Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 291 ULENDO wachikhrisitu ngosawutsa ndithu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 291 ULENDO wachikhrisitu ngosawutsa ndithu,

Hymn 291 ULENDO wachikhrisitu ngosawutsa ndithu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 291 ULENDO wachikhrisitu ngosawutsa ndithu,

 

ULENDO wachikhrisitu ngosawutsa ndithu,
Mavuto, mayesero adza kwa ine;
Komatu ndidziŵitsitsa kuti Mbuye wanga,
Asunga moyo wanga kosalekeza.

Ndine wanu Mbuye wanga,
Mavuto, mayesero adza kwa ine;
Komatu ndidziwitsitsa
Kuti Mbuye wanga,
Asunga moyo wanga kosalekeza.

Chifukwa cha dzina lake
Ndanyozedwa ‘ne,
Adani achuluka, ndachepa ine;
Ndiwakonda onse
Koma andisautsa ‘ne,
Pukutani m’maso mwanga misoziyi.

Tiyeni abale tonse
Tilimbe ndithu,
Pogwira ntchito zake
Za Mbuye wathu;
Iye analonjezatu
Tsiku lomaliza,
Tidzakhala muulemelero wake.

Post navigation

Previous: Hymn 280 YESU, afuna iwe unke kwawoko,
Next: Hymn 301 MBUYE, ndapangana

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1388 Tiimbire Mlungu wathu
  • Hymn 346 PEMPHERO ndiko kufuna,
  • Hymn 1745 Yesu aitana ife:
  • Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,
  • Hymn 553 M’munda muja ndaniyo
  • Hymn 428 Tiyandika, Mbuye,
  • Hymn 638 Ndi Mzimutu Woyera
  • Hymn 1546 Mubwere Mzimu Inu
  • Hymn 38 ANGELO ayimba,
  • Hymn 1217 Chisoni chonsecho
  • Hymn 439 MLUNGU wathu mwatifitsa
  • Hymn 1788 Mtimanga, bwera kuti upumule
  • Hymn 630 Ena atsagana nafe
  • Hymn 1204 Ambuyanga Yesu,
  • Hymn 415 PAMAYIKO pali mdima,
  • Hymn 1278 Kuti muyeretsa mtima ndibvomeratu;
  • Hymn 1644 Popachikidwa pa Golgotapo
  • Hymn 383 KASUPE ali wodzaza
  • Hymn 1198 Mabala ake m’manja
  • Hymn 599 Mlengi wathu Wakuyera,
  • Hymn 1332 Imba kawiri ndi kawirinso,
  • Hymn 999 Amaliwongo ochuluka amalowa m’mtima
  • Hymn 1035 Mphamvu zathu zonse
  • Hymn 1449 Pena imfa idza mawa,
  • Hymn 327 NTCHITO yonse yakeyo
  • Hymn 1334 Walandira inetu
  • Hymn 175 A! MBUSA wathu amvatu
  • Hymn 221 Yesu and’itana,
  • Hymn 1547 Mtisangalatse m’zonse,
  • Hymn 1744 Kale ophunzira ake
  • Hymn 1359 Ndi Aleluya imbirani
  • Hymn 243 Mtima wanga udzakondwera,
  • Hymn 1680 Aleluya, Aleluya, Aleluya!
  • Hymn 388 Ambuye, Mzimu wanu
  • Hymn 1724 Ambuye mthandize inetu
  • Hymn 1173 Sindinanyengedwa konse
  • Hymn 859 Pakufika tsidya lija,
  • Hymn 581 Mtiphunzitse bwinotu,
  • Hymn 331 Yesu ndimafuna Inu,
  • Hymn 128 Yesu Mfumu, ine ndingadzafe
  • Hymn 872 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 449 MLENGI wathu Woyeranu,
  • Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,
  • Hymn 1148 Ndiimba mumtima mokondwa
  • Hymn 904 Komweko akhala Yesuyo
  • Hymn 313 Muthire, Yesu, m’mtimanga
  • Hymn 683 Musamaopa kanthu ‘yi, tamani Yesuyo;
  • Hymn 370 KWACHA lero kwati mbee,
  • Hymn 1829 Mulungu ndiye Mbusa wanga, sindisowa konse;
  • Hymn 1077 Khalatu woyera,
  • Hymn 1161 Wapumitsa mtima wanga,
  • Hymn 1681 Mphamvu za imfa ndi za Satana
  • Hymn 510 Ngolizo zilira
  • Hymn 1743 M’kati mwa zobvuta zathu
  • Hymn 1171 Mulungu wanga
  • Hymn 655 Ndiphunzitseni, Mbuyetu,
  • Hymn 407 Zochimwa sizilowako,
  • Hymn 1795 A! chikondi chachikulu
  • Hymn 426 Mpulumutsi Yesu,
  • Hymn 98 Ndidzamwona maso ndi maso

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version