Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 243 KONDWANI nonsenu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 243 KONDWANI nonsenu,

Hymn 243 KONDWANI nonsenu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 243 KONDWANI nonsenu,

 

KONDWANI nonsenu,
Mpulumutsi anadza;
Onani kukhola,
Kumtanda ndi manda

Mlemekeze, bukitsani,
Naferatu kale;
Kondwerani, mlemekeze
Akhaladi moyo.

Kondwani nonsenu,
Anakhetsatu mwazi,
Natiwombola nawo,
Tikhale ana ’ke.

Kondwani nonsenu,
Atikhululukira,
Wosachimwa nafera
Anthu ’fe oipa.

Kondwani nonsenu,
Mfumu yathu yakwera;
Kwa Atate Kumwamba
Atipempherera.

Kondwani nonsenu,
Adzabweranso Yesu,
Waulemu, wamphamvu,
Kuweruza dziko.

Post navigation

Previous: Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,
Next: Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 580 Mwana wakuyera ‘Nu,
  • Hymn 536 Ana inu, myamikeni
  • Hymn 746 Imfa ndi mdima zinathawa zii!
  • Hymn 396 Mtitsogolere nthawi zonsezo;
  • Hymn 735 Mwa chikho chokumbutsa
  • Hymn 1389 Tithawire kwa Mulungu,
  • Hymn 1686 Ndi mtima wonse mwimbedi
  • Hymn 1068 Ambuye, thandizenitu
  • Hymn 453 Tiana ta Ambuye tili
  • Hymn 115 NTHAWI ija ya Sauli,
  • Hymn 30 YEHOVA, Mbusa wangadi,
  • Hymn 590 Mbuye, Msungi ‘Nu,
  • Hymn 1593 Wina atikonda ife,
  • Hymn 320 Ambuye, wakuti ndi mwaziwo
  • Hymn 902 Ndikondwa kuganizabe
  • Hymn 1588 Wandiwombola inetu
  • Hymn 395 Usiku uno mutisungedi,
  • Hymn 238 MULUNGU wanga,
  • Hymn 281 MBUYE, mwatiuza ’fe
  • Hymn 4 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 1535 Lichepa dontho lokhali,
  • Hymn 105 Tiyamike Mbuye Yesu
  • Hymn 1536 Ndilira Mzimu leroli,
  • Hymn 495 Wonga Inu ndikhaledi,
  • Hymn 1485 Unachimwachimwa ndithu,
  • Hymn 807 Mpulumutsi tikagona
  • Hymn 290 Ndi miyendo yathu iyinso njanu,
  • Hymn 298 “Tadodoma, abusa,
  • Hymn 355 DZIKO lonse mlambire
  • Hymn 946 Ngakhale enawo aleke kwimbako,
  • Hymn 133 NSEMBE yake ya Kaini,
  • Hymn 1161 Wapumitsa mtima wanga,
  • Hymn 975 Tiyeni, Akristu inu,
  • Hymn 791 Anthu opembedzawo
  • Hymn 135 USANABADWE, Yeremiya,
  • Hymn 480 Tifunitsa Inu tere,
  • Hymn 1551 Mukhale m’kati mwathu,
  • Hymn 1837 Mbuye ndiye wachifundo,
  • Hymn 665 Pomangidwa anthu nayo
  • Hymn 819 Lero tigone,
  • Hymn 153 NDAKUMANA ndi bwenzi lokomalo,
  • Hymn 24 “Ndakupeza womanga,
  • Hymn 1759 Powalitsira omwe
  • Hymn 188 Ine ndili ndi manyazi
  • Hymn 722 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 1292 Wolapa mtima simunyozadi,
  • Hymn 1690 Titama Yesuyo,
  • Hymn 653 Nditsogolere m’njirayi
  • Hymn 126 Mwa ine, moyo wanga ndi Yesu
  • Hymn 1178 Mawu omwewo, nyimbo yomweyi,
  • Hymn 391 Mufafanize m’bukumo
  • Hymn 1735 “Sezani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 161 Tibwera ndi tianato
  • Hymn 712 Mulungu akondadi leroli
  • Hymn 372 Potero onsewo
  • Hymn 1177 Ndidziwitsitsa Yesu ndi wanga,
  • Hymn 1106 Mlungu ndi wachikhalire.
  • Hymn 111 YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;
  • Hymn 167 KODI mwalandira Yesu?
  • Hymn 1115 M’munda wa Mbuyako

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version