Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 255 KHALA chete mtima wanga

  1. Home   »  
  2. Hymn 255 KHALA chete mtima wanga

Hymn 255 KHALA chete mtima wanga

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 255 KHALA chete mtima wanga

 

KHALA chete mtima wanga
Mlungu wako ndiye Mfumu;
Zinthu zonse zisinthika,
Mlungu ndi wachikhalire.

(Khala chete, Chidzakupinga n’chiyani?
Usaope, Mulungu ali nawe.)

Anthu onse pansi pano
Sakhutitsa mtima wawo;
Amadera zinthu zawo,
Namakhumba zakutali.

Khala chete mtima wanga,
Zikwanire zinthu zako;
Usakhumbe zapansipa
Koma Mlungu wako yekha.

Post navigation

Previous: Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,
Next: Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 386 MONGATU mawu anuwo,
  • Hymn 62 Tchimo lonse ligonjera
  • Hymn 992 Mukandipweteka,
  • Hymn 1562 Mzimu Woyera, mudze mumitima mwathumo,
  • Hymn 640 Anakwatira kale
  • Hymn 291 ULENDO wachikhrisitu ngosawutsa ndithu,
  • Hymn 646 Mudalitse nyumba yathu;
  • Hymn 1412 Imfa idzafika msanga;
  • Hymn 29 CHIKONDI cha
  • Hymn 112 Pangano lake m’mwaziwo
  • Hymn 721 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 680 Mbendera yake ikupiza m’mlengalengamo,
  • Hymn 474 MPULUMUTSI, Mbusa wathu,
  • Hymn 887 Pakupempherera
  • Hymn 1089 Ndionetsere kuunika
  • Hymn 827 Wonsewu usiku
  • Hymn 5 Inu Mulungu, tikuyamikani;
  • Hymn 301 Mwanawankhosa
  • Hymn 1537 Mulowe m’mtima, mdzazetu
  • Hymn 589 Koma ineyu
  • Hymn 1150 Pamtanda Mbuyanga ‘nafera,
  • Hymn 935 Mtima ukachita nkhawa
  • Hymn 152 Inde, Yesu, mundikonda,
  • Hymn 718 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 138 Kumva ulikumva, ulikumva,
  • Hymn 1153 Mtendere uli m’mtima mwathumu,
  • Hymn 565 Koma sitimpenya m’khola
  • Hymn 1239 Ndipo pakuima phe!
  • Hymn 1496 Mawu amveke bwino,
  • Hymn 1372 Zam’madzi zonse zakuopsyazo,
  • Hymn 1627 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 1676 Kondwerani dzuwa lino Aleluya,
  • Hymn 1739 Ife timakufunani
  • Hymn 1075 Ndikhazikike inetu, mumtima muli mwai,
  • Hymn 1615 Anakonda,
  • Hymn 1560 Mthandizi ndinu, mndithangate ine
  • Hymn 139 Bwerani inu nonse, inu nonse,
  • Hymn 861 Mbuye, Mpingo wanu usauka kwa kukuludi;
  • Hymn 1408 Kodi mwalandira Yesu?
  • Hymn 1144 Khalani duu! Ambuye adzatu;
  • Hymn 30 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 740 Tsopano nthawi yake phwandili,
  • Hymn 220 Kalekale ndinathawa,
  • Hymn 1732 Anapachikidwatu,
  • Hymn 70 LAMBIRA, Mfumuyo,
  • Hymn 1647 Kubweza inetu, kubweza inetu,
  • Hymn 1594 Chikondano chakechi
  • Hymn 844 Pogona ife, amadzuka
  • Hymn 448 CHIFUKWA cha zokoma mtima zonse zaulelezo,
  • Hymn 487 INE ndine mlendo
  • Hymn 171 M’manda munalibe
  • Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 1069 Zochimwa zathu m’mtimamo
  • Hymn 322 PAKUYITANIDWA munthu pa dziko ino,
  • Hymn 583 Anabadwa,
  • Hymn 976 Muyendenso kunka komwe,
  • Hymn 1546 Mubwere Mzimu Inu
  • Hymn 314 TIYENI nonsenu okonda YESUYO,
  • Hymn 1105 Khala chete mtima wanga
  • Hymn 684 Zipata zatsegudwa mbee! Za m’dziko monsemo;

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version