 1812 Kuzani Mlungu m’Mwambamo,
  • Hymn 1078 Khalatu woyera

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version