Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 216 NDISAUKA, ndinachimwa,

  1. Home   »  
  2. Hymn 216 NDISAUKA, ndinachimwa,

Hymn 216 NDISAUKA, ndinachimwa,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 216 NDISAUKA, ndinachimwa,

 

NDISAUKA, ndinachimwa,
Koma Inu m’nandifera;
Ndimo ndamva mund’itana,
Mwana Mlungu ndingobwera.

Ndisauka, ndimasowa,
Mphamvu yakuyera m’mtima;
Mwazi wanu wanditsuka,
Mwana Mlungu ndingobwera.

Ndisauka, sindikhoza,
Kuiletsa nkhondo m’ mtima;
Ndi chisoni, mantha nkhawa,
Mwana Mlungu ndingobwera.

Ndisauka, sindiona,
Ndingodwala, ndilefuka;
Zonse ndizitaya kwa ‘Nu,
Mwana Mlungu ndingobwera.

Inde, Yesu, mulandira,
Muchiritsa, m’ pulumutsa;
Mawu anu ndivomera,
Mwana Mlungu ndingobwera.

Inde, Yesu, mundikonda,
Zonse zina ndazitaya;
Tsono kukhala wanu,
Mwana Mlungu ndingobwera.

Post navigation

Previous: Hymn 200 YESU mundimve, ndikuliratu,
Next: Hymn 221 A! CHIKONDI chopambana,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 196 Tidzimba komweko nyimbo
  • Hymn 1036 Mtima wakufatsa
  • Hymn 1308 Ndi ine, m’mtima Mwanu mbee!
  • Hymn 1654 Mbuye, mutsaganetu
  • Hymn 132 Ganizansoni, ali pano,
  • Hymn 37 Pozunzidwa inu ponseponsepo
  • Hymn 1849 Nthawi zonse monga ‘Tate
  • Hymn 349 MOSE anamenya thanthwe kawiri,
  • Hymn 169 M’manda nagonamo
  • Hymn 57 TIYENI, dzalireni nane,
  • Hymn 632 Tsopano tipereka mapemphero athu ano,
  • Hymn 408 ABALE nonse mulindiranji?
  • Hymn 724 Ndine mlendo pansi pano,
  • Hymn 769 Ndi kutsukidwa m’mwazimo
  • Hymn 411 TAMVA mawu omwewo,
  • Hymn 350 Yesu ati,
  • Hymn 655 Ndiphunzitseni, Mbuyetu,
  • Hymn 463 MNANDIDZERA, Ambuye,
  • Hymn 1713 Zochimwa zanga zonsezo
  • Hymn 1047 Ambuye, chotsani zonse zomwezo
  • Hymn 925 Kodi umadandaula:
  • Hymn 453 Tiana ta Ambuye tili
  • Hymn 119 M’BUKU la moyotu Mbuye,
  • Hymn 1116 Kwawo kwa Mbuyako
  • Hymn 86 Mwandipatulira ine,
  • Hymn 305 NDALIMVA dziko la m’talimo,
  • Hymn 1352 Atate wa Kumwambako,
  • Hymn 531 Pakubweranso Inu m’Ufumuwo
  • Hymn 1270 Ndayesa kudzikonzadi,
  • Hymn 58 Titasokera tinabwerera,
  • Hymn 8 Nanu Atumwi akumveka aja,
  • Hymn 331 Yesu ndimafuna Inu,
  • Hymn 380 Ndipyola kodi chikhwawa
  • Hymn 800 Yesu munadzukanso
  • Hymn 1125 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 1800 Kalelo anthu onse
  • Hymn 398 Lero lino mwatipatsa
  • Hymn 289 Ndi manja athu awa nawo nganu,
  • Hymn 1605 Yesu, dzina lokondwetsa
  • Hymn 314 E, moto wanu woyera
  • Hymn 1520 Mbuye, Mawu anu
  • Hymn 1583 Dzina la Yesuyo
  • Hymn 516 Zitsamba zakuyera
  • Hymn 514 Osanatu, osana,
  • Hymn 653 Nditsogolere m’njirayi
  • Hymn 1297 Kumwamba komwe n’dzaimbira
  • Hymn 471 Mbuye, tili ana anu,
  • Hymn 189 MLENDO ali pakhomo,
  • Hymn 123 MULI ndi ludzu, idzani
  • Hymn 30 YEHOVA, Mbusa wangadi,
  • Hymn 812 Ndi ena sanamvera ‘yi,
  • Hymn 674 Anthu onse taukani,
  • Hymn 435 ANAKWATIRA kale
  • Hymn 882 Kodi tikulema nazo
  • Hymn 1051 Zin’sowa indedi
  • Hymn 407 Zochimwa sizilowako,
  • Hymn 506 Ndikondwa kuti Yesu akonda,
  • Hymn 1415 Iye anatsika m’Mwamba,
  • Hymn 737 Mommuno, Mbuye, tionanetu,
  • Hymn 219 YESU Mbuyetu, mwafera

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version