Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 216 NDISAUKA, ndinachimwa,

  1. Home   »  
  2. Hymn 216 NDISAUKA, ndinachimwa,

Hymn 216 NDISAUKA, ndinachimwa,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 216 NDISAUKA, ndinachimwa,

 

NDISAUKA, ndinachimwa,
Koma Inu m’nandifera;
Ndimo ndamva mund’itana,
Mwana Mlungu ndingobwera.

Ndisauka, ndimasowa,
Mphamvu yakuyera m’mtima;
Mwazi wanu wanditsuka,
Mwana Mlungu ndingobwera.

Ndisauka, sindikhoza,
Kuiletsa nkhondo m’ mtima;
Ndi chisoni, mantha nkhawa,
Mwana Mlungu ndingobwera.

Ndisauka, sindiona,
Ndingodwala, ndilefuka;
Zonse ndizitaya kwa ‘Nu,
Mwana Mlungu ndingobwera.

Inde, Yesu, mulandira,
Muchiritsa, m’ pulumutsa;
Mawu anu ndivomera,
Mwana Mlungu ndingobwera.

Inde, Yesu, mundikonda,
Zonse zina ndazitaya;
Tsono kukhala wanu,
Mwana Mlungu ndingobwera.

Post navigation

Previous: Hymn 215 TATE ndili mwana wanu,
Next: Hymn 217 CHIPULUMUTSO chathu chayandika,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 313 MUNDIŴALIRE m’njira mwangamo,
  • Hymn 1572 Mumbveke, mbveke, mbveke,
  • Hymn 222 Ndilikudzatu,
  • Hymn 1332 Imba kawiri ndi kawirinso,
  • Hymn 1151 Pomulambira Yesu Mbuyanga,
  • Hymn 887 Pakupempherera
  • Hymn 1773 Monga anapangana
  • Hymn 886 Chikondi, chimwemwe,
  • Hymn 899 ‘Tate wa Kumwambako,
  • Hymn 480 Tifunitsa Inu tere,
  • Hymn 631 Mulungu wa Yakobo Inu, mdyetsa anthu anu,
  • Hymn 816 Mdima wafika,
  • Hymn 1748 Ambuye tsopano lino,
  • Hymn 888 Polowa ndi Inu
  • Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,
  • Hymn 1817 Ndi m’munda muja chete, phee!
  • Hymn 1655 Mbuye Yesu,
  • Hymn 632 Tsopano tipereka mapemphero athu ano,
  • Hymn 300 Ona Mwanawankhosayo
  • Hymn 106 Ife, tapulumukadi,
  • Hymn 91 Ufuna kuyera kopambana?
  • Hymn 97 TIYAMIKE Mlunguyo,
  • Hymn 335 Mtembenuke mtima wanu,
  • Hymn 22 Mbuye mtsitsimutse!
  • Hymn 1215 Ndimkonde Kristuyo,
  • Hymn 473 Mzinda woyerawo!
  • Hymn 1222 Bwenzi ndimamkomanayo
  • Hymn 364 Ali wokhululukira;
  • Hymn 539 Anafika ‘kazi omwe
  • Hymn 2 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 1782 Poyamba paja analenga
  • Hymn 355 DZIKO lonse mlambire
  • Hymn 1408 Kodi mwalandira Yesu?
  • Hymn 1091 Mulamulire mtima, Yesu,
  • Hymn 1831 M’mitsinje yamtendere mtima wanga aumwetsa;
  • Hymn 1853 Etu ine, etu ine,
  • Hymn 1715 Kodi misozi itisowa,
  • Hymn 444 Mpemphe Mbuye asunge
  • Hymn 914 Nlokoma Dziko langa!
  • Hymn 481 USACHIMWE konse,
  • Hymn 263 AMBUYE mundisunge
  • Hymn 958 Ndikalowa m’mtsinje muja,
  • Hymn 889 Pemphera m’mbanda kucha,
  • Hymn 633 Tikasokera m’njira mutilondolere ndithu,
  • Hymn 233 M’mene ndapenya mwazi wa
  • Hymn 138 SANGALATSA akusowa, masiku alikutha,
  • Hymn 27 “Msanga ndidzabweratu,
  • Hymn 838 E, tsiku lonse Inu ndifunitsa;
  • Hymn 163 MALO anachepa,
  • Hymn 248 M’MENE ine ndisauka
  • Hymn 1316 Ndabwera kwa Ambuyeyo:
  • Hymn 1143 Tikhale ndithu pomwepo;
  • Hymn 1037 Mapemphero athu
  • Hymn 1543 Idzani, Mzimu Inu,
  • Hymn 136 Atumwi atummika, atumika,
  • Hymn 901 Musatifikitsemo
  • Hymn 925 Kodi umadandaula:
  • Hymn 1331 Yesu wathu Mbuyeyo
  • Hymn 1386 Ndi chifundo atipenya
  • Hymn 1626 Mbuye Yesu adzabwera,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version