Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,

  1. Home   »  
  2. Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,

Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,

 

USAFUNE chuma chokha,
Pena masewero okha;
Koma za Mulungu zokha,
Zipambana zinazo.

Ukafuna kulemera,
Pempha chuma chosathera;
Ndiwo mtima wakuyera,
Ndi wokonda Yesuyo.

Zosawutsa uvomere,
Ndipo Yesu chaulere;
Chikondano ndi mtendere,
Alowetsa m’mtimamo.

Zonse umazinyadira,
Udzaleka kusilira;
Uli nazo zokwanira,
Pakupeza Yesuyo.

Mbiri yake ubukitse,
Anthu onse nuphunzitse;
Kwa Mulungu nufikitse,
Osokera onsewo.

Yesu sakusiya konse,
Mphamvu, nzeru, chuma chonse;
Akupatsa nsiku zonse,
Tsata Yesu yekhayo.

Post navigation

Previous: Hymn 260 ODALA ndi onsewo,
Next: Hymn 281 MBUYE, mwatiuza ’fe

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 129 WODALA ndiye munthuyo,
  • Hymn 1662 Msandipitire, Yesu,
  • Hymn 1391 Ndiye wokondwa, E, munthuyo
  • Hymn 1374 Inu mumvere anyamatawo,
  • Hymn 828 Ndidzukanso m’mawa,
  • Hymn 71 Andiyembekeza, chinthuchi ndidziwa,
  • Hymn 117 CHOLIMBITSA mtima ndi chonditsogolera;
  • Hymn 606 Dzinja lokondweretsa lafikanso,litapumatu,
  • Hymn 285 DZIKO lino lapansi,
  • Hymn 920 Yatha misoziyo,
  • Hymn 835 Mukhale ndine, dzuwalo lalowa,
  • Hymn 827 Wonsewu usiku
  • Hymn 1016 Mbuye, mwatiuza ‘fe
  • Hymn 1236 Mbuye ndimva leroli
  • Hymn 340 PEMPHERA m’mbanda kucha,
  • Hymn 1624 Koma anthu onse omwe
  • Hymn 482 Ndinu wakuyera,
  • Hymn 314 E, moto wanu woyera
  • Hymn 98 Ndidzamwona maso ndi maso
  • Hymn 834 Tiyamike Mlungu wotipatsa zachifundozi,
  • Hymn 8 Nanu Atumwi akumveka aja,
  • Hymn 1139 Namondwe akawombabe,
  • Hymn 749 Ndiye wodyetsa anthu omwewo,
  • Hymn 217 E! kwa Inu, E! kwa Inu!
  • Hymn 1233 Tsopano ndibukitsabe chikondi chanu chija
  • Hymn 321 PAKUONA imfayo
  • Hymn 771 Tsopano alandira
  • Hymn 914 Nlokoma Dziko langa!
  • Hymn 383 KASUPE ali wodzaza
  • Hymn 490 Yesu, ndikabwera
  • Hymn 29 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 766 Monga zomera zonsezo
  • Hymn 768 Ndi ife tinga mbewuzo
  • Hymn 121 Imbira!
  • Hymn 1253 Ndingopatsa Inu Mbuye
  • Hymn 1050 Ndafoka inetu,
  • Hymn 374 Pakuti Mfumuyo
  • Hymn 1702 Pakufa ine Mbuye
  • Hymn 602 Mpulumutsi wakukoma,
  • Hymn 917 Ndi nkhondo ikaleka
  • Hymn 1059 Kalelo m’mtima ndinakondwa,
  • Hymn 874 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 1741 Yesu munalaswa m’mtima,
  • Hymn 1552 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 1759 Powalitsira omwe
  • Hymn 1113 Mtima wa Mbuyako
  • Hymn 95 TAMANI mphamvu ya Yesu,
  • Hymn 618 ‘Dzani Mbuye msangatu,
  • Hymn 320 Ambuye, wakuti ndi mwaziwo
  • Hymn 1441 Wochimwa iwe, bweratu
  • Hymn 1512 Cholimbitsa mtima ndi
  • Hymn 855 Aulendo amayenda
  • Hymn 1121 Ndifuna Yesuyo,
  • Hymn 292 Ndi makutu athu awanso nganu,
  • Hymn 101 MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,
  • Hymn 502 Ndikonda mbiri yomwe
  • Hymn 1213 Mwamva Yesu m’mtimamo,
  • Hymn 374 NDI lokoma m’Mwambamo,
  • Hymn 1066 Uchimo unapachikidwa pomwe
  • Hymn 1826 Amadyetsa Iye mbalame zam’mwamba,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version