Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 249 MBUYANGA Yesu, mundigwire

  1. Home   »  
  2. Hymn 249 MBUYANGA Yesu, mundigwire

Hymn 249 MBUYANGA Yesu, mundigwire

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 249 MBUYANGA Yesu, mundigwire

 

MBUYANGA Yesu, mundigwire
Dzanja.
Kuyenda ndekha sindikwana ’yi;
Mukandigwira dzanja langa, Mbuye
Sindikaopa kanthu kena ’yi.

Mbuyanga Yesu, mundisunge ine
Pafupi ndi ’Nu nthaŵi yonseyo;
Ndikasoŵatu Inu, Mpulumutsi,
Ndingosekera m’talimo.

Mbuyanga Yesu, ndikapanda Inu
Ukadza mdima m’mtima mwangamu;
Koma ndinutu dzuŵa langa ndithu
Lakuwalitsa m’mtima momwemu.

Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja
Pamene ine ndimwalirapo.
Mkhaletu m’fupi nthaŵi yomwe Mbuye,
Mundiloŵetse ine m’Mwambamo.

Post navigation

Previous: Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,
Next: Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 983 Nkhondo ya Satana
  • Hymn 114 Ndine Mbusayo wabwino,
  • Hymn 209 Mdima ufika, dzuwa lalowa,
  • Hymn 710 Nthano ya Hananiyayo
  • Hymn 157 INU nonse ovutidwa,
  • Hymn 1033 Mkristu gwiratu ntchito
  • Hymn 987 Ambuye wa Kumwamba,
  • Hymn 565 Koma sitimpenya m’khola
  • Hymn 945 Tiyeni pamodzi,
  • Hymn 341 Ayenda,
  • Hymn 1506 Ndikamfunafuna Iye,
  • Hymn 1693 Koma masauko ake Aleluya
  • Hymn 8 Nanu Atumwi akumveka aja,
  • Hymn 479 Munanena mulandira
  • Hymn 46 O! ufulu tigwirizane
  • Hymn 1263 Mbuye, ndingogonj tere, Ndibvomerapo;
  • Hymn 414 Ana ake adzapuma
  • Hymn 148 Ndisauka, ndimasowa
  • Hymn 1451 Okoma ndiwo mawu
  • Hymn 123 MULI ndi ludzu, idzani
  • Hymn 741 Chakudya ichi chidzapita du,
  • Hymn 159 Kamwana Yesu ‘nabadwa,
  • Hymn 184 LEKANI kubvutika ndi zinthu za padziko,
  • Hymn 686 Imbadi za Iyeyo,
  • Hymn 281 Atate, ndipempha
  • Hymn 902 Ndikondwa kuganizabe
  • Hymn 986 Tiyeni anzathu
  • Hymn 21 Mbuye mtsitsimutse!
  • Hymn 1027 Tithawiranji ifetu?
  • Hymn 1748 Ambuye tsopano lino,
  • Hymn 1354 Mzimu Woyera, m’mtimamo
  • Hymn 485 POMPANO pandikonda
  • Hymn 1239 Ndipo pakuima phe!
  • Hymn 555 Mkucha wake ndaniyo
  • Hymn 1310 Yesu wondikondadi,
  • Hymn 620 Mphatso zonse zathu
  • Hymn 1428 Penyetsetsa Yesu
  • Hymn 1698 Chinkana dziko lonselo
  • Hymn 1061 Mundichotsere tchimo lonse
  • Hymn 868 Atate yemwe anatuma Mpulumutsi mmodzi
  • Hymn 138 SANGALATSA akusowa, masiku alikutha,
  • Hymn 1814 Thupi lamwazi wathu’li
  • Hymn 663 Anyamata a Mulungu,
  • Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,
  • Hymn 328 Yesu ndiye mphamvu yanga,
  • Hymn 1479 Ndi Yesu yemwe kalelo
  • Hymn 843 M’maiko monse, zisi zomwe,
  • Hymn 283 AMBUYE m’chipululu,
  • Hymn 1316 Ndabwera kwa Ambuyeyo:
  • Hymn 1095 Mumtima wakufatsa
  • Hymn 1445 Tiyeni tonse, tinkeko
  • Hymn 174 YESU wathu Mbuyeyo
  • Hymn 678 Ibukike mbiri yanu,
  • Hymn 644 M’wasunge, m’wayendetse
  • Hymn 227 NDIM’KONDE Kristuyo,
  • Hymn 126 Mwa ine, moyo wanga ndi Yesu
  • Hymn 1365 Zozizwa za m’dziko,
  • Hymn 120 MUNDINYEMERE ’ne
  • Hymn 130 Tidzakondweradi m’Mwambamo
  • Hymn 104 M’mene ntchito yathatu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version