Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,

  1. Home   »  
  2. Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,

Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,

 

USAFUNE chuma chokha,
Pena masewero okha;
Koma za Mulungu zokha,
Zipambana zinazo.

Ukafuna kulemera,
Pempha chuma chosathera;
Ndiwo mtima wakuyera,
Ndi wokonda Yesuyo.

Zosawutsa uvomere,
Ndipo Yesu chaulere;
Chikondano ndi mtendere,
Alowetsa m’mtimamo.

Zonse umazinyadira,
Udzaleka kusilira;
Uli nazo zokwanira,
Pakupeza Yesuyo.

Mbiri yake ubukitse,
Anthu onse nuphunzitse;
Kwa Mulungu nufikitse,
Osokera onsewo.

Yesu sakusiya konse,
Mphamvu, nzeru, chuma chonse;
Akupatsa nsiku zonse,
Tsata Yesu yekhayo.

Post navigation

Previous: Hymn 272 AMBUYE, ndifuna nditsukenitu;
Next: Hymn 274 YESU and’itana,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1260 Yesu, mulikundipempha, Munaterodi:
  • Hymn 394 TATENGA mphatso zotani?
  • Hymn 217 CHIPULUMUTSO chathu chayandika,
  • Hymn 407 ADZAPAMBANA Yesu ponse
  • Hymn 1388 Tiimbire Mlungu wathu
  • Hymn 500 >AMEN, Amen, Amen.
  • Hymn 944 Tiyeni nonsenu okonda Yesuyo,
  • Hymn 658 Ndichitireni, Mbuye ‘ne,
  • Hymn 33 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 251 Kuli chimwemwe m’dzuwalo
  • Hymn 1735 “Sezani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 1411 Yesu akuitanani
  • Hymn 770 Atate, muwapenye
  • Hymn 973 Tigwire nkhondo yomwe
  • Hymn 485 POMPANO pandikonda
  • Hymn 293 Tidziperekadi konse kwa Inu
  • Hymn 1562 Mzimu Woyera, mudze mumitima mwathumo,
  • Hymn 1248 ‘Dzanitu Wamphamvu yonse,
  • Hymn 1098 M’mene mantha andigwira,
  • Hymn 550 Wosauka Iyedi
  • Hymn 427 Komwe ndi chimwemwe
  • Hymn 281 Atate, ndipempha
  • Hymn 82 YANG’ANANI, anthu onse,
  • Hymn 356 YESU Mbuye onani,
  • Hymn 74 Ndipereka zanga zonse
  • Hymn 36 AMBUYE tsopano lino, monga mwa mawu anu aja,
  • Hymn 702 Mbuye wathu mutipatsa
  • Hymn 1729 Munthu Wazisoniyo
  • Hymn 1184 Akondwerera nthawiyi
  • Hymn 1145 Khalani duu! Mulungu wanuyu
  • Hymn 492 Yesu Mbuye ‘Nu wafatsa
  • Hymn 296 Mngelo anatumidwa
  • Hymn 1007 M’mene umauka m’mawa,
  • Hymn 1347 Akukonda, akukonda,
  • Hymn 1075 Ndikhazikike inetu, mumtima muli mwai,
  • Hymn 1369 Paphiri paja papakulupo,
  • Hymn 1089 Ndionetsere kuunika
  • Hymn 340 Imvani,
  • Hymn 486 Yesu, Yesu,
  • Hymn 115 Mbulu wanding’amba m’nthiti,
  • Hymn 174 YESU wathu Mbuyeyo
  • Hymn 426 MBUYE, Mpingo wanu usauka kwakukuludi;
  • Hymn 1275 Mtima ‘we siya ndi Yesu nsonizi,
  • Hymn 241 Munadzera ndi Mawu a moyo
  • Hymn 1437 Yesu ndi wokonda;
  • Hymn 25 “Akaleka amake
  • Hymn 1235 Yesu wathadi
  • Hymn 165 Yendanitu m’ulemudi,
  • Hymn 135 Kudziwa ukudziwa,
  • Hymn 1457 Ndidziwa kuti Yesu
  • Hymn 376 PAMTANDA Mbuye anafera,
  • Hymn 283 AMBUYE m’chipululu,
  • Hymn 1334 Walandira inetu
  • Hymn 208 CHITHA n’chiyani kund’yeretsa?
  • Hymn 1150 Pamtanda Mbuyanga ‘nafera,
  • Hymn 1692 Timwimbire zomtamanda, Aleluya
  • Hymn 38 Kodi mubvutidwa naye katundu?
  • Hymn 1693 Koma masauko ake Aleluya
  • Hymn 1782 Poyamba paja analenga
  • Hymn 892 Tilibe madalitso

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version