Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 28 AMBUYE ngwodalitsika,

  1. Home   »  
  2. Hymn 28 AMBUYE ngwodalitsika,

Hymn 28 AMBUYE ngwodalitsika,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 28 AMBUYE ngwodalitsika,

 

AMBUYE ngwodalitsika,
Mulungu wa Israyeli ndiye,
Poti anayang’ana naŵawombola anthu ake,

Napulumutsa tonse mwapfuko la Davide mwana wake;
Monga analankhula mwa aneneri ake,

Adzatipulumutsa kudzanja la onse akutida,
Ndipo adzachitira akulu chifundo ndi chisoni.

Ndiye akumbukira pangani loyera lake lija,
Ndi chilumbiro chake cha kwa atate Abrahamu,

Choti timtumikire osaŵaopa ’dani athu,
Ndi kuyeranso mtima mwa chilungamo nsiku zonse.

Mwana, adzakuyesa mneneritu wa Wamkulukulu,
Ndiwe udzakonzera njira ya Mbuye Wakumwamba.

Udzadziŵitsa anthu za Mpulumutsi wawo yemwe
Aŵakhululukira
Nafafaniza tchimo lawo,

Poti Mulungu wathu ali ndi mtima wachifundo.
Ndiye kumwamba komwe
Ationetsa mbanda kucha,

Poŵalitsira omwe ali mumdima ndi muimfa,
Ndi potilunjikitsa tonse munjira yamtendere.

Post navigation

Previous: Hymn 20 CHIKONDI cha Mulungu wathu,
Next: Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 28 AMBUYE ngwodalitsika,
  • Hymn 743 Mudze, anthuni, talawani ‘nu
  • Hymn 1389 Tithawire kwa Mulungu,
  • Hymn 384 USIKU uja kalero,
  • Hymn 1363 Tamani Ambuye,
  • Hymn 1650 E, moyo wanga’we
  • Hymn 1081 Ndikabisala mwanu
  • Hymn 378 KWEZANI mitu yanuyo,
  • Hymn 265 Imbirira moyo wanga,
  • Hymn 1766 Ndilikulemekeza
  • Hymn 1692 Timwimbire zomtamanda, Aleluya
  • Hymn 1701 Nditani Bwenzi langa
  • Hymn 466 OSANATU, osana,
  • Hymn 1560 Mthandizi ndinu, mndithangate ine
  • Hymn 1351 Aleluya, Aleluya,
  • Hymn 361 Munka kangati kulawa
  • Hymn 325 Walira Yesu wolimbitsayo,
  • Hymn 1243 Kodi mayi wobereka
  • Hymn 690 Mu ulemerero,
  • Hymn 695 Pomveka konsekonse mbiri
  • Hymn 1476 Mipingo iyo idzatu,
  • Hymn 1043 Mbiri yake ubukitse,
  • Hymn 1052 Ndilira mtima wotamanda
  • Hymn 1614 Anabadwa,
  • Hymn 1620 Aleluya,
  • Hymn 61 Ndi chimwemwe ndimaona
  • Hymn 1677 Zomkweza zili m’Mwamba,Aleluya
  • Hymn 1644 Popachikidwa pa Golgotapo
  • Hymn 256 NGATI mtima sumakonda
  • Hymn 1154 Zakutsogolo sitidziwa ‘yi;
  • Hymn 1841 Kumadzi kuli njiratu andiyendetsa bwino,
  • Hymn 1460 Akuti anthu akumvera
  • Hymn 282 Ine ndili munthu
  • Hymn 192 ZAKEYU mkulu wa misonkho,
  • Hymn 31 Tamandani mbuye,
  • Hymn 1359 Ndi Aleluya imbirani
  • Hymn 753 Getsemane ndionako
  • Hymn 1829 Mulungu ndiye Mbusa wanga, sindisowa konse;
  • Hymn 1266 E, chimwemwe chachikulu, N’taperekadi
  • Hymn 438 TIYAMIKE Ambuye,
  • Hymn 211 Chakudya ichi ndi cha iwenso,
  • Hymn 596 Mlungu ali nane;
  • Hymn 1570 Mutidziwitse ‘Tate wathu,
  • Hymn 1552 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 1493 Mbiri yakalelomwe
  • Hymn 1548 Mtitsitsimutse ife
  • Hymn 39 MUNASIYATU dziko lanulo,
  • Hymn 1584 Konda dzinalo la Yesu
  • Hymn 359 Tonse timyamiketu,
  • Hymn 1676 Kondwerani dzuwa lino Aleluya,
  • Hymn 244 TIMVE za anamwali khumi,
  • Hymn 1342 Tadza kumtsinjeku
  • Hymn 1458 Satana ndi unyolo
  • Hymn 133 Yesu watidzera, watidzera,
  • Hymn 1672 Lambira Mfumuyo,
  • Hymn 130 Tidzakondweradi m’Mwambamo
  • Hymn 1604 Yesu, dzina lakukonda,
  • Hymn 944 Tiyeni nonsenu okonda Yesuyo,
  • Hymn 1549 Mtitsutse titachimwa
  • Hymn 294 Yesu anali khanda

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version