Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda

  1. Home   »  
  2. Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda

Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda

 

TIIMBE nyimbo zotamanda
Mulungu wathu wabwino,
Pakuti akondana nawo
Anthu okhala padziko;
Tero natuma Mwana wake,
Wakukondedwa kalelo,
Kutiphunzitsa ife tonse
Za chikondano chakecho.

Mulungu ndiye wachifundo,
Nadzalandira onsewa
Akuulula mphulupulu
Ndi kukondana ndi Yesu
Tilondelonde njira yake
Yopapatiza yaing’ono;
Adzatilondolera ndiye
Kutifikitsa m’Mwambamo.

Pakuwoloka mtsinje wa imfa
Dzanja Mbuyathu agwira;
Tikadagwira ntchito zake
Atipatsatu korona;
Komwe kulibe masauko,
Pena misozi maliro;
Mulungu tidzamtamandira,
Inde kosalekezanso.

Post navigation

Previous: Hymn 20 CHIKONDI cha Mulungu wathu,
Next: Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1191 Ambuyanga Yesu
  • Hymn 1360 Ndi Aleluya imbirani
  • Hymn 1511 Mndidalitsere ‘ne
  • Hymn 1197 Ndafoka ine kale,
  • Hymn 1308 Ndi ine, m’mtima Mwanu mbee!
  • Hymn 208 “Lowa, lowa
  • Hymn 1423 Oipa inu nonsetu,
  • Hymn 549 Ndiye Mbuye, Mfumu yanga,
  • Hymn 1023 Kodi m’njiramo ndimvadi
  • Hymn 1574 Anthu ose ndi mitundu
  • Hymn 1053 Mtimatu wopirira ndi
  • Hymn 1794 Mulungu awakonda anthu
  • Hymn 1275 Mtima ‘we siya ndi Yesu nsonizi,
  • Hymn 644 M’wasunge, m’wayendetse
  • Hymn 58 PAMTANDAPO Ambuyeyo
  • Hymn 438 Yesu ndiye Mbusa
  • Hymn 1770 Iye amazichita zamphamvu
  • Hymn 1537 Mulowe m’mtima, mdzazetu
  • Hymn 84 LIDZE msanga dzuŵa lanu
  • Hymn 1094 Ambuye anachoka
  • Hymn 828 Ndidzukanso m’mawa,
  • Hymn 207 Malo alimo m’nyumba ya Yesu,
  • Hymn 495 Wonga Inu ndikhaledi,
  • Hymn 1793 Pakuwoloka mtsinje wa imfa
  • Hymn 477 Mpulumutsi, Mbusa wathu,
  • Hymn 1298 Ndikhulupira ‘Nu,
  • Hymn 79 PAKWITANA Mbuye wanga
  • Hymn 1447 Yesu ngwachifundodi,
  • Hymn 500 Mbuye Yesu andisunga
  • Hymn 163 MALO anachepa,
  • Hymn 676 Adze amitundu yonse,
  • Hymn 1379 Mulungu yemweyo
  • Hymn 1162 Mumvetu abwenzi athu,
  • Hymn 668 Achisoni, obvutidwa,
  • Hymn 154 Pemphero ndiko kulira,
  • Hymn 1229 Dzinalo la Yesu,
  • Hymn 369 Lowani m’nyumba mwakemu
  • Hymn 1089 Ndionetsere kuunika
  • Hymn 1274 Chisoni andichotsera Mbuyeyu,
  • Hymn 206 Uzanitu abale,
  • Hymn 48 IMFA ya Mwana wa Mulungu,
  • Hymn 854 Timlemekeze Mlunguyu
  • Hymn 1685 Nla Mlungu dzuwali;
  • Hymn 43 Ulendo wathu ukadzatha
  • Hymn 1661 Ndimachitira
  • Hymn 769 Ndi kutsukidwa m’mwazimo
  • Hymn 702 Mbuye wathu mutipatsa
  • Hymn 1679 Tiyamike Dzina lake, Aleluya,
  • Hymn 519 Mverani, aimba anawo,
  • Hymn 624 Ndinu mwatithangatira
  • Hymn 140 NDINAMIRA m’machimo, wosaonekanso,
  • Hymn 464 AKAZI anadza kwa Yesu ndi anawo,
  • Hymn 334 KULI dziko labwino M’mwamba,
  • Hymn 381 MONGA zomera zonsezo
  • Hymn 1605 Yesu, dzina lokondwetsa
  • Hymn 871 Tiphatikane tonsefe okonda Yesu Kristu;
  • Hymn 1071 Kumwamba Yesu mthandize,
  • Hymn 84 Aleluya, Aleluya,
  • Hymn 279 Mbwere mudzamve nonse
  • Hymn 919 ‘Tate, mwa kusunga kwanu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version