Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 285 DZIKO lino lapansi,

  1. Home   »  
  2. Hymn 285 DZIKO lino lapansi,

Hymn 285 DZIKO lino lapansi,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 285 DZIKO lino lapansi,

 

DZIKO lino lapansi,
Moyo ndi wovuta;
Nthawi zina kuseka,
Nthawi zina kulira;
Komatu Ambuye wathu,
Amatisamalira;
Mbale wanga pilira.

Pilira, pilira, mbale wanga pilira,
Dziko lino ndi lovuta
Mbale wanga pilira;
Linadana naye Mwana wa Mulungu,
Mbale wanga pilira.

Zabwino zimabwera,
Ndipo zimapita;
Dziwa kuti Ambuye,
Afunitsa iwedi;
Kuti ugwiretu ntchito,
Yakeyi m’dziko lino;
Mbale wanga pilira.

Tsikulo lilinkudza,
Lomwe Mbuye Yesu;
Adzanena kwa iwe,
Bwera upumuletu;
Kuzovuta ndi zowawa,
Zam’dziko lapansili;
Mbale wanga pilira.

Post navigation

Previous: Hymn 280 YESU, afuna iwe unke kwawoko,
Next: Hymn 301 MBUYE, ndapangana

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 452 MLUNGU, Inutu,
  • Hymn 858 Anthu osawerengeka
  • Hymn 299 “Posunga nkhosa ife
  • Hymn 289 Ndi manja athu awa nawo nganu,
  • Hymn 1192 Pamtanda woopsa
  • Hymn 478 YESU atiuza tiŵale ’fe.
  • Hymn 11 NDI mitima yokondwera,
  • Hymn 40 Padziko pano tikhalira
  • Hymn 367 Nonse okhala pansipa,
  • Hymn 1376 Akulu nonse ndi mafumu ‘nu,
  • Hymn 1130 Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja
  • Hymn 490 YESU adza kuwerenga,
  • Hymn 450 YESU, munditsogoza
  • Hymn 963 Aulendo, munka kuti
  • Hymn 190 Nsiku zonse kwanja kwake
  • Hymn 1159 Mwalembedwa mukalata
  • Hymn 1680 Aleluya, Aleluya, Aleluya!
  • Hymn 1609 Idzani nose’nu
  • Hymn 237 SINDINANYENGEDWA konse
  • Hymn 1855 Yesu, msandipitirire
  • Hymn 1299 Mzimu mndipatseko,
  • Hymn 1554 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 940 Ndamvatu kuti tifika komweko
  • Hymn 158 Mzimu, mlonge m’mtimamo
  • Hymn 323 Tiwaliretu, tiwaliretu
  • Hymn 1178 Mawu omwewo, nyimbo yomweyi,
  • Hymn 693 Adzapambana Yesu ponse
  • Hymn 1443 Ambuye Yesu anatsira
  • Hymn 350 Yesu ati,
  • Hymn 514 Osanatu, osana,
  • Hymn 1661 Ndimachitira
  • Hymn 813 Wopulumutsa, Inunso
  • Hymn 428 MBUYE mtsitsimutse
  • Hymn 238 Mbuye Yesu, lowani m’mtima,
  • Hymn 1225 Ndinachita mphulupulu,
  • Hymn 201 NDILINKUDZA kwa Ambuye,
  • Hymn 231 AMBUYE, m’imfamo
  • Hymn 772 Muwalimbikitse onse
  • Hymn 864 Ndi chikondi mtithandize kuigwira nkhondoyi;
  • Hymn 1057 Ndilira ine kukayenda
  • Hymn 1322 Ntchito zanga zonsezo
  • Hymn 160 Kamwana kaja ‘nayamba
  • Hymn 1063 Pokhala mtendere mu mtimangamu,
  • Hymn 1328 Ndani afuna kunkako
  • Hymn 1302 Ndi inetu sinditha ‘yi
  • Hymn 298 “Tadodoma, abusa,
  • Hymn 1849 Nthawi zonse monga ‘Tate
  • Hymn 826 Mutonthoze mtima
  • Hymn 440 Yesu wakufatsa mtima
  • Hymn 1004 A! mizimu yakuipa
  • Hymn 1408 Kodi mwalandira Yesu?
  • Hymn 349 Aitana,
  • Hymn 670 Isaleke ntchito yake
  • Hymn 785 Yehova adalitse ‘nu,
  • Hymn 106 Ife, tapulumukadi,
  • Hymn 478 Ndife ana, mutikonda,
  • Hymn 511 Ntchito zake zatha,
  • Hymn 17 MULUNGU ndiye Mbusa wanga,
  • Hymn 135 Kudziwa ukudziwa,
  • Hymn 1403 ‘Mvani liwu lomwe

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version