Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga

  1. Home   »  
  2. Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga

Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga

 

NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga
Amva pemphero ndi kulira kwanga,
Namachereza khutu nditapfuula,
Andithandiza, nandipulumutsa.

Mulungu wanga ndiye wachifundo
Ndi wolungama mtima ndi wabwino;
Apulumutsa anthu akufoka,
Akathandiza nkhaŵa imachoka.

Mtimanga, bwera kuti upumule,
Wakuchitiranso zokoma Mbuye,
Wakuchotsera imfa ndi misozi,
Ndingakhumudwe asungira phazi.

Nditani ine kubwezera Mbuye
Zokoma zonse anandichitira?
Chipulumutso chake ndidzatama,
Ndinalumbira zija ndidzapatsa.

Imfa ya anthu ake imkomera,
Aŵalandira m’nyumba zokonzeka.
Mbuye, kapolo wanu ndipereka
Nsembeyi yonga yanu, ndine ndekha.

Post navigation

Previous: Hymn 300 AKRISTU limbikani,
Next: Hymn 321 PAKUONA imfayo

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 607 Dziko lonse lilikukondwa, mlengalenga mpheponso,
  • Hymn 259 Zoipa zakanikadi,
  • Hymn 18 POKHALA Inu
  • Hymn 51 Mbuye dalitsani Afrika,
  • Hymn 1523 Atisangalatsa,
  • Hymn 441 Tamverani, aitana:
  • Hymn 1024 Anasauka Mbuyeyo,
  • Hymn 1139 Namondwe akawombabe,
  • Hymn 205 KWA Inu Yesu ndilira,
  • Hymn 253 YESU ndinutu wanga m’njira zonse,
  • Hymn 434 Zondipingitsa zonse
  • Hymn 1402 Mverani Iye ati: idzanitu;
  • Hymn 888 Polowa ndi Inu
  • Hymn 789 Ndi lokoma m’Mwambamo,
  • Hymn 49 Ndi ife akudziwa
  • Hymn 663 Anyamata a Mulungu,
  • Hymn 1712 E! Yesu Mbuye wangadi,
  • Hymn 1550 Kutiyeretsa m’mtima
  • Hymn 378 Ku madzi ake odikha
  • Hymn 1489 Idzanitu, idzanitu,
  • Hymn 413 ZIPATA zachitsulo zitseguke zonse mbee!
  • Hymn 1091 Mulamulire mtima, Yesu,
  • Hymn 861 Mbuye, Mpingo wanu usauka kwa kukuludi;
  • Hymn 457 Palibe mwana wakuchepa
  • Hymn 198 CHITSIMECHO cha mwaziwo
  • Hymn 883 Pokupempherani
  • Hymn 1574 Anthu ose ndi mitundu
  • Hymn 551 Ndani kodi Munthuyo
  • Hymn 363 ATATE ndiyamika,
  • Hymn 295 Kubadwa kwa Yesu
  • Hymn 1410 Nthawi zonse mufunabe
  • Hymn 1268 Mundilandiretu,
  • Hymn 502 Ndikonda mbiri yomwe
  • Hymn 260 ODALA ndi onsewo,
  • Hymn 74 IDZA wolema,
  • Hymn 244 TIMVE za anamwali khumi,
  • Hymn 1790 Imfa ya anthu ake imkomera,
  • Hymn 1714 Tiyeni, dzalireni nane,
  • Hymn 66 >ALELUYA, Aleluya, Aleluya!
  • Hymn 1086 “Khala mwa Ine,” ndinu mwini moyo,
  • Hymn 1096 Tifuna Inu, Mbuye,
  • Hymn 3 TIMYAMIKIRE Mlunguyo,
  • Hymn 1258 Zonse zina sizikwana,
  • Hymn 938 A! Yesu Bwenzi langa
  • Hymn 936 Ukatha moyo wanga
  • Hymn 40 Padziko pano tikhalira
  • Hymn 1535 Lichepa dontho lokhali,
  • Hymn 242 M’mene mubwera
  • Hymn 6 LEMEKEZA Mulungu ’Tate,
  • Hymn 1858 Ha! Chikondi cha Mulungu,
  • Hymn 1794 Mulungu awakonda anthu
  • Hymn 1360 Ndi Aleluya imbirani
  • Hymn 1412 Imfa idzafika msanga;
  • Hymn 188 Ine ndili ndi manyazi
  • Hymn 1585 Dzina ili ndi lokoma
  • Hymn 507 Yesu ndimkonda, akondanso ine,
  • Hymn 188 MPULUMUTSI Wokondedwa,
  • Hymn 151 Inde, Yesu, mulandira,
  • Hymn 1525 Mbuye, mtiphunzitse
  • Hymn 301 MBUYE, ndapangana

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version