Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 216 NDISAUKA, ndinachimwa,

  1. Home   »  
  2. Hymn 216 NDISAUKA, ndinachimwa,

Hymn 216 NDISAUKA, ndinachimwa,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 216 NDISAUKA, ndinachimwa,

 

NDISAUKA, ndinachimwa,
Koma Inu m’nandifera;
Ndimo ndamva mund’itana,
Mwana Mlungu ndingobwera.

Ndisauka, ndimasowa,
Mphamvu yakuyera m’mtima;
Mwazi wanu wanditsuka,
Mwana Mlungu ndingobwera.

Ndisauka, sindikhoza,
Kuiletsa nkhondo m’ mtima;
Ndi chisoni, mantha nkhawa,
Mwana Mlungu ndingobwera.

Ndisauka, sindiona,
Ndingodwala, ndilefuka;
Zonse ndizitaya kwa ‘Nu,
Mwana Mlungu ndingobwera.

Inde, Yesu, mulandira,
Muchiritsa, m’ pulumutsa;
Mawu anu ndivomera,
Mwana Mlungu ndingobwera.

Inde, Yesu, mundikonda,
Zonse zina ndazitaya;
Tsono kukhala wanu,
Mwana Mlungu ndingobwera.

Post navigation

Previous: Hymn 200 YESU mundimve, ndikuliratu,
Next: Hymn 221 A! CHIKONDI chopambana,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 57 TIYENI, dzalireni nane,
  • Hymn 815 Dzuwa lapita,
  • Hymn 359 TADZUKA mzimu wanga ‘we,
  • Hymn 1258 Zonse zina sizikwana,
  • Hymn 1656 Inu mundibisadi
  • Hymn 683 Musamaopa kanthu ‘yi, tamani Yesuyo;
  • Hymn 538 Iye anachoka kwawo,
  • Hymn 1790 Imfa ya anthu ake imkomera,
  • Hymn 146 Inu ndidzatama
  • Hymn 1246 Ambuyanga, ndalephera,
  • Hymn 271 Zoipa zangazi
  • Hymn 1833 Podwala ine pobvutidwa Andisamalira;
  • Hymn 201 Ngati zakuipa zathu
  • Hymn 678 Ibukike mbiri yanu,
  • Hymn 1577 “Kwa Iye atikonda
  • Hymn 936 Ukatha moyo wanga
  • Hymn 79 Mlendo ali pakhomo,
  • Hymn 1307 Ndi ine simufuna ‘yi
  • Hymn 921 Komwe Mbusa kwawoko
  • Hymn 139 Bwerani inu nonse, inu nonse,
  • Hymn 233 AMBUYE Mulungu,
  • Hymn 802 Ndife anthu aulendo,
  • Hymn 123 Koma mudzisungire chuma cha Kumwamba
  • Hymn 288 Ndi maso athu awa nawo nganu,
  • Hymn 1783 Tinasokera ngati nkhosa,
  • Hymn 409 ANTHU akum’maŵa
  • Hymn 95 Palibe mmodzi akanatha
  • Hymn 1631 Mudzabwera, mudzabwera;
  • Hymn 197 NDIKHULUPIRA’Nu,
  • Hymn 376 Adzadalitsa ‘fe
  • Hymn 78 ALINKUDZA wansoni Munthu,
  • Hymn 1451 Okoma ndiwo mawu
  • Hymn 1275 Mtima ‘we siya ndi Yesu nsonizi,
  • Hymn 364 Ali wokhululukira;
  • Hymn 428 Tiyandika, Mbuye,
  • Hymn 199 NDINASOKERA kutali,
  • Hymn 3 TIMYAMIKIRE Mlunguyo,
  • Hymn 46 INALIPO nthawi,
  • Hymn 327 NTCHITO yonse yakeyo
  • Hymn 1785 Tiyeni tizipita kwathu,
  • Hymn 894 Mbuye, ndinu Mfumu yanga
  • Hymn 144 Yesu, ndipemphera
  • Hymn 1836 Ndi wamwayi munthu uja
  • Hymn 336 Perekani mtima wanu
  • Hymn 1802 Mulungu anatuma,
  • Hymn 308 Ifetu kuchimwa, Mbuye,
  • Hymn 969 Akathira nsembe
  • Hymn 481 USACHIMWE konse,
  • Hymn 1676 Kondwerani dzuwa lino Aleluya,
  • Hymn 226 Nditama mwaziwo!
  • Hymn 1180 Ndine kapolo wa Mbuye wanga;
  • Hymn 636 Yehova Mlungu wathu,
  • Hymn 114 Ndine Mbusayo wabwino,
  • Hymn 606 Dzinja lokondweretsa lafikanso,litapumatu,
  • Hymn 1402 Mverani Iye ati: idzanitu;
  • Hymn 426 MBUYE, Mpingo wanu usauka kwakukuludi;
  • Hymn 140 NDINAMIRA m’machimo, wosaonekanso,
  • Hymn 480 TIANA ife tingofoka,
  • Hymn 381 MONGA zomera zonsezo
  • Hymn 719 Anu Mbuye ndifetu!

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version