Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 243 KONDWANI nonsenu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 243 KONDWANI nonsenu,

Hymn 243 KONDWANI nonsenu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 243 KONDWANI nonsenu,

 

KONDWANI nonsenu,
Mpulumutsi anadza;
Onani kukhola,
Kumtanda ndi manda

Mlemekeze, bukitsani,
Naferatu kale;
Kondwerani, mlemekeze
Akhaladi moyo.

Kondwani nonsenu,
Anakhetsatu mwazi,
Natiwombola nawo,
Tikhale ana ’ke.

Kondwani nonsenu,
Atikhululukira,
Wosachimwa nafera
Anthu ’fe oipa.

Kondwani nonsenu,
Mfumu yathu yakwera;
Kwa Atate Kumwamba
Atipempherera.

Kondwani nonsenu,
Adzabweranso Yesu,
Waulemu, wamphamvu,
Kuweruza dziko.

Post navigation

Previous: Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,
Next: Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 890 Kumbuka ‘bale ako
  • Hymn 212 Onse am’Mwamba ali mowemo,
  • Hymn 899 ‘Tate wa Kumwambako,
  • Hymn 284 Yesu Mfumu Inu
  • Hymn 1834 Chisomo ndi zokoma zake sizileka konse;
  • Hymn 479 Munanena mulandira
  • Hymn 656 Ndipumulire panupo,
  • Hymn 626 Inde, ‘Tate, mtiyendetse
  • Hymn 252 MTIMA wa Mbuyako,
  • Hymn 1765 Zoonazi amithenga
  • Hymn 1315 Ambuye ‘naitana ‘ne:
  • Hymn 552 Analira ndaniyo
  • Hymn 243 KONDWANI nonsenu,
  • Hymn 68 M’MANDA, nagonamo
  • Hymn 474 Yesu ndafikatu,
  • Hymn 994 Limba mtima mbale wanga,
  • Hymn 256 Ndilira, ndilira,
  • Hymn 1358 Lemekeza Mfumu yathu,
  • Hymn 26 NDIKULEMEKEZA
  • Hymn 1188 Akumangidwa ndi mzimuwo,
  • Hymn 452 MLUNGU, Inutu,
  • Hymn 467 NGOLIZO zilira
  • Hymn 1390 Nditamatu Ambuyangayu,
  • Hymn 788 Moyo watsopano
  • Hymn 1331 Yesu wathu Mbuyeyo
  • Hymn 1851 Anthu onse, anthu onse,
  • Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,
  • Hymn 1231 Nlokoma dzinalo la Yesu, ndilo thanthwe langa,
  • Hymn 907 Dziko labwinotu, dziko labwinotu,
  • Hymn 507 Yesu ndimkonda, akondanso ine,
  • Hymn 976 Muyendenso kunka komwe,
  • Hymn 1154 Zakutsogolo sitidziwa ‘yi;
  • Hymn 1852 Mbuye ndamva mwawazira
  • Hymn 16 MTIMA wanga lemekeza,
  • Hymn 173 Mema nkhondoyo, wadza mdaniyo,
  • Hymn 953 Ichi chindisangalatsa
  • Hymn 622 Tiyamikira ‘Tate,
  • Hymn 387 MUDZE, anthuni, talaŵani ’nu
  • Hymn 180 MALO alimo m’nyumba ya Yesu,
  • Hymn 1110 Mulungu wanga,
  • Hymn 1221 Bwenzi ndinamkomanayo,
  • Hymn 1063 Pokhala mtendere mu mtimangamu,
  • Hymn 84 Aleluya, Aleluya,
  • Hymn 500 >AMEN, Amen, Amen.
  • Hymn 92 Ufuna kugwira ntchito yake?
  • Hymn 225 Yesu akhazika
  • Hymn 328 KULIBE vuto
  • Hymn 11 NDI mitima yokondwera,
  • Hymn 1549 Mtitsutse titachimwa
  • Hymn 1036 Mtima wakufatsa
  • Hymn 1207 Poyambapo ndakondwadi,
  • Hymn 188 MPULUMUTSI Wokondedwa,
  • Hymn 197 Tidzatama Atate wathu
  • Hymn 1575 Tifuna kuti komweko
  • Hymn 774 Tibatizidweko,
  • Hymn 1505 Ndikampeza, ndikamtsata
  • Hymn 503 Ndikondwa kuti Yesu
  • Hymn 1721 Mapazi ake namvatu
  • Hymn 1242 Ku zoipa zonse zako,
  • Hymn 1424 Malo anachepa,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version