Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,

  1. Home   »  
  2. Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,

Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,

 

IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,
Zachisautso chomwechili nkudza;
Cha nambala ya a sikisi atatu;
Kodi tidzapiliradi?

Kodi inu mayi mudzapiliradi
Kuyenda inu wausiwa.
Kodi inu bambo mudzapiliradi
Panthawi ya masautsowo?

Zizindikirozo zili kuwoneka,
Kutitu nkhondoyo yayandikadi;
Tisakhaletu odabwitsika konse,
Tilimbike kupemphera.

Tidzawona ena a ifetu zedi,
Tili kudindidwa pamphumi pathu;
Tidziwetu kuti sitinalembedwe,
Mayina m’buku mulibe.

Post navigation

Previous: Hymn 280 YESU, afuna iwe unke kwawoko,
Next: Hymn 301 MBUYE, ndapangana

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 275 NTHAWI yathu yafikatu,
  • Hymn 235 ADALITSIKA munthuyo,
  • Hymn 1568 Kudzoza kwanu kutipatsa
  • Hymn 1098 M’mene mantha andigwira,
  • Hymn 165 Yendanitu m’ulemudi,
  • Hymn 198 CHITSIMECHO cha mwaziwo
  • Hymn 395 AMBUYE, Mwini zonsezi,
  • Hymn 239 TILI ndi mtendere
  • Hymn 326 TSIKU Iidzafika mbale,
  • Hymn 68 M’MANDA, nagonamo
  • Hymn 1625 Ife tonse tikumbuke
  • Hymn 476 Mpaka ndabvala mbuu!
  • Hymn 261 Munafera pa mtanda
  • Hymn 1190 Aleluya, mlemekeze,
  • Hymn 1331 Yesu wathu Mbuyeyo
  • Hymn 59 IMVANI uthenga,
  • Hymn 401 Dzuwa la lero lonseli
  • Hymn 1622 Anthu onse amlambire
  • Hymn 389 NDIMAMVA njala, Yesu,
  • Hymn 26 “Ndakukonda ku imfa
  • Hymn 1666 Yesu, ndinutu chitsime
  • Hymn 1347 Akukonda, akukonda,
  • Hymn 476 MBUYE, tili ana anu,
  • Hymn 759 Ndilawako tsopanoli
  • Hymn 363 Funani Mlungu tsopano,
  • Hymn 1844 Pamaso pa adaniwo mwayala gome langa;
  • Hymn 266 Ukondwere moyo wanga,
  • Hymn 373 Ayamikire ‘Nu
  • Hymn 372 Potero onsewo
  • Hymn 93 Mverani mbiri yozizwitsa
  • Hymn 78 ALINKUDZA wansoni Munthu,
  • Hymn 1800 Kalelo anthu onse
  • Hymn 128 ANTHU m’maiko onse
  • Hymn 96 MTIMA wanga uyamiketu,
  • Hymn 120 MUNDINYEMERE ’ne
  • Hymn 220 Kalekale ndinathawa,
  • Hymn 1780 Titame Mlungu Wakumwamba,
  • Hymn 555 Mkucha wake ndaniyo
  • Hymn 392 Chimwemwe chomwe mpatseko
  • Hymn 371 Mulungu, anthu ‘fe
  • Hymn 1082 Ndidzaonana nanu
  • Hymn 194 AMBUYE’naitan’ne;
  • Hymn 917 Ndi nkhondo ikaleka
  • Hymn 191 Sindifuna Mbuye wina,
  • Hymn 154 SING’ANGA ‘mkulu ndiye Yesu,
  • Hymn 1638 Alinkudza wansoni Munthu
  • Hymn 1454 Ambuye, musendeze
  • Hymn 598 Mlungu ali nane;
  • Hymn 1587 Nditama Mlungu m’mtimamo,
  • Hymn 383 KASUPE ali wodzaza
  • Hymn 1808 Kutuma wabwereza,
  • Hymn 1173 Sindinanyengedwa konse
  • Hymn 1121 Ndifuna Yesuyo,
  • Hymn 432 Ulendo ungoyamba
  • Hymn 1108 Khala chete mtima wanga,
  • Hymn 422 DZIKO lonse lapansi,
  • Hymn 1614 Anabadwa,
  • Hymn 1546 Mubwere Mzimu Inu
  • Hymn 181 Zonse ndinakonda kale
  • Hymn 295 AMBUYE wa Kumwamba,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version