Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,

Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,

 

TIYENI, Akristu inu,
Mumenyane nkhondo iyi,
Mukafoka nonse, koma
Yesu akulimbitsani.

Muyendanso kunka komwe,
Mugonjetse mdani wanu;
Musafoke, musaleme,
Musagone konse inu.

Musagonje, anthu inu,
Mtamiretu Yekha Mbuye;
Ipambana mphamvu yake,
Ya Mtsogoli wanu yemwe.

Mtima wanu wonse ndithu
Udzakhala ndi chimwemwe.
Zida zanu mbvale bwino
Zakudzera m’Mwamba momwe.

Limbikani inu nonse,
Msangalalo ngwanu nokha;
Musaope kanthu kena
Mumtamire Mbuye Yekha.

Tiyeni ku nkhondo iyi,
Mugonjetse zonse konko;
Muingitse mdani uja,
Muyendetse m’njira momwemo.

Post navigation

Previous: Hymn 280 YESU, afuna iwe unke kwawoko,
Next: Hymn 301 MBUYE, ndapangana

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1151 Pomulambira Yesu Mbuyanga,
  • Hymn 610 Nafenso tidzadzuka kwa ‘ke ngati maluwawo,
  • Hymn 179 TUMPHATUMPHA moyo wanga,
  • Hymn 1745 Yesu aitana ife:
  • Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga
  • Hymn 1746 Mwachimwemwe, mwachisoni,
  • Hymn 58 Titasokera tinabwerera,
  • Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,
  • Hymn 169 ’MVANI liu lomwe
  • Hymn 220 MULUNGU mundichitire chifundo,
  • Hymn 1385 Anatsogolera kale
  • Hymn 159 Kamwana Yesu ‘nabadwa,
  • Hymn 1022 Mbuye, nditsate bwanjiko?
  • Hymn 1456 Pakuti anthu akumvera
  • Hymn 1454 Ambuye, musendeze
  • Hymn 874 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 1781 Timwimbire nyimbo,
  • Hymn 73 Mu ulemerero tidzakhala m’yaya,
  • Hymn 967 Mbuye, ndapangana
  • Hymn 1471 Ukapenya kwa Yesu uliko moyoko,
  • Hymn 19 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 1574 Anthu ose ndi mitundu
  • Hymn 267 Usekere moyo wanga,
  • Hymn 456 ANA inu, ana inu,
  • Hymn 402 M’mtima mwangamu mlowemo,
  • Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,
  • Hymn 1113 Mtima wa Mbuyako
  • Hymn 1185 Imfa ndi mfumu ya mdimawo,
  • Hymn 1101 Ngati mtima sumakonda
  • Hymn 252 M’dziko lino chimwemwecho
  • Hymn 1747 Yesu aitana ife;
  • Hymn 831 Mundikumbutse, ndikapanda tulo, za Kumwambako;
  • Hymn 664 Komwe asauka anthu
  • Hymn 1265 Tere moyo wanga wonse,
  • Hymn 1016 Mbuye, mwatiuza ‘fe
  • Hymn 223 ATI Yesu Mbuyeyo:
  • Hymn 1624 Koma anthu onse omwe
  • Hymn 1501 Inde, pakufa panga
  • Hymn 92 KONDA dzinalo la Yesu,
  • Hymn 684 Zipata zatsegudwa mbee! Za m’dziko monsemo;
  • Hymn 1216 Ndatsatatsatabe
  • Hymn 127 Mwazi wake ndi chitsime changa,
  • Hymn 588 Mlungu, Inutu,
  • Hymn 1282 Ndilinkudza kwa Ambuye,
  • Hymn 1105 Khala chete mtima wanga
  • Hymn 1388 Tiimbire Mlungu wathu
  • Hymn 1521 Poyensedwa ife
  • Hymn 105 Tiyamike Mbuye Yesu
  • Hymn 373 NYUMBA ya Mulungu, ili pano,
  • Hymn 333 M’DZIKO lino tikhalamo
  • Hymn 132 MVERA mtima wanga ’we
  • Hymn 1106 Mlungu ndi wachikhalire.
  • Hymn 1383 Dzina lake tibukitsa,
  • Hymn 172 TADZA kukudyaku,
  • Hymn 1010 Ndipo ngati ungolema,
  • Hymn 929 Chikondano sichifera;
  • Hymn 333 Perekani, perekani
  • Hymn 1669 Ukafuna kumdziwitsa,
  • Hymn 460 E! ang’ono ndifetu,
  • Hymn 97 TIYAMIKE Mlunguyo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version