Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 247 MULUNGU anditsogolera,

  1. Home   »  
  2. Hymn 247 MULUNGU anditsogolera,

Hymn 247 MULUNGU anditsogolera,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 247 MULUNGU anditsogolera,

 

MULUNGU anditsogolera,
Ndapumula m’mtimamo;
Ayang’anira njira zanga
Nsiku zanga zonsezo.

Mulungu anditsogolera
Nsiku zanga zonsezo;
Ndidzatsatira Mbuye wanga
M’njira mwake momwemo.

Masiku ena pali mdima,
Ndivutidwa m’mtimamo;
Masiku ena ndikondwera
Ndi zabwino zangazo.

Masiku onse m’mtima mwanga
Ndili ndi mtenderewo,
Chifukwa ndimakhulupira
Mtsogoleri wangayo.

Post navigation

Previous: Hymn 246 NAMONDWE akawombabe,
Next: Hymn 248 M’MENE ine ndisauka

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1329 M’tali mutali m’phirimo
  • Hymn 1144 Khalani duu! Ambuye adzatu;
  • Hymn 376 PAMTANDA Mbuye anafera,
  • Hymn 841 Mukhale, mukhale,
  • Hymn 738 Mommuno, Mbuye, mkate wanuwu,
  • Hymn 1497 Simbani mobwereza,
  • Hymn 357 TAMANDANI Mbuye,
  • Hymn 1029 Nkhawa tilibe; Yesuyo
  • Hymn 1728 Zofuna zanga zonsezo
  • Hymn 265 MUDZAZE Yesu mtima wanga ndi chikondicho,
  • Hymn 15 YEHOVA ndiye Mbusa wanga,
  • Hymn 1758 Poti Mulungu wathu
  • Hymn 309 Mwa Mzimu mulowe mumitima yathu,
  • Hymn 197 NDIKHULUPIRA’Nu,
  • Hymn 279 Mbwere mudzamve nonse
  • Hymn 1484 Idzatu, idzatu
  • Hymn 1600 E! dzina la Yesu,
  • Hymn 1793 Pakuwoloka mtsinje wa imfa
  • Hymn 171 IWE tiye, iwe tiye,
  • Hymn 659 Anthu ali m’mdima akuitanitsa
  • Hymn 222 Ndilikudzatu,
  • Hymn 850 Pemphero, pemphero,
  • Hymn 1057 Ndilira ine kukayenda
  • Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,
  • Hymn 331 Yesu ndimafuna Inu,
  • Hymn 1128 Mbuyanga Yesu, mundisunge ine
  • Hymn 1220 Bwenzi ndinamkomanayo
  • Hymn 842 Tipempha kuti Mpingo wanu
  • Hymn 1134 Pansi pano ndili mlendo,
  • Hymn 1746 Mwachimwemwe, mwachisoni,
  • Hymn 1604 Yesu, dzina lakukonda,
  • Hymn 455 TIIMBE ndi kulalikira
  • Hymn 1367 Wamphamvu yosatha,
  • Hymn 820 Ndife ananu,
  • Hymn 338 Imvani
  • Hymn 1468 Zobvala zake zonse
  • Hymn 862 Tidza kwa Mulungu Inu, ndinu wa chifundo;
  • Hymn 981 Tiyeni Akristu,
  • Hymn 1382 E, chifundo chake chonse
  • Hymn 683 Musamaopa kanthu ‘yi, tamani Yesuyo;
  • Hymn 1112 Masiku anga onse
  • Hymn 355 DZIKO lonse mlambire
  • Hymn 180 MALO alimo m’nyumba ya Yesu,
  • Hymn 1171 Mulungu wanga
  • Hymn 46 INALIPO nthawi,
  • Hymn 414 INU bambo, inu mayi,
  • Hymn 686 Imbadi za Iyeyo,
  • Hymn 998 Anatilemba Yesu tikagwire nkhondo yake,
  • Hymn 1744 Kale ophunzira ake
  • Hymn 480 TIANA ife tingofoka,
  • Hymn 887 Pakupempherera
  • Hymn 579 Pochezera m’dambomo,
  • Hymn 210 Nyumba yodyera ilikudzaza;
  • Hymn 1778 Angelo kwezani
  • Hymn 698 Polenga dzikoli,
  • Hymn 116 Nkhosa zanga zimandimva
  • Hymn 658 Ndichitireni, Mbuye ‘ne,
  • Hymn 31 Tamandani mbuye,
  • Hymn 652 Munene Mbuye ‘nenetu,
  • Hymn 67 PAMENEPO pokhala madzulo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version