Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 243 KONDWANI nonsenu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 243 KONDWANI nonsenu,

Hymn 243 KONDWANI nonsenu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 243 KONDWANI nonsenu,

 

KONDWANI nonsenu,
Mpulumutsi anadza;
Onani kukhola,
Kumtanda ndi manda

Mlemekeze, bukitsani,
Naferatu kale;
Kondwerani, mlemekeze
Akhaladi moyo.

Kondwani nonsenu,
Anakhetsatu mwazi,
Natiwombola nawo,
Tikhale ana ’ke.

Kondwani nonsenu,
Atikhululukira,
Wosachimwa nafera
Anthu ’fe oipa.

Kondwani nonsenu,
Mfumu yathu yakwera;
Kwa Atate Kumwamba
Atipempherera.

Kondwani nonsenu,
Adzabweranso Yesu,
Waulemu, wamphamvu,
Kuweruza dziko.

Post navigation

Previous: Hymn 242 NDIIMBA mumtima mokondwa,
Next: Hymn 244 TIMVE za anamwali khumi,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1769 Ndiye amachitira
  • Hymn 1549 Mtitsutse titachimwa
  • Hymn 378 KWEZANI mitu yanuyo,
  • Hymn 1081 Ndikabisala mwanu
  • Hymn 109 Chiyembekezo changacho
  • Hymn 435 ANAKWATIRA kale
  • Hymn 275 Mlungu akuyang’aniredi,
  • Hymn 416 PALIBE wina Kumwamba,
  • Hymn 357 Yesu ndiye Mtetezi,
  • Hymn 1153 Mtendere uli m’mtima mwathumu,
  • Hymn 1327 Bwezatu, bwezatu,
  • Hymn 1428 Penyetsetsa Yesu
  • Hymn 260 ODALA ndi onsewo,
  • Hymn 939 Ambuye andisunga
  • Hymn 960 Tilikupita kwathu kuja
  • Hymn 610 Nafenso tidzadzuka kwa ‘ke ngati maluwawo,
  • Hymn 65 Chisomo chodabwitsacho
  • Hymn 374 Pakuti Mfumuyo
  • Hymn 385 SINDILI woyenera ’ne,
  • Hymn 184 LEKANI kubvutika ndi zinthu za padziko,
  • Hymn 84 Aleluya, Aleluya,
  • Hymn 136 Atumwi atummika, atumika,
  • Hymn 442 MASIKA a m’dziko Mbuye,
  • Hymn 142 Kukondwa kwa wodwalayo
  • Hymn 106 MZIMU Woyera, mudzetu,
  • Hymn 917 Ndi nkhondo ikaleka
  • Hymn 192 ZAKEYU mkulu wa misonkho,
  • Hymn 951 Ndi kale lonse mnandisunga ‘ne;
  • Hymn 992 Mukandipweteka,
  • Hymn 574 A! Yesu Mbuye wakuyera,
  • Hymn 765 Chikondi chili m’chikhomu
  • Hymn 122 Musadziunjikire chuma cha padziko,
  • Hymn 993 Pakumalizidwa
  • Hymn 168 NDINGANENE malilime,
  • Hymn 1247 A Chikondi chopambana,
  • Hymn 396 Mtitsogolere nthawi zonsezo;
  • Hymn 160 MADALITSO ngati mvumbi,
  • Hymn 237 SINDINANYENGEDWA konse
  • Hymn 1810 Kalelo Mbuye Yesu
  • Hymn 1801 Nafuna kwaononga
  • Hymn 691 Akukhala kunja,
  • Hymn 173 Mema nkhondoyo, wadza mdaniyo,
  • Hymn 754 Ndi mtanda uli m’maso mbuu,
  • Hymn 1739 Ife timakufunani
  • Hymn 652 Munene Mbuye ‘nenetu,
  • Hymn 129 Mudze kwa Yesu, musachedwe,
  • Hymn 889 Pemphera m’mbanda kucha,
  • Hymn 1568 Kudzoza kwanu kutipatsa
  • Hymn 1111 Pamene ndilemedwa
  • Hymn 1094 Ambuye anachoka
  • Hymn 105 Tiyamike Mbuye Yesu
  • Hymn 894 Mbuye, ndinu Mfumu yanga
  • Hymn 1397 Okwawa pansi inu,
  • Hymn 634 Mtifungatire ndi mapiko paulendo pathu,
  • Hymn 1713 Zochimwa zanga zonsezo
  • Hymn 1001 Mafumu atiuza tikaletse ukapolo,
  • Hymn 704 Monga tilandira, Mbuye,
  • Hymn 1551 Mukhale m’kati mwathu,
  • Hymn 1226 Wandipatsa moyo wake,
  • Hymn 1026 Inde nditaya chumacho,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version