Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 249 MBUYANGA Yesu, mundigwire

  1. Home   »  
  2. Hymn 249 MBUYANGA Yesu, mundigwire

Hymn 249 MBUYANGA Yesu, mundigwire

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 249 MBUYANGA Yesu, mundigwire

 

MBUYANGA Yesu, mundigwire
Dzanja.
Kuyenda ndekha sindikwana ’yi;
Mukandigwira dzanja langa, Mbuye
Sindikaopa kanthu kena ’yi.

Mbuyanga Yesu, mundisunge ine
Pafupi ndi ’Nu nthaŵi yonseyo;
Ndikasoŵatu Inu, Mpulumutsi,
Ndingosekera m’talimo.

Mbuyanga Yesu, ndikapanda Inu
Ukadza mdima m’mtima mwangamu;
Koma ndinutu dzuŵa langa ndithu
Lakuwalitsa m’mtima momwemu.

Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja
Pamene ine ndimwalirapo.
Mkhaletu m’fupi nthaŵi yomwe Mbuye,
Mundiloŵetse ine m’Mwambamo.

Post navigation

Previous: Hymn 248 M’MENE ine ndisauka
Next: Hymn 250 MBUYANGA Yesu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 945 Tiyeni pamodzi,
  • Hymn 1342 Tadza kumtsinjeku
  • Hymn 412 MOYO uli pafupi,
  • Hymn 781 Tatsegukani inutu,
  • Hymn 1008 Wakuchezacheza naye
  • Hymn 1069 Zochimwa zathu m’mtimamo
  • Hymn 1136 Mulungu anditsogolera
  • Hymn 917 Ndi nkhondo ikaleka
  • Hymn 1698 Chinkana dziko lonselo
  • Hymn 31 Tamandani mbuye,
  • Hymn 965 Mundiuze, aulendo,
  • Hymn 374 NDI lokoma m’Mwambamo,
  • Hymn 451 MLUNGU alinane;
  • Hymn 1222 Bwenzi ndimamkomanayo
  • Hymn 5 Inu Mulungu, tikuyamikani;
  • Hymn 845 Ufumu wanu, Mbuye Yesu,
  • Hymn 1380 Tilemekezetu
  • Hymn 503 Ndikondwa kuti Yesu
  • Hymn 368 Yehova ndiye Mlungudi,
  • Hymn 413 Yesu ndiye Bwenzi lathu,
  • Hymn 110 Ndaima nji pa Kristuyo,
  • Hymn 1122 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 6 LEMEKEZA Mulungu ’Tate,
  • Hymn 1202 Ndikhumba mtimawo
  • Hymn 285 Ndipempha, Ambuye,
  • Hymn 678 Ibukike mbiri yanu,
  • Hymn 948 Tiimbe mokondwa, misozi iume;
  • Hymn 762 “Ndi thupi lopatsidwali
  • Hymn 1347 Akukonda, akukonda,
  • Hymn 483 Ndife akuchoka,
  • Hymn 313 Muthire, Yesu, m’mtimanga
  • Hymn 406 Kwa Yesu ndi kwabwinoko,
  • Hymn 730 A! Yesu mwapangana
  • Hymn 1350 Mvera Yesu, mvera Yesu,
  • Hymn 1027 Tithawiranji ifetu?
  • Hymn 1404 “Undipatsetu
  • Hymn 1675 Lambira Mfumuyo
  • Hymn 636 Yehova Mlungu wathu,
  • Hymn 270 Zoopsya zopambana
  • Hymn 1047 Ambuye, chotsani zonse zomwezo
  • Hymn 1415 Iye anatsika m’Mwamba,
  • Hymn 1327 Bwezatu, bwezatu,
  • Hymn 438 Yesu ndiye Mbusa
  • Hymn 332 NDIKONDWA kuganizirabe
  • Hymn 359 TADZUKA mzimu wanga ‘we,
  • Hymn 1543 Idzani, Mzimu Inu,
  • Hymn 971 Ndinu Mbusa wanga;
  • Hymn 459 KALE anthu m’kholamo,
  • Hymn 533 Ananu, ziimbani,
  • Hymn 425 Ine ndine mlendo
  • Hymn 1606 Yesu, dzina lakufatsa,
  • Hymn 462 Pothandiza amathu,
  • Hymn 1682 Atha masiku aja ansoni,
  • Hymn 288 HAYA! ’nzanga taonani
  • Hymn 787 Mzimu Wakuyera
  • Hymn 1665 Nkhope yanu ndifunitsa,
  • Hymn 537 Aleluya! Aleluya!
  • Hymn 169 ’MVANI liu lomwe
  • Hymn 1580 Akadakhalabe
  • Hymn 76 E, MOYO wanga’we

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version